Тёмный

2025 Kuvuta nkhondo yi ikhala Jane Ansah vs Annabel Mtalimanja 

Malawian Cameras
Подписаться 30 тыс.
Просмотров 22 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

11 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 141   
@AdamAhamad-k2i
@AdamAhamad-k2i 24 дня назад
Mwana wa John tembo ndiwa mcp kumene chakwera akufuna kubera mavote koma kuzamvuta simasewera
@ziwani3682
@ziwani3682 23 дня назад
APM my vote
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 23 дня назад
APM uja osazaphwekesa
@kekeaufi9834
@kekeaufi9834 24 дня назад
*A Boni Kalindo akuphika zotibweletsela asowatu 🎉🎉🎉🎉*
@priscillamangata4023
@priscillamangata4023 23 дня назад
Ndipo wasowadi apezeka mawa
@JoshuaNyirongo
@JoshuaNyirongo 23 дня назад
Zisankho it will be just a formality....gule kwao already
@damianokachingwe3531
@damianokachingwe3531 23 дня назад
Kkkkk pitala walephera even kupanga hold convention kudzalankhula komaliza chifukwa chokalamba ndie angayendetse dziko
@MarthaPhiri-q8m
@MarthaPhiri-q8m 23 дня назад
​@@damianokachingwe3531aaaaaa inu munali ndi cholinga chofuna kumuchera pobwerera mwagwa nayo achimwene amene uja si mwana anakuwerenga kare kuti kuli mbora nde mumafuna mumuchite mbora ng, ooo
@damianokachingwe3531
@damianokachingwe3531 23 дня назад
@@MarthaPhiri-q8m kkkkk km iwe waganiza bwanji ndani angataye nthawi imeneyo pa mdala amene uja,don't force matters please munthu sangalankhule for 2hrs choima ndibodza limenero vomerezan chilengedwe
@JohnBanda-ux9fy
@JohnBanda-ux9fy 24 дня назад
APA panunkha kkk tambala tamugwira pakhosi
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
😂😂
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 21 день назад
Ndipo kwambiri
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 23 дня назад
MCP idaononga mbiri pa 10 june nde vuto.. and sakubweresa report mpaka pano
@jackmambo2638
@jackmambo2638 23 дня назад
DPP is a system mwavomelazano😂😂
@yotamumahomed1313
@yotamumahomed1313 23 дня назад
Ndimmene tikuvela kuwawa amalawi ambirfe singalore chakwera apitilize apapa nde bola tifele chilungamo
@blessingsmimu5236
@blessingsmimu5236 23 дня назад
😂😂😂sakusamalaso zochosa moyo wamunthu
@brainsmkumbwa6267
@brainsmkumbwa6267 23 дня назад
Kuchokera pamene ndinamva kuti boma lamukhulukira Boni Kalindo milandu yache sakuonekanso,nkutheka pamwamba pa kukhululuka anapatsidwa ma millions ngati Chibanzi ,koma ndingadandaule bwanji chifukwa ndiyekhayo akuyankhulira amalawi tonse
@ReginaMulipa
@ReginaMulipa 23 дня назад
Sanapasidwe kathu iye uja samapanga za nyerotu akuti amadwala mupange search watulusa odio lero wapepesaso kuti amadwara alipo ndithu
@user-ms8tm3yf7d
@user-ms8tm3yf7d 21 день назад
Mhmmm ukunama aise amene ndi The DC
@YaqoobStandwell
@YaqoobStandwell 23 дня назад
Dpp ndiyowina kale
@MjombaMjuba
@MjombaMjuba 23 дня назад
Taa, ng'ooo mudzakhumudwa
@AchinaKellz
@AchinaKellz 23 дня назад
Exactly bro
@TamUs-u2h
@TamUs-u2h 23 дня назад
Tipex Thief Jane Ansa. Mtalimanja ndi machine Jane Ansa tipex Ansa wachepa
@VictoriaSibande
@VictoriaSibande 23 дня назад
Ukunama iwe chitsiru
@AustinMhone-r3s
@AustinMhone-r3s 23 дня назад
Zitsankho zogwiritsa ntchito akazi kubera mavoti no use of voting.
@BladesBullets-pu5uw
@BladesBullets-pu5uw 23 дня назад
Chakwera adaziipitsira posamutsa ma office omwe amabweretsa mwayi wandalama kwa ochita malonda matauni a Zomba ndi Blantaya nkuwasamutsira ku Lilongwe. Komwe kuli kupha chigawo chakummwera. Choncho muchigawochi adzangopeza mavoti ambuli zo
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 21 день назад
Apm my vote
@DalitsoPhiri-sq5nl
@DalitsoPhiri-sq5nl 21 день назад
Mistake yomwe amalawife achita maka aku opposion ndikuvomereza kuti ayese machine pamenepo ndi pomwe game yagonera mcp mphamvu zawo zili pamenepa cz monga kalindo ananena njirayo ndi imodzi yozabela next season
@OssmanAbubaker-k9w
@OssmanAbubaker-k9w 19 дней назад
Zoonadi brother simukunama apatu MCP singawine ngakhale atabera motani
@ChitsanzoMizere-tz7ye
@ChitsanzoMizere-tz7ye 24 дня назад
Kkkkkkkkk amwene koma mumaganiza apapa nde kunkhala drama sure and mwachiziwikire Jane asah azankhale monitor kkkk
@Ahlubyt
@Ahlubyt 24 дня назад
😂😂😂 Azakhaledi monitor 😂😂
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 23 дня назад
Adzakhar bwanj monitor ali phungu ? DPP inazolowela kubela kma MCP ndi 70+1
@blessingssaiti
@blessingssaiti 23 дня назад
Tizayenda kumene ASE MCP atayivotere ndan komaso inu khan imeneyo isiyeni zimenezo mumuphesa munthu
@Ahlubyt
@Ahlubyt 24 дня назад
Send a thief to catch a thief 😂😂😂😂
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 23 дня назад
😂😂😂
@user-xo8ms5wh2s
@user-xo8ms5wh2s 21 день назад
Adzawina ndi Dpp chifukwa iyenda ndi UDF,ndi Aford,UTM ndiye azaluza bwa
@user-en3ts5cp9l
@user-en3ts5cp9l 23 дня назад
Pamenepa yalakwa kkkkkk
@user-lv8yi7dm1l
@user-lv8yi7dm1l 19 дней назад
Iweso ndiwa dpp mcp sinaluzepo amayibera ili fans
@ChawandaBanda
@ChawandaBanda 23 дня назад
Musaganize kuti mungadzachotse MCP ndi mademo ngati itawina! Zimenezo iwalani chimene muchite ndikupanga kampeni kuti mudzawine basi
@MandalaChaona
@MandalaChaona 23 дня назад
👹🔨⛏️⚒️👹 Chikangawa Party 😂😂😂Devil at work
@rashidadan2533
@rashidadan2533 24 дня назад
Kodi muli ndimaloto oti Mr chikangawa azawina ??
@PeterChalechale-pz2bp
@PeterChalechale-pz2bp 23 дня назад
Mukapanda kusamala kukhala civil war Malawi be ready for any attack
@MjombaMjuba
@MjombaMjuba 23 дня назад
Zamkutu, mumayidziwa inu nkhondo, agang'anthi
@SurprisedDarts-di6fs
@SurprisedDarts-di6fs 23 дня назад
APM VOTE
@EllahEllah-hu7hi
@EllahEllah-hu7hi 22 дня назад
Dats true,aend a thief to catch a thief(ziliko)
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 22 дня назад
Mulungu ndiwadongosolo mwina wapanga dala kuti ikhale 50.50
@PempheroAlufandika
@PempheroAlufandika 23 дня назад
Mwana wa John tembo asamale azaona nyenkhwe
@KaliyapaSeeter
@KaliyapaSeeter 24 дня назад
Koma ine akulu awa nde amandisangalasa❤❤
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
🎉🎉❤Thanks 🙏
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d 24 дня назад
Amayendana pansi palibe kubela zisankho kkkkkkkk chaka Cha mawa kuli zinthu za nyo
@user-sh5wq4uf6r
@user-sh5wq4uf6r 23 дня назад
MCP PAYOKHA SINGATENGE BOMA MA DEMO AZAKHALA OCHEPA KOMA NKHONDO BASI
@kha6068
@kha6068 15 дней назад
You are just imagining things tachoka iwe
@PetersKondana
@PetersKondana 18 дней назад
Pointless, straight wine for APM
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 24 дня назад
Ada awawa ndazelu chimene amandisangala ine akabwela khani satenga mbali enawa mmalo angoponya khani koma kuyikokomeza kuchita kunetsa kuti iwowo Ali mbali ya DPP
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
❤🎉 Thanks broh 👌
@aminikondwani9361
@aminikondwani9361 23 дня назад
Ndipo kudzavuta 😢😢
@Biath-m4b
@Biath-m4b 23 дня назад
Koma iweyo sindmapanga comment koma lero wandisangalatsatu keep it up bro ukuesetsa ntchito
@harrispheleni2205
@harrispheleni2205 19 дней назад
Ndiwe galu ufuna kupereka perception yofoila
@AndersonBishop-i2t
@AndersonBishop-i2t 23 дня назад
Akazangoyelekeza kubela anne mtalimanja wawoyo azaonongesa ziko azawona cnanga ana atenga mwana wa tembo kuti azabele zisakho akhawula awonaso sitizalola tikuziwa kuti chikangawa ndi woluza luza kale ameneyo or atamati ku votako mawa chikangawayo sangawine ka 😂😂😂😂
@learnermuyaya-en9xi
@learnermuyaya-en9xi 18 дней назад
Kkkkk, ndipo live apa ndi game ya mbava zokhazokha
@RobertCosmas-bo1uo
@RobertCosmas-bo1uo 23 дня назад
Kkkkkk umakwana iwe wabwera
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
😂😂Thanks broh
@user-fm7yg5yc2c
@user-fm7yg5yc2c 23 дня назад
Koma bro😂😂😂😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
😂😂😂😂
@GraciousKhonje-k8f
@GraciousKhonje-k8f 24 дня назад
U are intelligent man
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
❤🎉 Much love thanks 🎉
@AdamMntonintshi
@AdamMntonintshi 20 дней назад
Apm my vote 🗳 ❤️
@BennettNjedza
@BennettNjedza 22 дня назад
Dpp ilowa awo kwao kwatha
@user-nz5jg5hv1m
@user-nz5jg5hv1m 23 дня назад
Aise zamademo usakaike mwinanso nkhondo
@NedGft
@NedGft 23 дня назад
Mcp sinawinepo zisankho
@kubengovender6996
@kubengovender6996 23 дня назад
Big up brother man!!
@paulnyondo7572
@paulnyondo7572 23 дня назад
Kkkk a send thief to catch a thief😂😂😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
😂😂😂😂😂 Eeeeeetu azagwirana ufiti
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 23 дня назад
Kodi DC anapita kut kwangoti zii
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t 23 дня назад
Uzikhala serious poyankhula
@MuhammadSamson-yz1kl
@MuhammadSamson-yz1kl 23 дня назад
Kungobera kuzanunga linya
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
Eeeee kwambiri 😂
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d 24 дня назад
Bolani asamupheso Jeni Ansa yo a MCP
@Ahlubyt
@Ahlubyt 24 дня назад
Athadi kumusowetsatu 😂😂 asamale kwambiri
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
😂😂😂
@PreciousHenderson-qc1hq
@PreciousHenderson-qc1hq 23 дня назад
APM My vote🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh 23 дня назад
Ife chimanga tikuchisinja mutondo
@user-ld8gb9xm7v
@user-ld8gb9xm7v 23 дня назад
Kumpoto tili pheee kudya zammathumba mwathu
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj 23 дня назад
🙏🙏🙏🙏🙏🙏
@user-vm7iz6oz6r
@user-vm7iz6oz6r 22 дня назад
Tamugwila pa khosi tambala
@HendrickBanda
@HendrickBanda 23 дня назад
Kuzavuta
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
Heavy
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh 23 дня назад
Kuzavuta kumwela Koko
@MerryWayson
@MerryWayson 23 дня назад
Kkkkkkkkkk nkhaniyo ndiyowona kuvutad
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 22 дня назад
Mumakwana Pali mwambi amati mwana mbuu make mbuu
@peterchikwakwa8476
@peterchikwakwa8476 24 дня назад
Paja winiko ananenatu kuti 2025 kuli zinthu 😂😂😂😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
😂😂😂 Atijigira madzi akuti mmidzimimu 2025
@SandfordBanda-gk2dp
@SandfordBanda-gk2dp 23 дня назад
Pajatu ndi 50+1 musayiware
@MosesDzonzi-em5px
@MosesDzonzi-em5px 23 дня назад
Ka Jane ansah nikandaniso kameneka kayidziwa MCP kuti sikugawa kamba idzawina iyeyo akuwona and adzavomekeza kt MCP wawina
@thomaswyson-e2q
@thomaswyson-e2q 21 день назад
Atiazvote ndiye ndiabamboako ndiamayiako kuphatikiza akazako anaako kumanso nkhukuzakwanu zonse olonso osazaiwala agalu ndiamphaka omwe kut ambwiyakoo azawine
@Martha-m6e
@Martha-m6e 24 дня назад
MCP zinawavuta chifukwa cha anthu anafa ku Chikangawa. Anthu tilibe mayankho
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
This is true Mayankho mpaka pano sanabwere
@FatimaUmali-pc8sy
@FatimaUmali-pc8sy 23 дня назад
❤❤❤❤
@daviechibwana3137
@daviechibwana3137 15 дней назад
Ine sindingavotere munthu oti Mano mkamwa anatha nkhalamba ine ai 😂😂😂😂😂😂😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 15 дней назад
@@daviechibwana3137 Boss mukuyankhula bwanji akumenyanitu anthu😂
@Jibsan-t2f
@Jibsan-t2f 24 дня назад
Mn pangani nzero ina.imemeyo simunaganize bho inuyo
@Ahlubyt
@Ahlubyt 24 дня назад
Ngati iyeyo akupanga nzeru? Mesa akuuzan za zomwe zizachitike kapena ndinu a Malawi Chikangress party 😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
Okay ndanva inusl mupeze comment ina ya nzeru iyiyi mulibemo zeru yayi😂
@SelinaGamaliyere-q8v
@SelinaGamaliyere-q8v 23 дня назад
Dpp 2025 woyeee
@user-rf4br1fv2z
@user-rf4br1fv2z 23 дня назад
Kutathauza kuti 2019 Jane adabela chisakho kuti pitala awine basi nowonso adzabela
@user-lp2sd7lt8b
@user-lp2sd7lt8b 23 дня назад
Kugwetsa boma sizamasewera
@StevenDastan-b9u
@StevenDastan-b9u 19 дней назад
Kkkkk koma ndiye
@SuzgoMkandawire-ss4kh
@SuzgoMkandawire-ss4kh 23 дня назад
Kungowina chakwera kudzachela tidzamatcha mpka kuchikangawa
@BLESSINGSSTOLO-lt9di
@BLESSINGSSTOLO-lt9di 17 дней назад
Ndipo ndili pambuyo Pako mix watitopesa mmmmh 😊
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 23 дня назад
Azakhaula
@fahadhasan2222
@fahadhasan2222 23 дня назад
50+1 m,bale
@Shamsdeenchikwakwa
@Shamsdeenchikwakwa 23 дня назад
😂😂Kuzachema
@INNOCENTMOFOLO-io8tg
@INNOCENTMOFOLO-io8tg 23 дня назад
ndipo kuzakhala kuomberana tizavotaso kawili
@FrankChanza-l3g
@FrankChanza-l3g 23 дня назад
Iwe tikamati ndiwe chisilu wawonatu kape wa mcp iwe galu
@Ahlubyt
@Ahlubyt 23 дня назад
@@FrankChanza-l3g Anthunu nde simukumunvetsatu munthu yu ena akumunena kuti wa Mcp ena akuti wa Dpp😂 video yi mukuionera bwanji kodi sanaimire mbali iliyose tu uyu apa
@Ahlubyt
@Ahlubyt 24 дня назад
😂😂😂😂 Apapa agwirana umbavadi 😂😂😂😂😂😂
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 23 дня назад
Ai Macson mbendela anabela zisankho, jane ansah anabelas ai palibe kusintha boma apa
@DONNEXKhama-bk1gy
@DONNEXKhama-bk1gy 23 дня назад
Ndipo 2025 kuvuta koopsa ..😂😂
@MoreenSemu
@MoreenSemu 20 дней назад
Jen asah wachani
@Edwinsanga-zh4yv
@Edwinsanga-zh4yv 20 дней назад
DPP bomaaaaaaaa 😅😅😅😅
@user-pf5er7gc9s
@user-pf5er7gc9s 23 дня назад
Akulu mukufuna mukambe chani sizikumvekatu
@GanizaniMagalasi-i1y
@GanizaniMagalasi-i1y 23 дня назад
Iweyo ndichitsiru kwambiri ase sukudziwqnso chimwe ukuyqnkhula
@Ahlubyt
@Ahlubyt 23 дня назад
Aaaaa iweyo nde namache... Chikangawa
@ClementMunyolowa
@ClementMunyolowa 24 дня назад
Kodi uli mbali ya mcp olo zita vuta ulendo basi
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
Ai baba 😂 nkhani ili apa ndiya Zisankho osati wa Mcp or not 😂
@MaikNkhoma
@MaikNkhoma 23 дня назад
Kape iwe timakudziwa kale ndiwe wa dpp koma ulendo Uno mulimwdzi Boma sitikusintha
@MalawianCamera
@MalawianCamera 23 дня назад
😂Ena akuti ndine wa Dpp ena akuti ndine wa Mcp 😂😂 That's what happens when you take me seriously Why so serious? 😂
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 23 дня назад
Boma sitikusintha jane ansah anatipanga kale chipongwe
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js 23 дня назад
Thieves and evil.
@user-xj9uy6wz7b
@user-xj9uy6wz7b 23 дня назад
😂😂😂😂😂
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 24 дня назад
Apaaa MCP yagwidwa basi ma plan awo atha basi😂😂😂😂😂
@MalawianCamera
@MalawianCamera 24 дня назад
😂Iwo anzao anawathothola ndi Mademo nao ayembekezere zomwezo 😂
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 23 дня назад
@@MalawianCamera 🤣🤣🤣🤣Ndipo Adha apapa kulinkhondo koopsa Zedi azalira a MCP 🤣🤣🤣🤣🤣 wapanga dala Jane Ansah Kuti azizati lakutipo tionenso nanga apaaa bwanji?🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of 23 дня назад
Dr Lz 2025 boma kale
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 23 дня назад
Ukulota ase kuchokera 1984 Mcp sitingawine payokha ma bwana anuwo akutiimbila phone kuti apa zavuta nde inu mukuti chani apa ena ayamba kale kugula nyumba kuno kudzakhala ena atumiza kale family yawo sitingawine ase
@ThokoMsonkho-hy4uc
@ThokoMsonkho-hy4uc 23 дня назад
Chakwera sangawine zisankho 2025 pokhapokha adzabere. Koma akadzangobera zidzaziwika bcoz ambiri samamufuna, tidzaonera zobwibwi
@spargomw
@spargomw 23 дня назад
Maloto achumba😂😂😂😂😂
@paulkalizangoma5904
@paulkalizangoma5904 23 дня назад
Day dreamer lwe!
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 22 дня назад
@@ThokoMsonkho-hy4uc komaso kubelako zivuta Jane Ansah maso alipompo paja nayeso ndi dolo kkkkkkkuchematu
@ElizaKumwenda
@ElizaKumwenda 23 дня назад
APM my vote
Далее
Open Message to Mathews mtumbuka
9:45
Просмотров 15 тыс.
Самый БОЛЬШОЙ iPhone в МИРЕ!
00:52
Просмотров 1,2 млн
Вопрос Ребром - Булкин
59:32
Просмотров 953 тыс.
TIMES TV KUING'ALULA MBC TV - APWETEKANA AWA🙌🙌
30:44
Obaseki: PDP May Not Sign Peace Accord
15:44
Просмотров 3,2 тыс.
MLELEMBA | KALIKOKHA NKANYAMA
21:26
Просмотров 32 тыс.
Nancy vs Che Nkope - Comrade Mitambo
13:52
Просмотров 11 тыс.