Dear SKC wherever you are the guy you trusted is no longer value what you planned for young and old generations 💔💔 our hero continue resting well😢💔💔 if it means to take us to promise land through him then God forgive us 💔 you departed un-expectedly ndife athu nditha kukakhula or kuganiza zambiri 💔💔💔 komwe muliko SKC control us spiritually through God intervention. 🙏🙏 we missed you so much at least mukanasiya mau or umboni winawake kuzera mwa ena ake or mulungu oneserani mphamvu yanu potitengera kuchoona 🙏💔❤️🙏
Chipembezo will remain a potent weapon mu toolbox ya wa ndale wa mu Africa. No wonder, wandale and wamkachisi/wamumzikiti are always pachinzake. Akangosemphana, systems fall.
Abale ndale mpaka mu church mupta nazo kut izi, Jesus Christ is the president of presidents, Judge of Judges, please, please 🙏🙏🙏. Muzwakonzera masku apadera anthu awa osamaphatikiza ndzaumulungu please let God be God
Koma zoti winawake anadzeetsa mavuto akuthawira Ku Nenevi mu sitima ukuzidziwa?Phepo NDI mafundo zidatha atamuponyera madzi kumezedwa NDI nsomba ukudziwa iwe Manganya
Koma Utsi kunena zoona u vp sakukwana, zoona vp anganene kuti dzikoli eniache ndi ama church ndi boma uyudi bolaa drama aja amapanga koma za u vp ndiye panja angochitadi kumukokerapo
Ok! Chifukwa Cha chikondi ndiye ife tizikuyimnirani mmanja mukulephera kukwaniritsa zomwe mudalonjeza? Maganizo opepera ochokera Kwa vice president. Worry not one year remaining
Funso komwe akufunsa amalawi kuseriku nlakuti Kodi anthu omwe akukukondani inu a Michael Usi azapereke Mavuto Anu Ku UTM kapena Ku MCP yankho liri lonse lomwe mungapereke perekani zifukwa zake
AKUONA NGATI KUPEZEKA KU CHURCH MULUNGU AKUKHULULUKIRANI MUTAPHA CHILIMA AGALU INU MANGANYA NDALE SIMBALIYAKO PITA KU TIKUFERANJI MFITI YACHABE CHABE IWE PETRO OMPEREKA YESU
Ochimwa ndi chakwera yemweyo coz anasiya ntchito yake ya ubusa kukayamba ndale, nde mulungu wakwiya naye ndipo akufuna awonese ukulu wake pa chakwerayo. Iyeyo si mulungu ayi, komaso amalawi si ochimwa, mr chikangawa nde ochimwa
Woipa amabisala nchurch,usamànene za MCP NDI chakwera m'busa wonyenga wakupha.chilima,ndiwe amene chitsiruu Satanayo ndiwe galu.uku tenga za zisuzo kupita nazo ku church, mpamene uku mango imba nyimbo za kuthezo pa msonkhano mbuli mbuzi ya Munthu Iwetu si president adaku sankhula ndani?mbava inzako chakwera mu ulure amene adapha Chilima,ankhandwe Inu,mu charichi simo ya nkhula za m'boma Wanthu aSatana Inu,mu ulure za imfa Ku Chikangawa mbuzi inu
A dpp chilima amamunyoza kwambiri wamwalira ayamba kumuyamikira zichani zimenezo. Mukuwona ngati achina kabambe ndi a utm aja ndima supporter's a dpp kuyambira kale kale mumupase u president muwone mugulisa chipani
Aaaa palibe chikumbvekapo apa maiko ambiri kunali cyclone sikuti ndi Malawi yokha koma maiko anzathu wo bwanji akuyenda? Muli pamaso pa Mulungu mudzinena chilungamo