Тёмный

A Thabo Chakaka Mupangitsa Manyazi Dziko La Malawi - Concerned Citizen 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 25 тыс.
Просмотров 21 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen says Attorney General Thabo Chakaka Nyirenda is embarrassing the country by giving the President poor legal advice.
Pa Nyasa VoiceBox, mzika yokhudzidwayi yati loya wamkulu wa boma Thabo Chakaka Nyirenda akuchititsa manyazi dziko popereka uphungu wolakwika pa zamalamulo kwa mtsogoleri wa dziko lino.
#malawi

Опубликовано:

 

6 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 101   
@FranklinNdovi
@FranklinNdovi 2 месяца назад
Why did President Chajwera remove Dr chikosa Silungwe? Dr chikosa Silungwe is a competent lawyer who has had worked in the Malawi Government for long long time with vast experience but because he advised the government accordingly. Mr Thumbo chajaja Nyirenda is an incompetent lawyer he occupied that seat because of political reasons and nothing else. somebody in the MCP had just favoured him yo become the Attorney General of the Malawi Government. Shame on you the president and his politically appointed Attorney General Thabo chajaja Nyirenda. He had never won cases in the Court of law for the RBM and his other clients before. Therefore the President should now terminate his fake appointment on that post of the Attorney General and give it to the rightful competent lawyers with vast experience. He is as incompetent as the former DPP before Dr Kalua.
@FunnyBasketball-er3vc
@FunnyBasketball-er3vc 2 месяца назад
The problem is ,the president advises the attorney general
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 2 месяца назад
Abambo awa akukalipa zoon, Thabo Chakaka sakukwana kulangiza boma, moti akuwononga ndalama za boma pochita zonsezi. Amuchotsepo paudindo.
@geraldtuwaga-iz6ll
@geraldtuwaga-iz6ll 2 месяца назад
Chakwera, ana mchosa silungwe, kadaulo pazamalamulo, ankafuna oti aziba naye, komanso kuphinja Malawi
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 2 месяца назад
For sure
@Eric-gb9ms
@Eric-gb9ms 2 месяца назад
Zoona big
@chitanibenito1109
@chitanibenito1109 2 месяца назад
Chakaka nyirenda chisiru cha munthu akumusochelesa president nkhani ya streight forward then why wasting kumakatenga chileso. Are you pleasing president for wat?? Are you quolified?? Anakutenga kuti??.
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v 2 месяца назад
Chakwerayonso ndi mbuzi yamunthu galu
@jamesgondwe6669
@jamesgondwe6669 Месяц назад
Thabo is just an honour's degree holder.
@Moffat-oi4yx
@Moffat-oi4yx 2 месяца назад
Mwapangitsa manyazi atumbuka anzanu ngati anthu osapita kusukilu mbuli zoyendetsa ziko.
@khoviwaedward
@khoviwaedward 2 месяца назад
Ulamuliro ochitisa manyazi mu mbiri ya southern Africa. Embassy ya dziko la kunja kupereka visa pomwe dziko lako kupereka fake passport dzoona?
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 Месяц назад
Eeeeesh 💔💔
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 2 месяца назад
Akulu awa ayakhula bwino kwambiri koma vuto lonse ndi Chakwela chifukwa sogoleri azikhala wadzelu ndiwonganiza bho
@ManesKamtambo
@ManesKamtambo Месяц назад
More fire big man you are talking
@GogomphatsoSinosi
@GogomphatsoSinosi Месяц назад
Kulankhula kolankhuliratu 😅😅😅
@JimmyKapunza
@JimmyKapunza 2 месяца назад
This is powerful iwe thabo chakaka futsek
@GrecianWyson
@GrecianWyson 2 месяца назад
Vuto NDI osewa amwene no sense chakwera 😊
@ivychithyoka1551
@ivychithyoka1551 2 месяца назад
Experience matters!!!!
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 2 месяца назад
They are busy breaking the law
@amiduclement2142
@amiduclement2142 2 месяца назад
Komaso ameneyu ndi wa mcp?
@user-zg7iw8kq4r
@user-zg7iw8kq4r Месяц назад
Ameneyi si attorney general ndi mbuzi kwabasi tsiku lina pofunika kuzamugenda miyala galu ameneyu
@user-je8jm5uy1q
@user-je8jm5uy1q 2 месяца назад
Wauza bola anve koma ngati sanva tumizani Ina audio apange manyazi
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s 2 месяца назад
Awuze bwana uyu ndi waunsilu
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
Dr Chakwela akanatha kumayendesa bwino ziko la Malawi koma vuto anthu omwe amuyandikila president ali ndi njiru kuti president azioneka oipa pomwe ndi wabwino.
@Ngwangwa-ej4rs
@Ngwangwa-ej4rs Месяц назад
Dzikoli laola kuposa nthawi ya Mutthalika izi ndiye zolopa zenizeni
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 Месяц назад
We want One Malawi One love, And this iz not Old Malawi, all the malawians know the truth people are crying and suffering Under the rule of MCP, and Chakwera the killer Man fake pastor panyini pa mawo both of them but what they should know is that, this is not Old Malawi, this cruel people must know justice of Malawian people One Day, and justice will come out One Day
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn 2 месяца назад
Pajatu anthunu munkati atumbuka ndiodzindikira kwambiri nanga izi nchiyani ? Anthuwa anasankhidwa ndi Chakwera ndipo amukhaulitsanso Chakwerayo nanga pamenepa a Chakwera zinthu ziwayendera ?
@CassimMbalaka
@CassimMbalaka 2 месяца назад
Akudxiwana wosewo alilimodxi mmesa adamusakha yekha chakwerayo
@JamilahMaluwa
@JamilahMaluwa Месяц назад
Onsewo nzitsiru retired abwelera bwanjinso mboma?
@joebrown1158
@joebrown1158 2 месяца назад
Noone is above the laws
@user-rk4ch1ly3z
@user-rk4ch1ly3z 2 месяца назад
Muthile moto kumene, mwana opusa kwambiri akuwona ngati,,zikoli lawyer alipo yekha mwana opusa kwambiri,,mukalipileni dziko akuliwononga ma guyz watu.
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 2 месяца назад
Aaaaa MCP simamva zaanthu kuyambila kele mvuto mtima wachipani chimodzi chakaka alibe mvuto mvuto chakwela ndi MCP
@jonathanmunthali8500
@jonathanmunthali8500 2 месяца назад
Ndi a Nyirenda akuti wosaphuzira 😢
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Месяц назад
We need chikosa silungwe back
@Ngwangwa-ej4rs
@Ngwangwa-ej4rs Месяц назад
He is after money not rules nao apresident aganize bwino za advisor wawo failing which mmmm
@user-bg7ur1gw1q
@user-bg7ur1gw1q 2 месяца назад
Auze anve
@user-iu6mr5xu6r
@user-iu6mr5xu6r Месяц назад
Munthu iwe Mulungu akudalise pa masomphenya ako
@BMadhlopa
@BMadhlopa Месяц назад
That Thabbo is the most failed is running away from the truth!
@PiterDeleza
@PiterDeleza 2 месяца назад
A Chembe intelligent yake ndiye yotibweresera nkhalambayo.
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b 2 месяца назад
Komanso apule anamuchotseranji lawyer oyamba uja, kuyika Thabo Chaka ka nyirendayo
@GraceLimani-zw7dx
@GraceLimani-zw7dx 2 месяца назад
Zoona amasureni athabo aaonjeza
@JimmyKapunza
@JimmyKapunza 2 месяца назад
Madala mwayankhula this is very powerful iwe chakaka futsek 😂
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Месяц назад
Osaona kuyendesa dziko mbuzi za anthu izi
@user-cv3zw9ic6d
@user-cv3zw9ic6d Месяц назад
Athabo chakaka akalowelera bwanji za ku immigration popeza si office yawo komakuti ma guy aku immigration agenda galu mwini wagalu waoneka poti akupangira ma passport kuchipinda munya muona 2925 dpp boma wokavota ndi ife tatopa kulamulidwa ndi gule
@user-jl6sq3ph1b
@user-jl6sq3ph1b 2 месяца назад
Zangokumana zisilu zokha zokha pamenepo ka awapange abwino kmaso cnanga ndi mbamva anakatani kubelako akubelako limozi ndi mcp 😂😂😂
@BernadFlackson
@BernadFlackson 2 месяца назад
Chiwudzeni chikuwononga dalaa
@user-sw2rn3xn3g
@user-sw2rn3xn3g 2 месяца назад
Zosayenda
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n 2 месяца назад
Anaphunzira kuzunza anthu basi, asatana achabechabe awa
@mathiasmastepe2873
@mathiasmastepe2873 2 месяца назад
Chomwe akuyankhula mkuluyu sindikukuchimvetsa. Who is to blame? Thabo chakaka ndi wabwino kwambiri. Koma anthu omwe amaunikiridwa ndiwo amene Ali ndi vuto. Ask ur president kuti Kodi AG amamuza chani?
@StiveKantiki
@StiveKantiki 2 месяца назад
Osewo ndi zisilu zidude zakuba
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 2 месяца назад
Achoke
@joebrown1158
@joebrown1158 2 месяца назад
If we speak of incompetent means Razarus Chakwera is incompetent.
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 2 месяца назад
Ngati ogwira nthito zaboma ziri zitini ofoyira oyamba ndi omusankha .
@user-eh1mg3ww6d
@user-eh1mg3ww6d 2 месяца назад
Ndipo chakwela tizamukumbukila osati ku zabwino ayi koma ku zowawa zomwe chakwela wativetsela kuwawa ndipo sitidzamuiwala
@yohanedaudi1740
@yohanedaudi1740 2 месяца назад
Anthu oputsa ,Koditu ine Ngati mmalawi mukamati anthu ambiri akupoto NDI ophunzira ine ndimaletsa Koma chomwe ndimadziwa ndichoti anthuwa amangolowetsana potengera kochokera tribelisim
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 2 месяца назад
Muuzeni galu ameneyu ndi chitsilu
@wayafrank2405
@wayafrank2405 2 месяца назад
Kamwana kameneka udindoo wamukulila
@jeffchikwapata6933
@jeffchikwapata6933 Месяц назад
This guy he called himself atoney General is useless
@FaisonLukiyo
@FaisonLukiyo 2 месяца назад
Mzowonad tiyamike kulankhula kwa abwanawa.
@AckimMhango
@AckimMhango 2 месяца назад
President ndiye akufuna munthu woti atsamulangize ndicho chifukwa anachotsa Chikosa Sulungwe poti akufuna zomwezo
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 2 месяца назад
Manyaka enieni adindo opanda nzeru
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 2 месяца назад
Akulitenga ngati dzikoli ndilambuyake
@isaaczuze
@isaaczuze 2 месяца назад
Chisilu cha munthu ichi kaya ndiwakuti munthu wopepela ngati ameneyi ....akuti pamenepa akufuna kusamgalasa president
@KasimIbbu
@KasimIbbu 2 месяца назад
Ndiwesilu kwabas apage mayaz kumene puleziditi wo
@LukaAron-el5qh
@LukaAron-el5qh 2 месяца назад
Thabo chakaka ndi Attorney general wa chakwera kalpana wamcp osati wa boma lamawi
@Littlefair7
@Littlefair7 2 месяца назад
RU-vid yaphweka kumalawi.
@user-is5dl7np9g
@user-is5dl7np9g 2 месяца назад
Thabo Nyirenda ndi kape kwambiri
@AbdulrahimoMassamba
@AbdulrahimoMassamba Месяц назад
Musamuchemerere mdalayu ndiwaganyu uyu.akukoma mkamwa akufuna 1kg ya sugar uyu
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp 2 месяца назад
Komadimtu Sona🤔
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 2 месяца назад
Ndinamva kuti ndi m'bale wawo wa a Chakwera uyu
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 2 месяца назад
Wa Monica chakwera cousin wake.
@user-hl3vl9nt1b
@user-hl3vl9nt1b 2 месяца назад
Nawe iwe chembe tamata kuchimbuzi kwakoko naweso ndiwe kape paja
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 2 месяца назад
NKHASA adayimba NYIMBO YONENA KUTI TINASAKHA ORAKWIKA izi lero zikuyikira uboni nyimba imeneyi ya PHUNGU JOSEPH NKHASA NAWONSO ACHAKWERA NDI UMBULI WAWO AKUGOPITILIZA KUSAKHANSO ORAKWIKA ZOMVETSA CHISONI DZIKO LATHU
@alexsumani6823
@alexsumani6823 2 месяца назад
Kumasiyanitsa Mlangizi wa boma ndi wa banja
@Ngwangwa-ej4rs
@Ngwangwa-ej4rs Месяц назад
He is not suitable for apresident he must go back to be apastor
@PhillspicJere
@PhillspicJere 2 месяца назад
Ngakhale ku thyolo kumachoka Bingu komaso Peter koma umphawi osayamba agalu inu
@Zelinakhisswell
@Zelinakhisswell 2 месяца назад
Nanga zugwirizana bwanji ndi main nkhani yomwe ikukambidwa, mesa umphwawi wasefukira chifukwa Cha president wako ongodziwa kugwetsa ndalama ndi kuba moti azilimbikira kupanga zinthu zoti apeze forex
@MarthaMalopa-kw9xw
@MarthaMalopa-kw9xw 2 месяца назад
Zomwe zikuonongeka ndi zakuThyolo kapena dziko lonse? Tiyeni tidzuke aMalawi ndikusiya kaganizidwe kodana ndi anzathu
@garnetphiri
@garnetphiri 2 месяца назад
Im Garnet J K Phiri, im here to comment on this audio, mzika zokhumudwa they are100% right,to tell our gaverment muli mbuli zosaona zokha zokha paja amati osaona salondolelana njila munthu sungatenge masanzo ndikuwabwezelesa mmimba kachiwiri ,mukutenga munthu wa retired wosanzidwa put back in gaverment Achakwela mutual wanu umagwira bwino ntchito or you are just enforced by some .Nyirenda ,attorney,are you a real qualify loyar?or you are there like a sign post that you don't know what you are doing?Even you Chakwela and your friend Chilima you can't feel shame to how how people are struggling on passports issue? Simuchita manyazi anthu kumabwezedwa pa immigration for sake of fake passport , Chills i thought you're brilliant but you are coward plus Chakwela too
@AbdulrahimoMassamba
@AbdulrahimoMassamba Месяц назад
Musalimvane ndi Athabo, bwanji mukudusa m'mbali? Kweni kweni muli mbali iti inuyo Apule ndiwo chizete chotheratu inunso mwagudwa timawaxiwa omwe akutimenyera nkhondo tsekani chimbuzicho mukutinunkhitsa kuno
@isaaczuze
@isaaczuze 2 месяца назад
Kodi munthu ameneyi anakamutenga kuti ......kungotengana zisilu zokhazokha
@amiduclement2142
@amiduclement2142 2 месяца назад
Zikozakuteka kuti ndi wa udf
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 2 месяца назад
Chakwela ndi athabo chakwaka ndi 🐕‍🦺 kwambili
@user-sw2rn3xn3g
@user-sw2rn3xn3g 2 месяца назад
Kkkkkkkkk
@ChembeWaimba
@ChembeWaimba 2 месяца назад
Chakaka Nyirenda very interigent, iwe do you know behind this mess, do you know that Kalumo is fighting corruption at immigration hence this and yet supporting corruption, inu munakhalapo kuti attorney general??¿???
@PhillspicJere
@PhillspicJere 2 месяца назад
Sakudziwa awa zambiri Ku DPP ndizitsiru zomwe akumazipasa bundle kumangolankhula zopanda mutu agalu awa
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 2 месяца назад
Fake passport, fake president, kkkkkkk 🔥🔥🔥🔥boma lofoyila ili
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 2 месяца назад
Akuthana ndi corruption? Koma akumapanga ma passport a fake nkhani yochititsa manyaz musamuikile kumbuyo nanu😢😢😢
@user-to5of3ks3g
@user-to5of3ks3g 2 месяца назад
Fake govement passport fake
@user-hd7wq2yc6m
@user-hd7wq2yc6m 2 месяца назад
Pali zanzeru pa chakaka nyirenda apa? Iwe mbizi eti khoti laweriza bwino bwino iwe nkumanena kuti sizilibwino opanda nzeru iwe khala chete malamulo simuwaziwa Inu boma muziyendetsera unkhungu ,.kuba chitsiru iwe ndi usapota wako wauchitsiru
@user-qn2nu4xs9i
@user-qn2nu4xs9i 2 месяца назад
Angokumana okhaokha,...ubwino wakenso ma passport wo akuvutika nawo okha.....ife timangoyendatu olo opanda passport ..crossboarder😂😂😂😂😂😂
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 2 месяца назад
😂😂😂😂😂😂
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN 2 месяца назад
Chichosen pampandopo musazachiyikeso pa mpando uliose chimenecho aaa chandikwana msaname, and Which pelezideti instead of president you talking about ,not we don't have a leader in malawi,I shall show you a really president of malawi in 2025!!!!
@PhillspicJere
@PhillspicJere 2 месяца назад
Thabo chakaka Nyirenda ndi dolo koma zisiru ngati inuyo a DPP ndiamene mukumuona ngati palibe chomwe akudziwa, mwaiwala kuti munali ndi mhango lawyer wa mutharika emwe samadziwa kanthu? Mwaiwala kuti kunali Mai Jane Ansah wa DPP koma Peter anakhala chete? Ndiye nzeru zomwe mulinazo inu Ndiye ziti zotibwelesera nkhalamba kuti izalamulese? Agalu inu zisiru Ku DPP kwanuko musaone ngati akakupasani ma bundle wo a DPP Anthu Ndiye asintha kuvotera nkhalamba? Chitsiru iwe ndi ufulu otengera nkhani Ku court lina mbuzi iwe sudziwa kanthu galu
@Zelinakhisswell
@Zelinakhisswell 2 месяца назад
Anthu ukuwatchurao munthaw Yao zinthu zimayenda ngt Pali zomwe amalakwitsa kma sizinafike ngt apa pokhotesera Dala malamulo Ali clear, ufune usafune 2025 gule kwao abwelere kudambwe
@JamesLongwe-qz9fd
@JamesLongwe-qz9fd 2 месяца назад
Takhala chete naweso Malawi wavunda naweso ukuyankhula mbwerera
@user-hd7wq2yc6m
@user-hd7wq2yc6m 2 месяца назад
Ndichifukwa chake iwe ukusapota chiboma ichi uli chindere nkhani yachiziwikile iyi iweyu kuyamba kuyamkhula za DPP palizeru apa? Iwe zeru ulije kwali ndiwe wa mcp ulichindere chomene DPP ungafanizire ndi mcp, DPP inayendesa bwino boma kusiyana ndi mcp yakoyo mcp kuba,kulemba nthito pa chibale, kikondera chigawo chimoza, kulembana ntchito pa mpingo wa Assembles of God pama boma ghose agho takhala nagho since democracy 1994 this is the worst of the worst government munthu iyo wakusapota boma ili kulongola kuti mutu wake ngwakufuntha mahala walije chindere foseki
@vytwistthelion98
@vytwistthelion98 2 месяца назад
Mwana wanjoka seka pachombuzi pakopo chifukwa suziwa chomwe ukunena
@richardbanda9997
@richardbanda9997 2 месяца назад
Izizi musazitengere Ku ndale. Time zoona pano Ku Immigration kwaola. You mean you can't see. Kapena inuyo mukapita Ku Immigration, mukuthandizidwa? Tamaganizani osati chifukwa Choti mukudya nawo nde basi kumangotsutsa pomwe Pali chilungamo. SHAME MCP.
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
Ameneyu anali mulimi sakuziwa za ndale vuto akumasankhilana chibala ndichifukwa akumakanika kuyendesa dziko akumasiya anthu okhala ndi experience ya kuyendesa boma zamanyanzi Malawi
Далее
Symmetrical face⁉️🤔 #beauty
00:15
Просмотров 4 млн
LIVE: Lok Sabha Budget Session
2:32:22
Просмотров 3,9 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH MICHAEL USI (MANGANYA) Part 2
58:38
Symmetrical face⁉️🤔 #beauty
00:15
Просмотров 4 млн