Лучшее на RU-vid
Кино
Авто/Мото
Видеоклипы
Животные
Спорт
Игры
Приколы
Развлечения
Хобби
Наука
Авторизоваться
Зарегистрироваться
COMRADE NTANYIWA PA LIMPOPO FM - CHAKWERA WAKAKAMIZIDWA KUTULUKIRA POYERA NDI ABOMA LA MCP
8:13
Evance Meleka -Yashuta
5:10
Sardor Mamadaliyev ilk bora Toshkent Citydagi uyi, oilasi va “Sardori men man” haqida
2:05:03
2 дня БЕЗ АНТИФРИЗА. Что с мотором?
37:47
ПОГОНЯ ДПС ЗА ОБЕЗЬЯНОЙ в ГТА 5 РП (GTA 5 RMRP / Криминальная Москва)
00:59
Seja Gentil com os Pequenos Animais 😿
00:20
ABWANA PAULENDO - BLESSINGS CHIMANGENI
Mpungwe-Pungwe mw
Подписаться 62 тыс.
Просмотров 42 тыс.
50%
1
Видео
Поделиться
Скачать
Добавить в
Опубликовано:
11 окт 2024
Поделиться:
Ссылка:
Скачать:
Готовим ссылку...
Добавить в:
Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии :
224
@FaroukSaliem
День назад
Chikangawa ulendo, watsala chimwendo. Dzina langa ndine FAROUK SaLIEM. Kuchokela mu mzinda wa Lilongwe. Ku kasiya. Ondifuna ndilipo nditu. Thaxs
@brianjames211
День назад
Those who live their life by the sword they'll die by the sword, God has said it all
@dalitson3558
День назад
God help us we’re going through a lot tikuvutika chifukwa anthu ochepa
@kennethnasteve4721
День назад
This song reminds me BINGU once this song come out that means something big happens 😢
@MtendereChimbuto
День назад
It came out in 2007 0r 2008
@JemaxChibwanazulu
День назад
Exactly
@ellensambo6323
День назад
😢😢 nyimbo iyi mmmmm Ambuye ankhuze Malawi
@kingstonekalonga8435
День назад
Achimwendo Mulipo koma kumeneko kkkkkkkkkk azanu oipa mtima ndamenewo ikwaswndera ifa 😂😂😂😂😂
@lawremmakanyenda3390
12 часов назад
Manyazi bwanji
@kasimmussa-c5v
День назад
Ambuye please tengeni satana ameneyuu 🙏🙏🙏
@victorauwana7258
День назад
Komatu ndiye lelo ndilezela ,,, nananangati wafa mmmm ayi munthuyu wawononga ziko
@AmissKumakanga
День назад
Ineyo panopa misoz yachimwemwe irimasaya mwanga murungu atimenyera khondo❤❤❤❤
@ronaldordinga6537
День назад
@@victorauwana7258 anthu mkuyankhura ngati MLI ndi umboni oti munthu wamwalira bwanji
@wisdomsadyalunda2001
День назад
you can say that again umamwa chani ase kkkkkkkk
@benzobanda-ed8tp
День назад
@@AmissKumakanga kodi ndizoona zoti wamwalila abale
@OdetaGidypro
День назад
Zoti akudwala ndizoonad, stroke. Ndaonera sabc news koma sanakambepo zot wamwalira ayi. Ndiye zinazi tiyen timusiye Mulungu akhale Mulungu basi
@PeterNamphwanya
День назад
Tivine kaye koma otsaiwala mother's day ikubwela🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤
@SamuelMtambo-p1z
День назад
Straight
@BannetMwale
День назад
I
@MoosaSidrick
День назад
Komabe apete watikwana athu Akufa ndi njala usiku onseu ndimangopephe kuti apite ndithu tikapeza komweko achilima Ali paseu akukudila abwana
@RuthTimothyChirwa
День назад
I like this song keep it up my brother ❤❤
@EphraimNyirenda-e3s
День назад
Nyimbo iyiiiiii ikangolila ndkt China Chake chachitika😭😭😭
@BlessingsCperumal
День назад
Are u seriuos
@GraceMakawa-b8e
День назад
Ndipo zoona
@AlexKaunda-ny2eg
День назад
Ambuye please chakwera mtengeni akuchinda akazi ayeni
@vanessachimbayo1247
День назад
Zoonadi mpaka pamenepo
@BlessingsTembenu
День назад
Kkkkkk koma ndaseka,ameneyu atsogole basi
@HawaMamo-q2v
День назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂koma abale
@EstherMaonga
День назад
Ine ndimafuna asafe nsanga azamangidwe kaye ndikuyankhanso milandu
@HestingsChibalo
День назад
Ndipo inu aaaa😂😂
@MarkManyowa
День назад
Akamwalira nanga ndalama asiila ndani🤦 Zimangoona kuvuta koma kuzikonda kuja nkosapindulitsa
@festongreston
День назад
Let the will of God fulfill
@IdressaMussa
День назад
Chakwera 💔💔💔💔💔 ayende bwino 🎉🎉🎉🎉🎉anali oyipa ngat 🎉🎉🎉kambuku 🎉🎉🎉🎉🎉🎉 nyimbo 🎉🎉🎉🎉🎉ya chakwera 🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@TamaraSeleman-cl2fc
17 часов назад
boma ilooo ife sitikusintha boma nkhalamba ikagwere ukoo chakwera oweeer
@MiddayDeleza
День назад
Apule mungamuphe mzanu atagwira colona zoona? Colona ndi woopsa lero ndi zimenezi dzakutsatilani, ngati zikumbvekazi zili zowona
@RaheemNgoma-pk1ev
День назад
Kamajete next
@mariamahamadu8402
День назад
Nde Mene dzatelemu Dani Lu mukuti bwanji apatu nde ndalama dzija simudya kujijilika umakagwa matope mubwelelaso kwa Dade kapena Mwangi Taya thawi pachabe 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@pemphokatembe443
День назад
😂😂😂😂😂😂😂
@rashidadan2533
День назад
What goes around comes around
@paulmanyamba5437
День назад
Iyi ndiye tiyivinadi 😂😂😂😂
@AugustineChimaliro-e5i
День назад
Achimwendo mwazukako bwanji nthupi
@VeronicaChirwa-ct4os
День назад
@@AugustineChimaliro-e5i kkkkk
@AngolanChinga
День назад
Kkkkkkk km guys
@RemitterFlik1130
День назад
Paja amalondola misonkhano yanzawo tiyenitu ku chinamwali kuzomba kuli msokhano lero 😂😂😂😂
@fannyzimba149
День назад
😂😂😂😂😂kamaliremba kkk ndi mzake Jezebel kkk
@TiwalumbeNathan
День назад
Let GOD BE GOD
@thomluciouss7360
День назад
Oyenda ndilupanga azafatso ndilupanga,palibe wamuyaya pa dziko ask kamuzu Banda
@HassanSaid-q8q
День назад
Yaaa pano ukuona bwanji kumene uliko..mulungu siosewela naye
@AdamuKasimu-x5o
День назад
Kukhuyu mukumva bwanji tupimo😂😂😂😂😂😂
@omarajibu860
День назад
Very educative song
@ThomsonChipwele
День назад
Akafa tisangalala
@zelliachamboto5744
День назад
😂😂😂
@RemitterFlik1130
День назад
Tizika janza nyimbo yomweyo pa bingu stadium
@ChristophrMaiko
День назад
Nditangomva izi inenso ndimaiganizila nyimbo yomweyo eeee koma tivine kaye mowa uli pambalipa
@JosephHill-fy1bb
День назад
Commission of enquiry ija anakoza
@KettieNathaya
День назад
Chikangawa hoyeeeeeeeèe ukawapatse mon anthu 9 aja
@LameckNgwangwa
День назад
The more u plant the more u harvest
@JemaxChibwanazulu
День назад
Mau akulu akoma akagonera.
@jennyx6914
День назад
kulsmkhula mwachikulu good msg like it ndipo ndskumva though ndine mtinga based in joburg
@rodgerstembo7866
20 часов назад
Amen what you plant is what you harvest
@VeronicaKelias
День назад
Mulungu salakwitsa watilanditsa ku mimbulu imenei ngat ndi zoona ai zakhala bwino akanatitha tose koma ambuye atilanditsa
@DanfordMkalimbaBanda
19 часов назад
Kuthawa ntchito yamulungu, koma imfa siithawika
@EmmanuelNtago
День назад
Am enjoying reading comments than listening to this music
@nuhiabwanali-jo5eq
День назад
That's true bro
@WisdomChimalizeni
День назад
Nyimbo ilibwino iyi🇲🇼 oyimba analosera kale
@JeanKambala-gm1zr
День назад
Wafa imfa yabwino ameneyo yosadulidwa miyendo muyende bwino ,,imfa yosavulidwa jekete ayi zikomo mngwilizano unja Kuno
@MemoryChaima
День назад
Ngati zili zoona ambuye kumwambako mwamva mapempelo akatolika tonse tipange mpwando anatimpela munthu wosalakwa mfiti imenei
@BonfaceMpokosa
День назад
Ndikhale mbuli ine chete
@user-nt5yn2im6t
День назад
Thanks Lord
@ElizabethMajiga
День назад
Mulungu amava ndithu
@MustapherLino
День назад
Get well soon mr chakwera,we still need u
@AliceGeorge-il6ig
День назад
Oooh,Ambuye atiyankha bas,,Linali pembedzero langa la kolona
@trickermussa472
День назад
Or angoika komko plz
@PaulNyirenda-d7k
День назад
There is no guarantee in this earth
@LonjezoChitseko-lx4qb
День назад
Akafa ntendere ufika mmalawi
@RoyTrading-b4x
День назад
Blessings Chimangeni on repeat 🎉🎉
@AllenBanda
День назад
Only God knows
@mariamahamadu8402
День назад
Mmmmm chikangawa mudzimu yawanthu 9 ija ikukudikila
@nuhiabwanali-jo5eq
День назад
Koma di azi pita, akayankhe zomwe ama phela anthu pa dziko la pansi osalakwa.
@ThomasChiwaya-qx9mf
День назад
Ndikufuna Charly patache choipa chisata mwini
@Mpungwe123
День назад
Iponyedwa imeneyo bwana khalanibe pompa zitheka ndithu
@issahmaloto9141
День назад
Ndichita choyenda maliseche lamulungu lino
@VeronicaChirwa-ct4os
День назад
Mpaka kuyenda maliseche😂😂😂😂😂
@samchibenene4458
День назад
😂,,,
@SolomonNjolomole
День назад
Ukayamba ndi zomwezo umamaliziranso zomwezo,kuyamba ndege kuikwera eeeee mkutsazikana nayonso.
@KassimWilson-g6m
День назад
Abwana paulendo akajele kumwamba ndrama zakubazo 😂😂😂😂
@meganabigail-ye7fw
День назад
Nyimboy simatuluka wamba ikatuluka choncho kumakhala kuti wina Akuonana maso ndi maso ndi anthu omwe anasogoza.
@patricksamson4852
День назад
Tidikire ntanyiwa
@FlorenceDouglas-x5c
День назад
Koma ma comments ali apa mmmmm 😂😂, ine lelo ndiumwa mowa size kukana pati !!!! 😂😂
@JosephIsaac-s1c
День назад
Best song ever, once I hear this song I feel cry
@EsetaGerate
День назад
😂😂😂😂😂 komatu mukhalike Kodi chikangawayo wafa kapena chani 😂😂
@lyiemanganjira9708
День назад
Ineyo sindufuna afe,, koma akhale ndi moyo kuti adzazione ndi maso
@EsnartGirivin
День назад
Rip chakwelq
@Richardbanda-hg6pt
День назад
Let's pray for Malawi something happen
@MarthaMbewe-uk5nn
День назад
NDILI KU MSIKA NDIKUDIKILIRA CHI GALIMOTO CHA NKHUKU😂😂
@LameckLubanimbewe
День назад
Palibe wa muyaya
@LinlyMatheweKufakwina
День назад
😂😂😂😂aaaaaa komatu Malawi muli ndi chipongqe iiiii
@KhadijaMsosa-d7z
День назад
Amalawi sititha kucheza😂
@NancyLennoh
День назад
Kmanso tili pa changu kwambiri 😹🙌🙌🙌
@AbdulrazaqHussain
День назад
Let's wait for news, no speculation, here,l love mpungwe pungwe coz only the truth comes out on this platform, so let's wait 4the updates
@CassimMbalaka
День назад
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pomuyika aliyese ukhudzidwa pa ifa ya chilima
@ChristophrMaiko
День назад
Ngati zili telo mulungu asakamulandile ai galu ameneyo watizunza kwambili
@EyobeAyala
День назад
Koma guys zoonad izi kapena ndikulota tandizuseni ine
@JrAlfeoLungu
День назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 ndipo isaphonye ikulondola ndiku garden city
@nuhiabwanali-jo5eq
День назад
But guys tell us what's going on,, '" its. true story that president Chakwera died?"
@JuniorHala-vf9ov
День назад
Osamasewela ndangoni amene anapanga nao program yokupha chilima paulendo bwezela agwile ntchito yake apa
@MonijaKataika
День назад
🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔🤔 😭😭😭😭😭😭😭😭😭 🤐🤐🤐🤐🤐🤐🤐🤐🤐 Whatever it is God save Malawi..
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
День назад
Ndi wamwayi amene amabwelako ndi moyo ku Galden city koma Mulungu akukhuzeni nonse omwe muli kuchipatalachi imfa siyabwino ngati kuli moyo.Moyo kunyenga nthawi yolapa inalipo koma chuma chimanyenga
@MarkManyowa
День назад
😂😂😂😂😂
@MarkManyowa
День назад
Imfa yanji yokondweretsa 🤣😂🤣🤣 Koma ngati sizitheka panopa His days are numbered for sure 😂
@Alice-z7t4z
День назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂@@MarkManyowa
@ElizabethMulinde
День назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂@@MarkManyowa
@MarkManyowa
День назад
@@ElizabethMulinde 🤣🤣🤣🤣 Akanangopenga Misala onse omwe anatenga nawo mbali pa plan yozimitsa Chilima ndi ena onse aja
@adsonphiri6497
День назад
Guys kodi zikuti bwanji tiuzeni bwino
@MariaNyamwera
День назад
Kkkkk kkk koma kumeneko chete ku ma stand
@JosterNgalawa
День назад
Apaso chimwendo wasala ndi days yokha ulosi wanga watelo the 4th is kamajekete
@CameronVisser-k7i
День назад
Pangani search manganya ma bodigadi ake kunyumba kwakwe kuli bwanji apo ndiye tidziwa chiona
@DavidPhiri-o6w
День назад
Honest this ikayikidwa something happens
@doreenkaliati3166
День назад
Okumpha nzake samwalira😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@samdiverson9733
День назад
Koma ma trillion a malawi apitatu😢😢😢
@EnerstManess
День назад
🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉Fire 🔥 🔥 🔥 🔥
@DeborahChikumbu-c2v
День назад
Lero masanawa ndakumana ndi conivy ikuthamangira mulungu airport kaya sakukawatenga a bwana vp kaya.
@ShamimuBisani
День назад
Guys maliro Achakwera alephereka ali moyo wapita ku Israel panop nkhondo ija yavuta anaivotera ija wapita koleresa ndthu usiku Lebanon yaphulisa Israel anthu awiri afa ndye Chakwerayo alikumeneko ndthu
@ShakiraJackson-x8w
День назад
Ndikukagura sound music basi
@yassinn5634
3 часа назад
Anyamatawa ali boo chifukwa sanabise kuti iwo kuimba ndi business. Ndiye amene sakutha kuwamvetsa apite ku RUO azikagwira nkhanu
@AubreyNdeule
День назад
Kkkk mwatibwanj ku chikangawa?
@MuhammadPyson
День назад
Ammbuye tengen chikangawa
@MosesTangwe
День назад
Kanyimbo aka anakomza
@ChristopherMaulidi-m3v
День назад
Good
@LawrenceBamusi
День назад
Ndee ena akuti Usi akungotola ma 3 points awulere😂😂😂😂
@Kabwilachikangawa
День назад
NDILI KWA TELALA KUSOKESA BLACK CHEERS❤❤❤❤❤
@GeoffreyBAyatuKazembe-q7u
День назад
😂😂😂😂😂😂
@MaryNyirenda-nq3mh
День назад
😂😂😂😂😂😂
@zelliachamboto5744
День назад
😅😅😅
@WisdomChimalizeni
День назад
A St chikangawa mphakati akaphikira kuti kumene kukuoneka kuti kungakadyeke bhoo😂😂
@Kabwilachikangawa
День назад
Osayiwala kulongeza tsabola wa kambuzi okadyera nyama ku siwa ku kasiyaa hehehehehehe
@TonykalicheloKalichelo
День назад
Chonde tithandezen mwachangu abale tiyambepo kulezela plz
@GoldenHappy-gt6ld
День назад
Ngati zili zoonadi Malawi wapulumuka
@AliceGeorge-il6ig
День назад
Osasewela ndi kolona wa mkatolika
@WellingtonChipembere-l1i
День назад
No comment🙅🙅🙅
@JosephIsaac-s1c
День назад
What is going on here??????
@JOHNSANGWALI-n2f
День назад
What is going on guys
Далее
8:13
COMRADE NTANYIWA PA LIMPOPO FM - CHAKWERA WAKAKAMIZIDWA KUTULUKIRA POYERA NDI ABOMA LA MCP
Просмотров 35 тыс.
5:10
Evance Meleka -Yashuta
Просмотров 38 тыс.
2:05:03
Sardor Mamadaliyev ilk bora Toshkent Citydagi uyi, oilasi va “Sardori men man” haqida
Просмотров 96 тыс.
37:47
2 дня БЕЗ АНТИФРИЗА. Что с мотором?
Просмотров 119 тыс.
00:59
ПОГОНЯ ДПС ЗА ОБЕЗЬЯНОЙ в ГТА 5 РП (GTA 5 RMRP / Криминальная Москва)
Просмотров 165 тыс.
00:20
Seja Gentil com os Pequenos Animais 😿
Просмотров 5 млн
10:02
PROPHECY! DPP this 5th party in your "Alliance" shouldn't be in it| Prophet Emmanuel Zomba Malawi
Просмотров 48 тыс.
12:31
Zeni Zeni zake Zokhuza Chakwera
Просмотров 118 тыс.
5:10
Evance Meleka _Yashuta
Просмотров 7 тыс.
36:46
NKHANGA ZAONA KOMANDA KWA SING’ANGA MZIMU WA BHIYENI WAVUTA NDE KULIBE TUROTU ABWANA
Просмотров 64 тыс.
14:16
BRIAN BANDA KUWERENGA NKHANI ZA LERO PA 09 OCTOBER KUFOTOKOZA CHENICHENI CHIMENE CHACHITIKA LERO
Просмотров 192 тыс.
11:55
Chifukwa Chimene Anthu Amamudera Miracle Chinga
Просмотров 96 тыс.
23:12
THE BEST OF MALAWI COMEDY | MLELEMBA WAGWA MCHIKONDI NDI A ZAKHALI | CHIKONDI SICHIONA MSINKHU
Просмотров 13 тыс.
2:21
Chikuchitika ndichani Amalawi 🤔
Просмотров 60 тыс.
12:24
COMRADE NTANYIWA - SATURDAY MR PRESIDENT AKUKASEWERA MASEWERO A GOLF
Просмотров 27 тыс.
6:03
EVANCE MELEKA _CHITA MWANZERU, MISTAKE NDIKAMODZI, KAWIRI NDI ZADALA
Просмотров 20 тыс.
2:05:03
Sardor Mamadaliyev ilk bora Toshkent Citydagi uyi, oilasi va “Sardori men man” haqida
Просмотров 96 тыс.