Machende anu nonse aku Immigration,kunzunza amalawi basi,akafunsidwe kaye mafunso ndi Mr Brian Banda osati mafunso mukufusana apa apachibale chifukwa nonse ndinu a M.C.P
Akuluwanso nawo kulankhula za mbwelera..palibe zachilendo apa, pokhapo pokachitira printing ku Lilongwe means no improvement in service delivery..kukhala backlog 10 days sizingatheke..
Ine ndimaganiza kuti ma passport ayamba ku printer ku blantyre koma zimene akunena Abambo awa sizikuveka kwa munthu wazeru akuti ma president kuchokera blantyre angolembesa koma print ndi ku lilongwe . Sitikufuna zimenezo ma passport azipangika ku blantyre komweko
Kodi Amalawi amveziti akapita kuka wombora Passport yawo akumawauza kuti apereke ndamala zina kodi chilungamo chake ndi chiti K50,000.00 but people they are playing more than that advice your worrks not to do COLLAPUTION when people goes to collect their Passport PLEASE We Malawians were tired. STOP IT,STOP IT.
Nanga ndi chifukwa chani inu ngati a immigration munthu kuti atenge passport koma apereke ndarama zoposa mtengo WA passport,, mwachuluka kuba nonse kumeneko muchoke basi sitikufunani mwationjeza
Ma boza okha okay, munayambapo mutatulusa passport munthu atapereka 90 thousand before ,after kupereka 90 pin ,mumademandanso 100 something mumunthu Osaka agalu inu,mulungu akulangeni , in our own country like passport amalawi muziweni mulungu ,coz passport it very important thing for residents mukut r50 pin 2 weeks wm ,maboza munthu akapita ku migration yenkha kopanda ma agents and anthu aku migration simumamuthandiza anthunu ummm only for passport please we ate all Malawian we have right to have passport please have mercy to us we don't have money to bride you guys,