Vuto si a police ayi, vuto ndi malamulo a dziko lathu. Zikanakhala kuti kuli malamulo kwathu kuno, kuyambira galu akumuti bwanayo ndi a police onse anapanga zimenezo bwezi pano atamangidwa onse.
Let lawyer's fight for this man's justice, the foreigner and police men need to answer to the LAW. This is not acceptable, #Chakwera do something urgently. Owners of the land are suffering at the cruelty of foreigner's
Muthune ndikumalota ndili ku school pafupifupi tsiku lilonse Koma school ndinasiya 2019 nditalemba mayeso a4 anthu amati za school ndimadziganizira kwambiri komano sidziri choncho ndani Muthu angandimasulire maloto amenewa.
It's bad that these kind of things are too much in Malawi since it's not new issue. Ambli akulavulazidwa kwambli nd apolis I think many they are not knowing their role
This is a very bad situation and their Asian bossis using the abuse of his power and it's a felony charges against this poor innocent man May the Lord heal him and have mercy on his soul.
a mabungwe please lowelelanipo po thandiza felix kut mwenye ameneyu amuliupile ndithu ndipo ndalamazisakhale zochepa chifukwa uku ndye ndikuphana komaso a police wo alanbdiole zilango