Ndipo a DPP asasiye ku gwiritsa ntchito imfa ya Chilima ngati nyambo yowakolera a MCP. Ndenge inagwera pa ground la mpira iwowo kumapita kuthengo daladala zazi. Pamene panagwera panafera CHILIMA ndipoti titha kusewelerapo mpira wamiyendo si kuthengo ayi ife tili ku mpoto kokuno tinawonapo
Anthu ambiri aDPP ndi aku Ntchewu akupusitsidwa ndi ndizomwe akupanga zokhudza imfa ya a Chilima . Imfa imeyi aDPP akupangira campaign ndipo ndi zachisoni kuti DPP ndiyomwe imasangala kwambiri pa imfa ya aChilima anthu ambiri sakudziwa kuti imfa ya Vice president idzaiwalika chisankho chikangodutsa. DPP ndi imene inali mdani weni weni wa Chilima zonse akupanga a DPP zi ndi MISONZI YANG'ONA YOMATI UKU IKUDYA UKU MISONZI IKUTULUKA. WANZERU AMVE MAU ANGAWA OPANDA AKHALE.
Ndipo usakayike kambani bwino report silikumveka ngati report ya school yakwacha kampeni ndimeneyi kumene onse otsutsa wo ine simpanga nawo zandale km imfayi inandiwawa koopsa
Pamaso pa mulungu moyo uli onse ndi ofana ma udindo ndi apadziko lapansi pompano ngatidi sulemani ali wa chisoni ndi imfa bwanji sanapitenso paja anthu 26 anapsera mini bus or mchipinda momwe Bingu anafera mwadzidzi? Akudziwa kuti izizi it's not trending. Ndipo musamatchule kuti Sheikh . Sheikh ndi title yakuti amapitira ku mapaphunziro achipembedzo.