Bushiri amathandiza ndizolinga za kumidima. Chifukwa Bushiri zake zonse zimene akuchita ku Malawi ndi zakumidima ndichifukwa chake anathawa ku South Africa ndi mbava ogwilira
Chikhomeni ali nfundo ndimayesa nkhani ya chamba imene avomeleza aphungu week yathayi anabweletsa ndi Las Chikhomeni masiku ambuyomo. Which means this guy he is a clever guy and i support him Chikhomeni