Тёмный

Anthu omwe ali ndi kuthekera kozawina u President Chaka cha mawa 

Andrew Pilliot
Подписаться 27 тыс.
Просмотров 66 тыс.
50% 1

#malawi #trending #politics

Опубликовано:

 

30 мар 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 353   
@mayesojameskatete
@mayesojameskatete 4 месяца назад
Kungowina chakwera I'm going to extend my stay in South Africa because there's nothing I see in chakwera's leadership
@user-yx6oo2pc3r
@user-yx6oo2pc3r 4 месяца назад
Bushiri amathandiza ndizolinga za kumidima. Chifukwa Bushiri zake zonse zimene akuchita ku Malawi ndi zakumidima ndichifukwa chake anathawa ku South Africa ndi mbava ogwilira
@user-ln3zx6wo4w
@user-ln3zx6wo4w 4 месяца назад
Or atapanga kampeni munthu amenewamvakuwawa zakatadusazi sangavotele chakwera
@user-rl5zq1qr4d
@user-rl5zq1qr4d 4 месяца назад
Am sure unafulumira kubwera poyera usanagakhonzeke ukayambirenso sizikumveka bushiri si wandale chikoneni ñdi osaziwika ukumudziwa ndi iweyo ndiponso iweyo ukungochula onse andale kusonyeza siukudziwa chimene ukukamba mwina unapengapo some time back wangonditayisa nthawi kumangobwaza basi😅😅😅😅😅
@JamesLinno-ec1zq
@JamesLinno-ec1zq 4 месяца назад
Komaso akulu inu munasowa zolankhula et?
@user-xn9ov2fn4i
@user-xn9ov2fn4i 4 месяца назад
Akulu inu kuganiza kwakuvutani mwanyika koopsa Anga umadya chachikulu kumaona Momwe dziko anthu zokhumba zawo
@paulmanyamba5437
@paulmanyamba5437 4 месяца назад
Mwasowa chokamba inu aaa komatu musamale ndindalama mukulandilazo plz amalawi siopusa
@Evancemdoka
@Evancemdoka 4 месяца назад
Gwape wachabe chabe ndimangot uyankhula zamzeru watumidwa eti
@ronaldflitwick3383
@ronaldflitwick3383 4 месяца назад
Iweyo mavita ulindi khunyu ukudwala
@honourablemcgregorysc97tv
@honourablemcgregorysc97tv 4 месяца назад
Bushiri akulephera kuyima coz ali mbali imodzi ndi Chakwera so come 2025 if akufuna kulowa ndale he will be a running mate of Dr Lazarus Chakwera
@YunusVima-ce8yk
@YunusVima-ce8yk 4 месяца назад
Sukuziwa chomwe ukuyankhula iwe mbuz.
@user-yt8qn1uv3d
@user-yt8qn1uv3d 4 месяца назад
Man mukasowa zochita muzipita ku chimbuzi kokanya kusiyana ndizoopusazi mukunenadzi mwanvaa
@GEORGE-yr7nx
@GEORGE-yr7nx 4 месяца назад
Pachakwela yekha ndiye wapala ayise komaso nakhumwa wapala uchosepo awiliwo ndipo uyikepo atupele muluzi
@user-pf6qw3pv9s
@user-pf6qw3pv9s 4 месяца назад
Ndawi zina umayakhura bwino koma iweyoso ndichisiru
@ronaldflitwick3383
@ronaldflitwick3383 4 месяца назад
Chakwera kuwina ndekut wabela mavoti
@user-yx6oo2pc3r
@user-yx6oo2pc3r 4 месяца назад
Chikhomeni ali nfundo ndimayesa nkhani ya chamba imene avomeleza aphungu week yathayi anabweletsa ndi Las Chikhomeni masiku ambuyomo. Which means this guy he is a clever guy and i support him Chikhomeni
@user-hr2cg3ku1l
@user-hr2cg3ku1l 4 месяца назад
Amalankhula zaziiii ameneyu
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 4 месяца назад
Abambo inu ndiopoira bwanji mmmmmmmm😂😂😂
@LenardKayisi
@LenardKayisi 4 месяца назад
Ameneyu mutuwake sugwila
@DanielXzelera-op6tx
@DanielXzelera-op6tx 4 месяца назад
Are u in malawi or not
@user-ee6be5kl5o
@user-ee6be5kl5o 4 месяца назад
Musamukakamize bushiri musiyeni achite ntchito ya mulungu osati ndale musapusitse amalawi kawiri palibe kukhulupilila chilimanso atinamiza kwambiri
@giftchale672
@giftchale672 4 месяца назад
Ngati kuli channel yachimidzi ndiye ndi iyiyi guys let's un follow this galu
@suwednyenje3557
@suwednyenje3557 Месяц назад
Ayi ndithu dzikomo mene atikwanila achakwera inu galu ndithu ziko loyendetsa athu atsataniki sititsapetsaso thendele paka kale ohh😢😢
@user-bu7ut2gb7o
@user-bu7ut2gb7o 4 месяца назад
Bwana Sam Nankhomwa yekhayo mchotsenipo, Malawi adapenya lelo and Nankhomwa wathandizila mavutu ndziko muno. Timakunyadilani
@user-dk6yc8pl2m
@user-dk6yc8pl2m 4 месяца назад
Koma iwe ukuyakhula we ndkape kwambili mbuz yamunthu wangobwelesa no sense
@mzeewandembonyirongo2972
@mzeewandembonyirongo2972 4 месяца назад
Aliyense angayimire alindi mwayi owina. They risk of being chosen...and the probability effects. Thats how they work. So their is no analysis here...
@JerryChain-cz8ru
@JerryChain-cz8ru 4 месяца назад
Iweyo nde waboza basi
@user-yd3zw7ye5u
@user-yd3zw7ye5u 4 месяца назад
Wanyopola ndlama iwe galu iwe sumatha kulankhula nyapapi iwe
@user-nc2yo7rt7z
@user-nc2yo7rt7z 4 месяца назад
Ànalysis yanu ndiyabodza, chisankho sawina anthu Ambiri, amawina ndi modzi, ndiye mutitchulire Munthu mmodziyo ngati mukumudziwa.
@user-nm7pv4bs2y
@user-nm7pv4bs2y 3 месяца назад
Ma program ako amandinyasa ase
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 4 месяца назад
Kkk koma ngati wadya chamba ngati supenga ndi mwayi ndithu
@user-in8of6mu1f
@user-in8of6mu1f 4 месяца назад
Iwe ndi galu kwabasi
@ElizaMalaya-nv6gl
@ElizaMalaya-nv6gl 4 месяца назад
Chakwera Ngati angazawine ndiye Kuti wa Bela Koma kwa chilungamo sangawine
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 4 месяца назад
Ndiwe nkhumba
@LovelyBlini-cu3iu
@LovelyBlini-cu3iu 4 месяца назад
Zaziii ndiwe wa MCP number 1 ndi Peter basi enawa ndi manyaka
@RobertLuka-wy9cl
@RobertLuka-wy9cl 4 месяца назад
Manyi ako mbolo yosadulayo
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs 4 месяца назад
Ndaona ulindimisala
@juniortsegula3847
@juniortsegula3847 4 месяца назад
Mboliyako kape u don't know what u say
@user-nj3gn5xq2s
@user-nj3gn5xq2s 4 месяца назад
Zamanyi
@KasuMustafa
@KasuMustafa 4 месяца назад
Ndewamaliza onse mesa nde opanda kuthekela ndiyati popeza makandidet onse chitsilu iwe
@user-cs4ud8wd5f
@user-cs4ud8wd5f 4 месяца назад
Takukhululukirani akulu
@user-dp6tz3pn1b
@user-dp6tz3pn1b 4 месяца назад
Kkkkkk iwe akupasa chani mbava yakoyo ichotsepo imozdiyo
@user-ky4we4nu2v
@user-ky4we4nu2v 4 месяца назад
Mbuzi yamunthu
@user-pl8kw3dc9d
@user-pl8kw3dc9d 4 месяца назад
Tanenani zaurosi mbuzi iwe
@user-jd9yz5hp7y
@user-jd9yz5hp7y 4 месяца назад
Chilima sakulolendwa kuyimanso pa chisakho, Watikwana Chilima akapume wakhalapo matemu awiri it's enough now Kuphatikizapo Chakwera sakufunikanso pamalawi adzikapanga zawubusa zake adzipita
@user-wr4rb1pt4c
@user-wr4rb1pt4c 4 месяца назад
Ndiwe mbuzi ya munthu
@user-rv8gi4ro6r
@user-rv8gi4ro6r 4 месяца назад
Kodi anthuwo sakuziwa kuti bushiri akuziwana ndi chakwela ndiye pamene akuthandiza anthu akuthandizira chakwelayo.ndiyeno muziziyamba dala
@user-ud9wl8yg1t
@user-ud9wl8yg1t 4 месяца назад
Wadya chamba chowawa kwambiri uzawuza makolo ako
@lymonmanda-cd8ol
@lymonmanda-cd8ol 4 месяца назад
Wakhuta nyawu iwe
@daltonkapalamula7931
@daltonkapalamula7931 4 месяца назад
Aaaaa iwe ndi galu eti
@SandramuMakina
@SandramuMakina 4 месяца назад
Utiuzenso olephela chifukwa wanena ozawina chisankho cha 2025😂😂😂😂😂😂😂
@osmanwanja3733
@osmanwanja3733 4 месяца назад
Boza
@aaronbagatelle4529
@aaronbagatelle4529 4 месяца назад
Zopanda umboni izoo
@ChikondiChauluka
@ChikondiChauluka 4 месяца назад
Peter is our grand father so how
@Alomwe
@Alomwe 4 месяца назад
Chikomeni n Nankhumwa n Joice Banda mmmm no way
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 4 месяца назад
Las Chikomeni yemweyooooo! Nfundo zake ndizolondola, chamba ndi gold. Yili mu manfeto yake.
@user-jb5yb9wq3y
@user-jb5yb9wq3y 4 месяца назад
Chilima sangaime muzifunse Justin Malewezi... Nthawi yake yatha
@amonprincegenamu7203
@amonprincegenamu7203 4 месяца назад
😂Matumbo panu akulu inuyo ukuyenera mupite mu Ndyangu comedy 😅😅😅
@chisomochavula
@chisomochavula 4 месяца назад
Kodi amene amakupatsa ndalamayo amati uzitani pomalankhula zopanda mutuzi ndakulankhulanso kokuvuta unayamba yolakwika simbaliyako yolankhulalankhula odontha iwe ukawauze akazi Ako azilankhula angalankhule zanzelu p Palibe owina pamenepo wandithela bandoll😔😔😔
@mclorydamiano
@mclorydamiano 4 месяца назад
Chamba eti akutuma eti
@user-rk5ye2tv9z
@user-rk5ye2tv9z 4 месяца назад
Iweyo ndichipwisi chamunthu ndithu or kaye kunya mau
@felixjoseph8161
@felixjoseph8161 2 месяца назад
Chakwera sangawine boss Malawi anapenya pano man si Malawi wakale
@carenchikwe268
@carenchikwe268 4 месяца назад
Malume zisiyeni basi palibe zikuveka
@edenbelievemseteka5197
@edenbelievemseteka5197 4 месяца назад
Nde aliyese ali ndi mwayi kuthandauza kuti chan? Chamba eti
@IsaacChimbalanga
@IsaacChimbalanga 4 месяца назад
Pa chilimapo mwatinamiza man Chilimo tikalowa mmalamulo adzikolino sali ololedwaso kuima us president or vice coz ma term ake 2terms anakwana
@MuhammadSamson-yz1kl
@MuhammadSamson-yz1kl 4 месяца назад
Muziyamba mwamina Kaye forsake iwe galu machende ako
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 4 месяца назад
What does you smoke mate????
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o 4 месяца назад
Kodi ukamayankhula umakhala wadya nandolo nde umakhala ukulota?? Zaziii kagwere
@user-hy6gc6ld9w
@user-hy6gc6ld9w 4 месяца назад
Iwe choka mbuzi iwe palibe chomwe ukunena chomveka
@user-jb5yb9wq3y
@user-jb5yb9wq3y 4 месяца назад
Ngati analuza Kamuzu ndi JB, nde Chakwera nkandani?
@user-on5qq9tg1y
@user-on5qq9tg1y 4 месяца назад
Ndaononga data yanganso apa eisheee, maphwala ako galu iwe
@user-oq5rg5mz7q
@user-oq5rg5mz7q 4 месяца назад
Zobowa zikuyakhulidwa apa 😮
@johnman4619
@johnman4619 4 месяца назад
Iwe chimfini usatithere nthawi .Kodi mulibe zochita musadzadzitse mabodza mukusokoneza media anthu akudziwaokha zochita osatikwapusisa zaziii
@user-zs7pn3tv1j
@user-zs7pn3tv1j 3 месяца назад
Mu nkhani zanuzi mulibe za nzeru. Onsewa anayi oyambawa sizingatheke. Bola mwanena za Peter . Enawa ayi
@user-ee6be5kl5o
@user-ee6be5kl5o 4 месяца назад
Wachamba angàlamulire dziko monga ukunenelamo osamaseweretsa upulezidenti
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 4 месяца назад
Awa zokamba zawo sizimaveka ndikuona ngati mutu wake sukoka
@user-rv7tk8cv2q
@user-rv7tk8cv2q 4 месяца назад
Akulu inu nkhani zanu zimakhala zofoyiraso bwanji
@edenbelievemseteka5197
@edenbelievemseteka5197 4 месяца назад
Maviti anji aliyese ali ndi mwayi wowina za ziiiii
@FrancisStima-sc7zs
@FrancisStima-sc7zs 4 месяца назад
Iwe kuteleko amakutuma achakwela et Kani ndimakusata ulimbuzi yamuthu
@mannietwea
@mannietwea 3 месяца назад
DPP under Peter Mutharika ndamene angawine osati manyaka awawa
@user-dk4he8zr7m
@user-dk4he8zr7m 4 месяца назад
Nfiwe chitsiru kwambiri ok?
@user-wh2my2ey3l
@user-wh2my2ey3l 4 месяца назад
Uzikhala ndi manyazi popanga zinthu anthutu ndiokwiya
@mayilosmonongwa
@mayilosmonongwa 4 месяца назад
Kumeto kuchipatala yasala bedi yimozi wokagonepo iwe Malo asanathe
@user-gw4dt9hq9l
@user-gw4dt9hq9l 4 месяца назад
Wandithela bundle yanga Kaya watumidwa
@user-zz4pn8wn3n
@user-zz4pn8wn3n 3 месяца назад
Okay
@HopesonMkomaula
@HopesonMkomaula 4 месяца назад
Chakwera ine voti yanga sangaipeze
@user-hp4rl8cv3h
@user-hp4rl8cv3h 4 месяца назад
Peter 🔥🔥 ndiwala osati wana sanapezekepo zopoyila ezi
@usumanidaudi
@usumanidaudi 4 месяца назад
Kd inu mumadya chamba yeti pano musamabweresi nkhani zopusa pano
@SulaimanaIssah
@SulaimanaIssah 4 месяца назад
Iwe ndi chisilu di eeee
@md.ruhul-aminmd.ruhul-amin298
@md.ruhul-aminmd.ruhul-amin298 4 месяца назад
Kodi galu ameneyu akuganiza bwanji tamangopitani ku dimba mudzikalima zoputsa eti
@user-wb3us4pg4b
@user-wb3us4pg4b 4 месяца назад
Ukumpemph ndan garu
@KhumboSimukonda-li6pe
@KhumboSimukonda-li6pe 4 месяца назад
Peter muthalika emwey
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i 3 месяца назад
Zabodza izo chikomen ndi Chilima ife ai ndineso prophet Dr Uncle D Zitande. Ine yemwe angatenge boma ndi Peter basi.
@mannietwea
@mannietwea 3 месяца назад
I support you
@rashidlamos3403
@rashidlamos3403 4 месяца назад
Ukutanthauza chani angawine bwanji onsewo 2025 kkkkkkkkkk
@user-nx9tj5ho2c
@user-nx9tj5ho2c 4 месяца назад
Iweyo nd zero 😂😂😂😂😂😂😂
@giftchale672
@giftchale672 4 месяца назад
Kuyambira lero ndikukupanga Un follow ndakuona kuti ndiwe opusa kwambiri you need to be educated
@usumanidaudi
@usumanidaudi 4 месяца назад
Iweyo kuyambira rero sindizayang'anaso ma video ako ndiwe wopoyira
@moseschipanga4970
@moseschipanga4970 3 месяца назад
Aaah ASE iweyo ulikutiko
@HopeNandola-ew8td
@HopeNandola-ew8td 4 месяца назад
Kkkkkkk kod amaneyi ndiwakut kkkkkkkk
@MasterJailos-kv5sd
@MasterJailos-kv5sd 4 месяца назад
Omwe sunawachulewo ndi omwe angawine
Далее
Ching'aning'ani comedy, ft Ngiringande
6:53
Просмотров 308 тыс.
Разоблачение ушные свечи
00:28
Просмотров 504 тыс.
LATEST NAGAMESE NEWS 6/8/2024 MORNING UPDATES
11:15
Просмотров 12 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 62 тыс.
MOSES KUNKUYU EXCLUSIVE INTERVIEW
56:13
Просмотров 28 тыс.
KAFUKUFUKU PA IMFA YA ACHILIMA
30:18
Просмотров 137 тыс.
zaululika!! Miracle Chinga amapanga uhule
9:19
Просмотров 69 тыс.