Kod ndinu muli ndi ka RU-vid Channel kanu kopepela mumakatcha bakili muluzi 🤣🤣🤣, zot kutali pass out week yatha ya ma cadet simumaziwa? Zot kunafika ma general from different countries like Zambia, Rwanda, eswantin, Mozambique,Kenya, Tanzania pamwambowo chifukwa ena mwa omwewa amapanga pass out are from those countries simukuziwa iyayi? Page iyiyi yazaza NDI ma bulutu.. very foolish, stupid and ignorant.. ka school kaja pena pake kamathandiza
This is true story I remember well my friend from Rwanda who were taken to that country they were killed by this guy's truly you can feel bad what I Saw that time please work up Malawi
Km iziz sizabwino these ppo came here bcoz they wanted peace and they hav sweat alot fo them to get wat ever they hav now penapake ndbwino kumaganiza kut ndtakhala ine ndkupangidwa zimenezo ndnganve bwanj, God must be the only helper
As malawian citizens I will never allowed this nonsense to happen m"boma liyenela kuwasiya anthuwa tizikhalanawo mwantendele ngatimene timakhaliramu osamati kumazuka ndikumasawusa mitima yaanthu osalakwa
Whaooww 😲😲 I can't believe that in Malawi you have such brilliant journalist 🤔🤔 Tell them, teach them 😂😂😂 Many people don't know exactly what we be the consequences of the presence of this rwandeses on the Malawi land
Malawi lero Ali pa mpeni vuto ili Matsatatsata Amalawi lero ndi izi Ntchito Qne million zija ma Mega farm aja Kudya katatu kuja ndikumeneku amalawi kususuka lero ndi nkhondo iyo