More Fire 🔥 🤧......Bon Kalindo....Auze amenewo amvetsese...Chakwera wationongera Mother Malawi... People are suffering tindikwera kwa zithu zofunika kwambiri.
Winawe olo manyazi ulibe, ukulimbana ndi Bon Kalindo apa , CHOTI udziwe Bon Kalindo ndi president waife osauka ndipo izi akuuza ife, iweyo abale ako nda a Chikangawa Party takudziwa shame on you! Our president please more 🔥🔥🔥 Tell them the truth, winawe uziluma pa mchombo, wekha- wekha- kunyoza Bon Kalindo yaaa , Useless boy
Ayiwala kuti ndalama zo agule fertilizer NDI mbewu za subsidy kuti mwina anthu alandile mwachangu komanso anthu ambiri Koma azapeleka mbewuzo February chaka chamawa