Тёмный

BON KALINDO KUYANKHULA PAMBUYO PA CHIGAMULO CHAKU COURT 10 July 2024 

HOT 265
Подписаться 69 тыс.
Просмотров 10 тыс.
0% 0

Опубликовано:

 

8 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 65   
@MuhajirinaSaid
@MuhajirinaSaid 17 дней назад
Keep it up mr Dc
@ForsterThawan
@ForsterThawan 17 дней назад
Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu
@user-lz5yv4vj6h
@user-lz5yv4vj6h 17 дней назад
Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir
@josephinemisomali6840
@josephinemisomali6840 17 дней назад
Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!
@NelsonbastonMandela
@NelsonbastonMandela 17 дней назад
Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂
@robertchitsulo8006
@robertchitsulo8006 17 дней назад
Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk
@SamfrayGvng
@SamfrayGvng 15 дней назад
Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC
@user-mk7fh5ml8s
@user-mk7fh5ml8s 16 дней назад
Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤
@user-jk8sh7fh2d
@user-jk8sh7fh2d 17 дней назад
Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 17 дней назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂
@AufiThera
@AufiThera 16 дней назад
Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa
@TougiedaAjam
@TougiedaAjam 16 дней назад
It's the Dc keep it
@PeterKathewera
@PeterKathewera 16 дней назад
Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢
@AlickMakunganya-o4w
@AlickMakunganya-o4w 16 дней назад
Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂
@PetroMatias
@PetroMatias 17 дней назад
🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 16 дней назад
DC 🥰
@EvsonNgurube
@EvsonNgurube 16 дней назад
Bon kalindooooooo
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 17 дней назад
Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?
@AufiThera
@AufiThera 16 дней назад
Wanthu wanthu DC 💪
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e 16 дней назад
DC ❤
@MariamJaffali
@MariamJaffali 17 дней назад
Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 15 дней назад
Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili
@user-fz3gu2ez1o
@user-fz3gu2ez1o 15 дней назад
Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe
@MisheckAselo
@MisheckAselo 17 дней назад
Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 17 дней назад
Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤
@GracePhirie
@GracePhirie 16 дней назад
Mwana woipa kwambiri😂😂😂
@allansili-rc9gc
@allansili-rc9gc 17 дней назад
🤣🤣🤣🤣 mpaka a police 200 kkkkk
@williamchatha6139
@williamchatha6139 16 дней назад
The DC salute
@ShaibKudzinja
@ShaibKudzinja 17 дней назад
The DC, ndipo anthu tizamulilira kwambri mkului nd ntchto yakei akazasamira mkono
@ZexNkhoma-p8t
@ZexNkhoma-p8t 17 дней назад
The braval child of Malawi, Speak out without fear and favor! Bon kalindo, The DC...
@user-mi3fw1zg8b
@user-mi3fw1zg8b 16 дней назад
😂😂😂😂😂the DC machine
@kondwanimandala4575
@kondwanimandala4575 16 дней назад
Winiko the DC pachilungamo sumawopa iweyo umatha
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 16 дней назад
❤❤❤❤❤ more fire 🔥
@lazarousnamakhwa6549
@lazarousnamakhwa6549 16 дней назад
boni kalindo malawi 😂😂😂😂
@IbrahimYusufu-z9d
@IbrahimYusufu-z9d 16 дней назад
Bon Kalindo
@NorahMangasanja
@NorahMangasanja 17 дней назад
Mr Dc mumakwana inuyo tilinanu ife amalawi
@HaruunWalusa
@HaruunWalusa 16 дней назад
The DC
@moseskalande9853
@moseskalande9853 16 дней назад
zopanda ntchito zomwe ukulu inu mumalankhula
@nafejonga972
@nafejonga972 17 дней назад
Chizagwira zipolopolo😅😅 iwe ndi machine, wait to destroy them with you
@EmmanuelNgambi-y6h
@EmmanuelNgambi-y6h 16 дней назад
Umakwana DC
@user-zs6qc9dx8s
@user-zs6qc9dx8s 17 дней назад
The DC🔥
@user-ql8nf2vb8s
@user-ql8nf2vb8s 17 дней назад
It's plezident of poor people
@AustinBornface
@AustinBornface 17 дней назад
The DC!
@ArnoldKamanga-r6k
@ArnoldKamanga-r6k 17 дней назад
Uyu yekha timuteteza I swear
@PoxisNation-fe1kr
@PoxisNation-fe1kr 16 дней назад
The DC 😂😂😂
@OnexAliMwale
@OnexAliMwale 16 дней назад
Kulankhula wina aliyese atha kulankhula koma kuchita zakupsa...Bwana Bon kalindo akumalankhula koma ndi action yanji yomwe ikuchitika? We need kulankhula ndikuchita namaona progress..Mukatiuza zomwe mwapezazo kenako muzinenanso kuti tipanga izi pothana ndizimenezi...tisamangokhalira kumva mwana oopsa mmalankhulidwe, action nothing
@myheartforkids2876
@myheartforkids2876 16 дней назад
Inu mene mwayankhulamu mwapanga action yanji? Kkkkkkkkkk
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 15 дней назад
Kkkk mbuli ife timakonda DC
@OnexAliMwale
@OnexAliMwale 15 дней назад
@@myheartforkids2876 Amene amawatsata omenyera ufulawa atha kudziwa kuti nthawi ya Bingu kunali Mavuto Bamusi ndipo amati akanena amapanga action ndipo Mpaka Bingu anasintha machitidwe azinthu zina, nthawi ya Peter kunali Timothy Mtambo, za amenewu mukudziwa zomwe amachita, Koma Bwana Bon mmmm tiyeni tizingomva Mwana oopsa komanso kung'alura kenako tiseke osaona chisintha...I always appreciate for actions not talking that's why tonse Government tikudana nalo coz nawoso kulankhula amatha koma kukwanilitsa kukuwavuta
@RedrawLittleMushutula
@RedrawLittleMushutula 16 дней назад
DC mewafika
@williamalvis6028
@williamalvis6028 17 дней назад
The DC umakwana
@phindiswatshibo7101
@phindiswatshibo7101 17 дней назад
Chipangoline😂😂
@chipanganofackison5185
@chipanganofackison5185 17 дней назад
Zamanyi basi kape ndiweyo akanadakhala Ofuna kupha akanampha iweyo umatisokoneka mutu amakutuma ndindani? Umango uwanamizila anthu wosawuka ndidziko lanji lomwe kungapezeke wolemera wose?
@musaphiri317
@musaphiri317 16 дней назад
Iwe akupasa zingati koma inu ndi onvesachifundo kupusa uchisru
@SamKaposa-i5c
@SamKaposa-i5c 16 дней назад
Nyau imeneyi itayeni
@EvsonNgurube
@EvsonNgurube 16 дней назад
Matako ako nyau iwe
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 15 дней назад
Kape uyu
@moseskalande9853
@moseskalande9853 16 дней назад
Even ur voice doesn't sound like a leader
@FrankMulola
@FrankMulola 17 дней назад
😂😂😂😂😂
@samhussen708
@samhussen708 17 дней назад
😂😂
@brightkaunda920
@brightkaunda920 17 дней назад
Ati amangidwe ndamako
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x 17 дней назад
😂😂😂😂😂Amangidwadi ndi amake a Chakwera 😂😂
@chifukanyo9447
@chifukanyo9447 17 дней назад
😂😂😂
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 15 дней назад
Kkkk
Далее
Stay on your way 🛤️✨
00:34
Просмотров 9 млн
ODM Leadership in Kenya Kwanza Government.
43:38
Просмотров 5 тыс.
ZOMWE ZACHITIKA KU ESCOM YAKU BLANTYRE🙌🙌🙌🔥
20:54
Lwasa afunye sente bupya,aguze benz ne rangerover
30:52
Times Exclusive featuring Bon Kalindo - 6 January 2024
1:03:20