Тёмный

Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI” 

Makosana
Подписаться 66 тыс.
Просмотров 31 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

9 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 81   
@user-ix2ux5ss1b
@user-ix2ux5ss1b 21 день назад
More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika
@JowasiMasina-fy8ji
@JowasiMasina-fy8ji 21 день назад
Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏
@EversDman
@EversDman 20 дней назад
Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯
@LuyoloTlhapane
@LuyoloTlhapane 14 дней назад
A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila
@PeterKasiya
@PeterKasiya 20 дней назад
Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili
@MomeryPhiri
@MomeryPhiri 20 дней назад
❤❤❤❤❤❤❤ love it
@user-kk4uj8ko8k
@user-kk4uj8ko8k 21 день назад
bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo
@user-xm5cq1fb8g
@user-xm5cq1fb8g 20 дней назад
Ulemu wanu big❤❤❤❤❤
@user-dj6rc3lc4t
@user-dj6rc3lc4t 21 день назад
Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana
@UthmanKapungu
@UthmanKapungu 21 день назад
Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife
@neemahkapatamoyo9563
@neemahkapatamoyo9563 21 день назад
Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
@AffickChaona
@AffickChaona 18 дней назад
❤❤❤❤❤
@DauglassNkhoma-dj9lp
@DauglassNkhoma-dj9lp 20 дней назад
😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi
@FarookRaphael
@FarookRaphael 21 день назад
More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 21 день назад
Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂
@FlorryVugy
@FlorryVugy 20 дней назад
A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂
@user-wm4rs4kd7d
@user-wm4rs4kd7d 21 день назад
@user-lg6ym4hz3w
@user-lg6ym4hz3w 21 день назад
Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira
@user-hq8fw5hz2l
@user-hq8fw5hz2l 21 день назад
Awa ndie mawu
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem 21 день назад
Big up bro
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j 21 день назад
Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima. Agalu a anthu ndithu
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 21 день назад
😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe
@EllinaBitto
@EllinaBitto 21 день назад
Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@FwasanMwenefumbo-zq7sg
@FwasanMwenefumbo-zq7sg 21 день назад
The DC 🔥
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 21 день назад
Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
@HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 21 день назад
Ambuye akudalitsen
@PeterMaulana-qk5uq
@PeterMaulana-qk5uq 21 день назад
Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!
@NdawaPhillipfortunePhakatie
@NdawaPhillipfortunePhakatie 21 день назад
Motor 💥 kalindoooo
@user-zt3gv7md6x
@user-zt3gv7md6x 20 дней назад
Zoona amwene
@FrankMilias-og3js
@FrankMilias-og3js 21 день назад
Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko
@BernadettaTengula
@BernadettaTengula 20 дней назад
Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂
@JoyceChitsulo-mw7wg
@JoyceChitsulo-mw7wg 21 день назад
Makosana apa nde mwapita
@ericlarks8165
@ericlarks8165 21 день назад
,🔥🔥🔥🔥
@benjulius6070
@benjulius6070 21 день назад
😂😂😂😂😂😂
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 20 дней назад
Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza
@user-kx4cj7iu9q
@user-kx4cj7iu9q 21 день назад
Dc
@D.RJALLI-qo6yd
@D.RJALLI-qo6yd 21 день назад
Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa
@VincentMalika-w7x
@VincentMalika-w7x 21 день назад
Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath
@EdwardMukholi
@EdwardMukholi 21 день назад
Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi
@RamseyWasi
@RamseyWasi 21 день назад
Blasa, Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC) My opinion: Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.
@SmartMoles
@SmartMoles 20 дней назад
Zofunikila kulangura mwayangure kumene
@BlessingsKalonga
@BlessingsKalonga 20 дней назад
Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha
@ChisomoamitoniSauzandeamiton
@ChisomoamitoniSauzandeamiton 21 день назад
bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu
@JuliusMunthali-z7j
@JuliusMunthali-z7j 21 день назад
Awuzeni
@directorkfuture118
@directorkfuture118 21 день назад
Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂
@gerrardgladstone2473
@gerrardgladstone2473 21 день назад
Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣
@user-dm6xq6cp1m
@user-dm6xq6cp1m 21 день назад
Ai zikomo 🥱
@HendersonDziwa
@HendersonDziwa 21 день назад
Dzelu zachepa kkkk
@maxwellcaptain3937
@maxwellcaptain3937 21 день назад
Kalindo samaopa😂😂
@TshepoModise-xs4qu
@TshepoModise-xs4qu 21 день назад
Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee
@user-tw5iw7gf2v
@user-tw5iw7gf2v 21 день назад
😂😂😂😂 mpaka muchenga license
@ChrispinEdward
@ChrispinEdward 20 дней назад
Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto
@MathpeterLemon-ls1ns
@MathpeterLemon-ls1ns 21 день назад
Ati kutitola kapena chani
@DaudiAbdullah-o5l
@DaudiAbdullah-o5l 20 дней назад
Mumatiyimilila
@nicholasmutano6017
@nicholasmutano6017 21 день назад
Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?
@user-yl3lg5fk8f
@user-yl3lg5fk8f 21 день назад
Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious
@PeterGrant-ih1sr
@PeterGrant-ih1sr 21 день назад
Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 21 день назад
Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk
@ikmusic-s9f
@ikmusic-s9f 21 день назад
koma nde eeee mpaka licence mchenga
@pempheroraynnoxmpesi8713
@pempheroraynnoxmpesi8713 18 дней назад
😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp
@user-ls5zj8qn6k
@user-ls5zj8qn6k 21 день назад
Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 21 день назад
Bigiliman naweni
@sir-wanton-2001
@sir-wanton-2001 21 день назад
Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo
@YonaMartin-kb3do
@YonaMartin-kb3do 21 день назад
😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe
@AaronLitete
@AaronLitete 21 день назад
Kkkkk boma lopusa
@user-ky8us1ff5b
@user-ky8us1ff5b 21 день назад
😅😅😅😅
@CaptainNyenga
@CaptainNyenga 20 дней назад
😂😂😂😂😂 koma DC
@lytonmaseko4534
@lytonmaseko4534 21 день назад
😂😂 kung'alulatu
@user-vn1wq6wg6i
@user-vn1wq6wg6i 21 день назад
K.K😂
@YohaneMbewe-u4k
@YohaneMbewe-u4k 21 день назад
😂😂😂😂
@AnthoniohMazengera
@AnthoniohMazengera 20 дней назад
Hahahahahahahahahaha😂😂😂
@Aluwenkareem-ev3ro
@Aluwenkareem-ev3ro 20 дней назад
😂🤣😂🤣
@PhillipMtonga-g7o
@PhillipMtonga-g7o 21 день назад
🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance
@GiftKulture
@GiftKulture 21 день назад
🤣🤣🤣🤣 mipunga
@BenjaminKayembe-j7j
@BenjaminKayembe-j7j 21 день назад
km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km
@Kachelephiri
@Kachelephiri 21 день назад
Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 21 день назад
Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe
@ChristopherKawilam
@ChristopherKawilam 21 день назад
Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe
@user-wz6jy3re8n
@user-wz6jy3re8n 21 день назад
😂😂😂😂😂😂
@MadalitsoManyozo
@MadalitsoManyozo 21 день назад
😂😂😂😂😂😂😂😂
@myheartforkids2876
@myheartforkids2876 21 день назад
😂😂😂😂😂
Далее
MANGANYA VS AKWENI - KWAPHULIKASO INA KU UTM
13:37
Просмотров 33 тыс.
Meninas na academia
00:11
Просмотров 2 млн
PATRICIA KALIAT WABWENZA MOTO KACHIKENASO
12:51
Просмотров 19 тыс.
Maloto A Bon Kalindo (Part 2) - Bon Kalindo
14:17
Просмотров 109 тыс.
Top U.S. & World Headlines - July 29, 2024
10:31
Просмотров 176 тыс.
Meet the Press NOW - July 29
49:59
Просмотров 945 тыс.