Тёмный

BON KALINDO LERO UTM YAGULITSIDWA NDI MCP 🤔🤔🙌🙌 

HOT 265
Подписаться 82 тыс.
Просмотров 21 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

28 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 104   
@MansonNyamwela-g5r
@MansonNyamwela-g5r 2 месяца назад
Mr DC, watching you live from dar es salaam, Tanzania.just wishing you a very great Sunday, keep on doing good job.
@GreyMwanyimbo
@GreyMwanyimbo 2 месяца назад
Kalindo wabalalika kuno!!!!!!! This is the game of politics
@xinalungu9616
@xinalungu9616 2 месяца назад
Wabalalikadiiii kkkkkk
@edsonnyasulu5394
@edsonnyasulu5394 2 месяца назад
Bwanji manganya asiye utm please
@JohnfosterNkusengwa
@JohnfosterNkusengwa 2 месяца назад
Restening from cape Town pa boma❤
@MaryNgola
@MaryNgola 2 месяца назад
Inutu ngt mumadziziwa kt ndinu a MCP ndibwino musamamvele Za born kalindo,chifukwatu tsiku lina mudzagwa ndi BP,ngt likumulephera boma nde kulibwanji iweyo????
@CharityMhone-uk9ym
@CharityMhone-uk9ym 2 месяца назад
Inenso munthu uyu ndimamudabwa akayankhula zambiri zomunena chilima pano wafa ..akuonetsa ngati iye amamkonda mmm Ada Inu mdziwen Yesu kusanade...vuto anakumanan udindo..mwamutukwana peter eeeee pano ukutinso peter ndiwabwino😮😮😮😮
@rashidadan2533
@rashidadan2533 2 месяца назад
Yudas anali ophunzila wa yesu , komanso yudas anamugulitsa yesu , History is the best teacher .
@jeremiahmalikebu2393
@jeremiahmalikebu2393 2 месяца назад
Palibe zogulitsidwa! Zikuchitika ndi Manganya ndi propaganda ya MCP. Koma ma supporter a UTM enieni tili nganganga pambuyo pa UTM ndi Kaliati. Team iri ku MCP yo ikhale komweko
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 2 месяца назад
Iwe Kalindo zangokuvuta kkkk you’ve met your match in Jesse Kabwira…..munatumbwa kwambiri pakatipa nde pano mutsegula mmimba simunati 😂😂😂
@ShabaniKuswere
@ShabaniKuswere 2 месяца назад
Kodi Jessie Kabwira ndendani?
@Martinmkapangakapanga
@Martinmkapangakapanga 2 месяца назад
dzeru palibe
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 2 месяца назад
Dziko la Malawi Lili pa mavuto eeti eeeish 💔😭 which means will be in trouble forever
@GregoryMatambo-m6y
@GregoryMatambo-m6y 2 месяца назад
Osasunga legacy iweyo bwa
@mzeewandembonyirongo2972
@mzeewandembonyirongo2972 2 месяца назад
Akufuna aku banja aziwadyera..ndrama
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 2 месяца назад
Usi ndimuthu oyipa kwambili mm ndiapo anamupereka chilima
@MazyYanga
@MazyYanga 2 месяца назад
My president
@Cee-H-Cee
@Cee-H-Cee 2 месяца назад
First to watch
@hot265.
@hot265. 2 месяца назад
Kukunyadilani Thanks 🙏
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 2 месяца назад
❤❤ zomwe amayankhula uyu ndi zeni zeni and zikuchita kuwonekelatu
@OmegaChingamuka
@OmegaChingamuka Месяц назад
Mwati M C P ndi yazibekete 😂😂😂😂😂😂
@yobesaikonde6166
@yobesaikonde6166 2 месяца назад
Kalindo drama amatha go ahead we will keep roughing kkkkkk
@tasmania527
@tasmania527 2 месяца назад
Aise Kalindo umandiwaza ndi nthabwala zako. Please keep up the good work ya nthabwalazo- the DC mwana oopsya kwambiri kkkk. Bwanji osangonena kuti umafuna UTM ipite kwa Adadi? Come on man be honest...kodi zakuwawa eti? Nobody should be mad at Kalindo because he's a funny dude.
@Martinmkapangakapanga
@Martinmkapangakapanga 2 месяца назад
osati nthabwala koma zoona
@MisheckZako
@MisheckZako 2 месяца назад
Dc
@victormbewe7462
@victormbewe7462 2 месяца назад
Let's admit that politics has become a global problem
@MercyHassan-p4e
@MercyHassan-p4e 2 месяца назад
😂😂😂😂 mukharise a president anthu anthu aanthu osauka mumatipasa chirimbikitso ndipo timakhurupirila kuti tsiku rina tidzadyera nyama ndipo dima ungakute bwanji kunja kudzawara dzuwa ridzaomba Bon karindo woyeeeeee, timakutsatani ngankhare tiri kutari ndi dziko ra malawi🇲🇼💗
@LashidMalindima
@LashidMalindima 2 месяца назад
Mumakwa adala
@NoorRasheed-re5vh
@NoorRasheed-re5vh 2 месяца назад
Ukufuna tiziyendela.maganizo ako ulapa
@daltonjafali3856
@daltonjafali3856 2 месяца назад
We salute you our president
@esaMoha-dm4kj
@esaMoha-dm4kj 2 месяца назад
Nkalindo bwanji mullipo mulinkut bwanj malipot andege ankushedwaso after too months guys shonde bk TV mtanyiwwa
@lyiemax
@lyiemax 2 месяца назад
Zomvetsa chisoni kwambiri, may the spirit of SKC do something on this bad move
@GodfrleyTembwe
@GodfrleyTembwe 2 месяца назад
Warira mokweza kunooooo 😂😂😂😂
@thulanimpphiri6873
@thulanimpphiri6873 2 месяца назад
Ngat utm inatuluka mu mcp pali chifukwa chani chovalirira makaka pa musonkhano wa mcp. Zimene zinapita kukalandira president ndi makaka a utm ndi zisiru zipanda zeru sizikuziwa kuti uku ndi kwa mcp uku ndikwa utm sizikusiyanisa. Or usi asavareso makaka a utm
@JohnNamakonje
@JohnNamakonje 2 месяца назад
True
@junasssabiwa1996
@junasssabiwa1996 2 месяца назад
DC
@YammsyZebron
@YammsyZebron 2 месяца назад
The DC great
@GodfrleyTembwe
@GodfrleyTembwe 2 месяца назад
Akalindo agwira pambali
@xinalungu9616
@xinalungu9616 2 месяца назад
UTM and Kaliati has no money to run the party. If MCP is funding UTM, let them help UTM an alliance partner. Dr. Kabambe has 50 followers in Thyolo, considering his last rally. He doesnt have money either. Its Utsis camp through MCP n Mary that have money.
@mzeewandembonyirongo2972
@mzeewandembonyirongo2972 2 месяца назад
Kabambe has money...only that is relatively new in politics and giving out money is not his taste. In UTM Kambala is doing everything by himself. Imagine the whole top guys beg fuel money from him. Money as less than 300, 000 kwacha. They want him to pay. They the rest are not contributing to the party. And seems Kambala is tired. He is being told kuti zabwino zikubwera soon😮
@MosesTchauya
@MosesTchauya 2 месяца назад
Ndiwe wachipani chanji iweyooo
@OnenessLestas
@OnenessLestas 2 месяца назад
Kalondo ife MCP timayikonda enafe zokamba zako sizimatisangalatsa ai
@PreciousDzonzie
@PreciousDzonzie 2 месяца назад
Wamisara wamisara wamisara zindikiran nose mumatsata citsiru ici kt ndiwamisala watsara pang'ono kuyamba kutora zinyatsi uyu kkkkk
@brightkaunda920
@brightkaunda920 2 месяца назад
Iweso ndekuti ndiwamisala bwanji ukumutsata?
@kondwanivyalema9449
@kondwanivyalema9449 2 месяца назад
Mbava zaba Chipani cha SKC
@MphatsoMwale-it4xd
@MphatsoMwale-it4xd 2 месяца назад
Kalulu mwale from jonz D C tiyenaoni ambalame amenewa
@LindaLimbe-fo1oy
@LindaLimbe-fo1oy 2 месяца назад
Ulemu wanu bwana Kalindo
@Martinmkapangakapanga
@Martinmkapangakapanga 2 месяца назад
l like u born
@AnnieJutta
@AnnieJutta 2 месяца назад
Mr DC sizokanika kung'alula apa ai popeza ndimzanu manganya nenani kuti manganya wagulitsa chipanichi ku MCP ndipo akunama kumwamba Mulungu aliko angoutsa mkwiyio wa Yehova chabe mapangano akeo ndiopusa akuganiza MCP ingakamupatseso u vice president 2025 ndi munthu omvetsa chisoni betrayer
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 2 месяца назад
No ways....anthu ogulidwa ndi Manganya amenewo not real SKC followers
@SlindiryLoveness
@SlindiryLoveness 2 месяца назад
Koma akalindo pumani kaye pathe mwezi umozi nkhani yikuwoneka kuti yatha mumutumo ndiye mukhale kaye cheti muzitipasa nkhani zanzeru ndiye kuti aroma alowelerepo kodi UTM ndiya roma koma munthu uyu
@DicksonLutere-p9k
@DicksonLutere-p9k 2 месяца назад
Kalindo wayamba kulila kuno imeneyo ndiye politics kkkkk
@ChawezChinkhuntha
@ChawezChinkhuntha 2 месяца назад
First comment ❤
@hot265.
@hot265. 2 месяца назад
Mumakwana Thanks
@JamesSingini-t4j
@JamesSingini-t4j 2 месяца назад
Kupita Ku msonkhano wa MCP doesn't mean uzavotera MCP Mr kalindo aaaaaaaaahh,,,aja anapita Ku convention ya DPP ali mu makaka a utm,afford,why smunanene kut ndi a DPP??? Nde palibe chifukwa wa utm kupita kokalandla chakwera coz vote Nd mtima nde musasegule nazo mmimba..
@mathewsnachuma8086
@mathewsnachuma8086 2 месяца назад
Maganya ayakhule za 5 years tione pomwe uziwe kut siwa utm
@FannyWadson-zg4oj
@FannyWadson-zg4oj 2 месяца назад
Inu mwaoneka kale vote yanu munama kuti ndi mtima bwanji
@BoscoKalua
@BoscoKalua 2 месяца назад
a DPP UDF UTM AFORD ndi onse enanu tengani zimene akune bon kalido seriously if not then you are finished completely and forget to be in government in 2025
@xinalungu9616
@xinalungu9616 2 месяца назад
Bwanji tinene kuti IWE CHILUNGAMO NCHAKUTI ndiwe munthu WA NSANJE kwa anthu amene si a Ku Mulanje or Thyolo. Correction. Iwe SI PRESIDENT WATHU ayi. I we ndi president was anthu 50 amapanga ma demo timawaona aka. Kkkkk NSANJE. KKKKKK
@HarryThomson-n7n
@HarryThomson-n7n 2 месяца назад
M matiimiliradi man
@GraceMbwana-y8d
@GraceMbwana-y8d 2 месяца назад
Amene mekuyankhulanu mukungofuna ndalama ife anatinyasa kale mtambo
@kingsleyhopematchaya5184
@kingsleyhopematchaya5184 2 месяца назад
Iweyo mesa chili a umamunyozaso lero ukhale ngati umamukonda chili a wosokoneza iwe
@AchinaKellz
@AchinaKellz 2 месяца назад
apita okha ku chikangawa ife tidangoyikonda utm but the moment they join mcp ife tonse ku dpp basi or atangura anthu 200 ife tikukawinisa dpp
@chimwemwenkute3839
@chimwemwenkute3839 2 месяца назад
Tge DC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri
@omarajibu860
@omarajibu860 2 месяца назад
Dziko kuwonongeka chifukwa cha dyera, ndalama.
@mthelisokadambo8895
@mthelisokadambo8895 2 месяца назад
Chapompano uyuyu uyu tipita naye ku mental Ndale ndi choncho
@PaulWilly-ge1tx
@PaulWilly-ge1tx 2 месяца назад
Zoona
@TaweniChavulaKamwendo
@TaweniChavulaKamwendo 2 месяца назад
Eee
@MoreenSemu
@MoreenSemu 2 месяца назад
Aliyese akunena zakuti awina wabalalika kalindo😅😅😅
@GregoryMatambo-m6y
@GregoryMatambo-m6y 2 месяца назад
No logic why kuveka anthu ma t-shirt yet you know kuti ndi anu kale kkkkk . Aaaaa kulowerera za catholic Kkkk fotseki
@CassimMbalaka
@CassimMbalaka 2 месяца назад
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxiwa pa ifa ya chilima
@EsetaGerate
@EsetaGerate 2 месяца назад
❤❤❤❤
@HarrietSainetStone
@HarrietSainetStone 2 месяца назад
😢
@MarkBannda
@MarkBannda 2 месяца назад
Kalindo, you don't have evidence you are just making pipo to fight
@Paworo-h5r
@Paworo-h5r 2 месяца назад
Awuzeni anthu azipita kumunda si nthawi yochemelela zipani iyi. Inu ndi amene mumabweletsa njala every year
@ElizabethMulinde
@ElizabethMulinde 2 месяца назад
Mmmm zabodza izoo
@MulowokaBlessings
@MulowokaBlessings 2 месяца назад
A DPP adadi Anu amene ananena kuti ovotera MCP amwa mutnjani KOdi amawauzao ndi a Malawi?olo ndaku Mozambique?a Kalindo misara yakulisa yendani ku Mental
@GraceMbwana-y8d
@GraceMbwana-y8d 2 месяца назад
Choti muziwe adale simuzatheka mpakana kalekale ifetinakuziwani
@StephenPrinceScale
@StephenPrinceScale 2 месяца назад
The DC😂😂😂
@ElesonChalemera
@ElesonChalemera 2 месяца назад
A Mr kalindo ingojoinani ndale chifukwatu mmm zomenyera ufulu zakukanilani ndithu sizikuendapo
@worldamazingvideoz9416
@worldamazingvideoz9416 2 месяца назад
Wamisala anaona nkhondo
@GiftMaiden-g5w
@GiftMaiden-g5w 2 месяца назад
Live show
@ephraimkadamika
@ephraimkadamika 2 месяца назад
No utm singathe utm yeni yeni tikuyidziwa
@JonathanMtambo-w6e
@JonathanMtambo-w6e 2 месяца назад
This. was already planned before. chilima was killed
@ChicoBanda-kq7py
@ChicoBanda-kq7py 2 месяца назад
Pitilizani bwana
@DumisaniMhango-e4i
@DumisaniMhango-e4i 2 месяца назад
Or atagula sitingavotele awa akanganya awa
@JimmyMhone-b5p
@JimmyMhone-b5p 2 месяца назад
Manganya wagulisa chipani cha UTM kung'ona
@JeanKabotolo
@JeanKabotolo 2 месяца назад
Maganya munthu oipa
@bridgetmajor3646
@bridgetmajor3646 2 месяца назад
Ndare ndi Mabozatu
@macchitsulo2986
@macchitsulo2986 2 месяца назад
Munthu amene angavala zovala za utm koma ali wa chipani china magulu ake ali ngati iweyo the DC
@sauuladi6753
@sauuladi6753 2 месяца назад
Zakeyo
@MaikNkhoma
@MaikNkhoma 2 месяца назад
Inu munapenga palibe zazelu mungakambe
@moseskapelekeza8849
@moseskapelekeza8849 2 месяца назад
Mukuva kuwawa man
@MulowokaBlessings
@MulowokaBlessings 2 месяца назад
Akalindo zipitani chabe ku DPP uko
@TelinaNjanje
@TelinaNjanje 2 месяца назад
ⁱᶠ ⁱᵗ ˢᵒ ᵗʰᵉⁿ ᵗⁱᵏᵃᵛᵒᵗᵉʳᵃ ᵉⁿᵃ
@RobertMisheck-w1v
@RobertMisheck-w1v 2 месяца назад
Awanso mutu wamaminawo
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 2 месяца назад
A MCP ndi mbulidi zoona, sasiyatsa za boma ndi chipani, mai awa azitengela pa mgong'o.
@ziyamporoma377
@ziyamporoma377 2 месяца назад
@@MathewKalinkhu Inuyo mukamayankhula ntudzu mumasiyanitsa ?
@LukaThawe
@LukaThawe 2 месяца назад
Ndipo mbuli ndiyeyo
@isaacybanda-s6e
@isaacybanda-s6e 2 месяца назад
Mumatha inuyo bwana
@ChilindeHarry
@ChilindeHarry 2 месяца назад
Za chamba zokhazokha.
@Cee-H-Cee
@Cee-H-Cee 2 месяца назад
First to watch
Далее
Top U.S. & World Headlines - October 23, 2024
13:41
Просмотров 184 тыс.
KUFA NDI NJALA UTAPHODA // DENIS MAHATA
29:56
Просмотров 17 тыс.
Face The Nation | GNU/Russia/National Dialogue/BOSA
54:24
BON KALINDO LERO 29 October 2024
12:46
Просмотров 4,9 тыс.
born Kalindo wa lero pa 29 October 2024
13:12