❤❤❤ mr DC. Opposition please wakeup ndinakuwuzani kuti mec inene anthu wose omwe ali ndi ma ID district by district. Ife tili kumbuyo kwanu osusa koma musagone tikufuna kukoza.
Mukungolimbana ndi a chakwera koma chakwerayo sakuyankhani nkomwe, ndie vuto lanu nchiyani? Mbuyomu mwakhala mukuti muvula n muyenda munseyu muli chivulireni chifukwa chot ma alubino akungofa koma lero muli kumbuyo kuikiraso omwewo amene ankapha alubinowooo ndie nkumati amalawi azikutsatani inuyo?? Shame on u akalindo. Chanzerutu ndikuyang'ana kwa Yehova basi not munthu obadwa kwamunthu ai coz ulamurilo wolamulidwa ndi anthu ndiolephera basi
Akulimbana chifukwa ndi driver wa Malawi right now, bus ngati sikuyendesedwa bwino anthu samaloza ma passangers ai a maloza driver, wabwadwa liri let me remind you, ma presidents onse ngakhale chakwera amazuzula a dpp kuti sakuyendesa bwino
Kod uyuu DC akamati ndioophyaa amatanyhaunji kutulusa ma vn bs kupanga mademo adaleka kalekale ndiye kuophyako kuli pati mumamuziwa munthu oophya kkkkk samaopa mademo osaliopa boma kom uyuuu ndayamba kumusamuka he is not serious