Koma iweyoo dc ndikanakhala kuti ndimatha mayere ndikanangoaloza onse a mcp ndi kupangaso enawo angonena kut president wathu ndi bon kalindo umatiyimilira wokukumbira dzenje agweremo wokha in Jesus name
Mumalankhula kuchoka January mupaka lelo za mademo koma tsitikuwaona mademo Pena tiganiza kuti mumadyapo mukalankhula za mademo mukalephela apapa muzalankhuleso za mademo chifukwa yangokhala nyimbo
ma demo akhalekodi koma this time ku mzuzu asakhaleko chifukwa amatenga serious kwambiri ku mzuzu ndikuphana,ndiye akhale ku Lilongwe blantyre ndi ntcheu