We always supporting you all freedom fighters in malawi , You encouraging us as Malawians to know our freedom without scare anyone We will fight our freedom together with you . We will continue to blame the stupid things from any government
A Vice President athu Dr Michael Bizwick usi I like ur speech iwe umandiwaza komano bola Lazaro waumphawiyo asakutume pa Ndege mkudutsira ku Chikangawa Forest
Please Bon Kalindo do not associate with Timothy Mtambo, he is a devil 👿 just like Chakwela, please do not trust him, please, please. He is MCP do not be cheated.
VP zimene ukunenaz ndizoona km usatipusitse ai Ubwino wake the dc ndizako wenewene bola menyan nkhondo chakwera achoke Malawi abwerere pakale osat manyakawa
Michael usi as our vice president pamenepo ulemu wanu kumeneko ndiye kuyankhula kp it up.aboni kalindo akungonena zinthu zomwe akuziona ndimaso zomwe boma likuchita samaonjezera koma poti iwowo akulankhula chilungamo that's why amcp ndizimene amadana nazo .koma l love your speech 🎉🎉