Akuru u Comrade sitipangira ku dziko laweni....ndipo muthokodze kuti dziko la South africa siili pa ubale wabwino ndi dziko la malawi kamba ka nkhani ya bushiri ija bwedzi mutatumidzidwa kalekale kumudzi.....komaso ndikambepo za malawi first ...chiyambireni malawi 🇲🇼 first siinapangisepp mademo dziko .ndipo mademo onse amakhara akurephereka ...ndipo ngati kunali mademo ndi akalindo ndipo anadzungulira dziko lonse ....
Olo atakhala kuti bon kalindo analakwisa Koma simumayenera kupanga zimenezo,mukanayamba kaye kukambilana nyumba mwanu...a Ben longwe mwalakwisa..grow up man....
I think nkhani Yoona NDI iyi Mr Ben longer akunena Chilungamo anthuwo alandiladi vindalama zankhani nkhani kuchokera KU Boma , ndibwino nonse mungosiya kudzuzula Boma chifukwa Palibe chimanga inu asiyeni amalawi NDI Mulungu yekha amene amenyere nkhondo Ife Amalawi 1992 Mulungu anatimenyera nkhondo kumuchosa Kamuzu kuzaika Bakili Muluzi so don't waste your time live it
Ben longwe ndiwe kape kale ndimakutsata ndimaona ngat ndiwe wa nzeru koma pano ndakuona coz ukanakhala wa nzeru ukanabwela kudziko lako ndikumapanga zomwe ukunenazo tikanakukhulupila koma uli kwina nde ndikumati umazitsata assssaa ku mademo sumakhalako umangomva basi ndikumachuluka nzeru
Too shameful, I didn't expect Malawi First to be decided like this, if it's like this then who is going rescue us, we poor Malawians are going to suffer a lot
Nobody is wanted by either ICC or UNHCR Mr Ben we don't 've any problem with our leaders. Mr mphepo and Mr chipungu r very cool guy unless u have smthng against them
Comrade bwana Ben Longwe phunzirani kukambirana ku ma office anu aMalawi first chifukwa chomwe mungadziwe, Malawi first mwatenga aMalawi onse kukhala m'manja mwanu ndipo aMalawi pano adalira inu ndiye ngati pa maudindo anu ngati musanamvetsetsane please pezani njira zina mpaka mumvane.
Basi Malawi sazathekaso 😢sindinayembekezere kuti zikhonza kukhala zotere ku malawi first...my fellow Malawians let's just focus about our future don't trust these nosence called freedom fighters and politicians 🙌🙌
Bon Kalindo wayankha inde Koma Ben Longwe is right because Bon Kalindo sanatsutsepo Za kugulitsa mademo ndipo sanalowepo ai . Kwakulu wakana kulankhula momveka bwino kusonyeza Kuti ndi bodza
Azisogoleri nonse a Malawi First a Malawi ochuluka amakukonda I Komanso amakusatani ndiyeno mukayamba kutosana chonchi ndiyeno a Malawi athawire Kuti chonde anthu akuvutika
Ben wabodza uli ku jozi kuno ukukhalatso munkhunkhu ine ndimawona ngati uli kumalawi kkkkkkk Ben ndikape kkkkkkk za redson munuro ndi kalindo there together as one
Beni longwe usaputsitse anthu look your staying in South Africa koma kumakamba zakumalawi we know you Beni longwe u like to mess up things eshiii you know God knows kalindo alimumalawi momwemo redson munulo alikotso kumalawi koma Ben longwe uli kuno ku joni hahaaa alekeleni redson ndi awiniko amenyele ufulu anthu
Ben Longwe ndiwe mbuzi, coward,ongoyankhula pa Air pomwe Bon k the DC amamenya pa ground,Redson munlo ndi wamantha sangathe ku yenda pa nseu.....ine ndi the Dc viva Bon kalindo.
A Ben Longwe penapake tamakulani, MA audio anu ndinayamba kuwamva kale kwambiri ndipo ndimakutsani kwambiri koma Pena Pake kupupuluma sibwino, inu ngati vice president and president wanu walakwitsa mkungofikira PA air mwatani??