Listening to this song in deep grief for the loss of the vice president and the others who died in the plane crash in Chikangawa forest 😢😢😢 12/06/2024.
It’s 22 July 2023, exactly 1 week since we lost our son to cancer & this song has been on repeat. The only thing comforting us now. May his soul continue to rest in peace 🙏🏽😭
It's 14 years since mum died and this song was sung when the body for mum was lying in state at chipata RCZ. It touches me a lot,may the soul of my mother continue resting in peace till we meet by God's grace.
When ever I feel low I always listen to this song. It speaks to my soul. Knowing that God exist it's something special to me. Thank you so much madam Clara,
Our father who at in heaven God Lord continued Bless You Crala You know how to sing ,since iborn Malawi inever seen alady like you ,good voice love you
I had a friend we used to miscarriage a kangokhala ndi mimba. But when travelling to work, his husband use to put this song. Mpaka kukafika ku ntchito. As am talking now Ali ndi Ana awiri wa mkazi ndi wa muna zoonadi Mulungu amapuputa misozi.
It's been 12 days since I lost my mum.i have questions without answers. Last year I lost my husband. I'm just wandering in thoughts why I m passing through this!
The voice and dressing exactly Deborah Fraser a South African lady....she's also a gospel singer...I love her songs alot...so whenever I'm listening to Clara's songs always remind me about Deborah....this is how gospel artists should dress
My aunt, Iness Bwino Magwira used to sing this song when I was at Chikwawa,,, now she is no more,,,I always remember her when I listen to this song Only God knows why He took her so early Till we meet again aunt 😢😢😢
A song that brings one to God, and outpour his heart to Him in submission knowing that that Him alone is the solution to all the questions we have. Nditani ine kubwezera Mbuye. 🎉
Death pains iand there is nothing that can can be more painful than death. I lost my dear brother Bendicto chakanda kawonga on 29/12/23 in Lilongwe was taken chitipa was buried behind kalowe CCAP church . I thank the admiration the CCAP for the job they did for us when lost our dear son, brother , father, and this song encourages me that there still life after death my his soul rest in peace of God
2. O Yehova, Mulungu wa akutsogolo kwanga, aneneri, Inu ndinu Mulungu yekha m'mwamba, ndipo inu ndinu Mulungu yekhayo amene amalamulira milungu yonse ndi mitundu ya dziko lapansi. Ndipo m'dzanja lanu muli mphamvu ndi ny’onga. Inu ndinu Woyeretsetsa kwa kuyera. Inu Ndinu Mmodzi yekha, Inu Ndinu Wamphamvuyonse. Inu mwanapangitsa zinthu zonse kukhalapo mwa Mawu anu. Pa kuwomboledwa kwa anthu, Inu, Mulungu Wamphamvuzonse, Imu munabwera kudzera mu thupi la umunthu ku Israeli, Inu munafa m'malo mwathu chifukwa cha machimo athu ndipo Inu mudatiwombola ife. Mwa anthu onse, Inu nokha munamwalira, mudauka kwa akufa ndipo munakwera kumwamba. Ndipo tsopano, kuchokera ku kam’badwo kufikira ku kam’badwo, Inu mumadziwonetsera nokha kupyolera mwa anthu otchedwa aneneri kuti atenge miyoyo yathu kwa Moyo Wamuyaya mwa Inu. Inu mudakondwera kudziulula nokha mwa ine ndi cholinga chakuti ine ndikhoze kukhala wamnthenga wanu mu m’badwo uno wa Laodikaya. 3. Inu munanditumiza ine kwa Asilamu, Akhristu, Ahindu, Abuda komanso Ayuda. Inu munandiwonetsa ine kuti anthu adzabwera kwa ine kuchokera ku mafuko onse, zipembedzo zonse ndi zinenero zonse za dziko lapansi ndipo, tawonani, amuna anabwera kuchokera kulikonse. Ngakhale Amwenye, Asilamu, Mabuddha ndi anthu omwe sanakhulupirirepo mwa Mulungu akhulupirira mwa ine. Ndipo moposa kuukitsidwa kwa munthu wakufa, ine ndawona mipingo yonse ikukhulupirira mwa ine tsiku limodzi ndipo kulandira ubatizo wa kubwezera umene Inu munandiwululira kwa ine. Ndipo ine ndawalamulira iwo: Pitani kukafalitsa Uthenga uwu wabwino wa Mateyu 25:6 kuti apange amitundu onse akhale ophunzira anga. 4. O Mulungu, ine ndine kapolo wanu. Ine sindinasalepo kuti inu mundigwiritse ntchito mwamphamvu, muli Inu amene munandilenga ine ndiponso amene mukudziwa zomwe ine ndinapangidwira. Ndi chifuniro chanu chimene chiyenera kuchitika osati changa. Cholinga changa sikuti Inu mupangitse dzina langa kukhala lalikulu padziko lapansi kapena kuti dziko lonse lizibwera kwa ine kapena kuti Inu mundipatse ine kuchita zozizwitsa ndi zodabwitsa, koma ine ndikufuna kuti ndipulumutsidwe ndi onse omwe amanditsata ine. Inu, mbuye wanga komanso Mulungu wanga, pakuweramira pansi, ine ndaponya chipewa changa pa mapazi anu. Ine ndinali munthu wakhungu Bartimayo amene maso Ake Mudatsegula pa Epulo 24, 1993. Ine ndimachokera ku Rikédiba. Ine ndine kapolo wanu, ndicho chifukwa chake ine sindinayambe kuyenda pazoyala pansi pamaso panga chifukwa ine ndine amene ndiyenera kukhala mwala okwerera kwa osankhidwa. Prophet KACOU PHILIPPE
This song reminds me of my late brothers Chisomo Nsandu, Keith Miranda, Jesus Mkanda and Chikumbutso Malama....may your souls continue to rest well my brothers