Congratulations to this brother, m'bale ameneyi zingakhale bwino atapitilizadi maphunziro pamapetoko pake ndi kuchita ubale ndi anthu a business amene angamuthandize kumapanga zinthu zoti akhoza kumagulitsa kwa anthu ambiri. Popanda kuchita business sangapindule, koma kuti adalile boma kapena mabungwe azangochidwa, ama bungwe ndi a boma amangochedwetsa munthu ndi ma paperwork basi. #wesupport you bro.
Joab mwanayo Alindi luso tisanve kuti mwanayo luso lija lafa ai remember mbuyomu alipo anazapangapo airplane koma boma linakaniza kuyesa kumati ipha anthu ndiye timadandaula kwambili tili ndiana aluso koma boma limapondeleza so uku ndi kumulanje mwapitaku sizopondelezana ai Big up George
this interview is one of the many interviews made with him. I started seeing him kali kamwana than now koma he is still a village champion mpaka lero. Why Malawi
Joab i love your work , but can you please try to approach the government and ask them why we keep on wasting our own talent ? it was like the same with Kankwamba till the Americans saw his talent and gave him opportunity now maybe he might not come back to Malawi again. we should not repeat the same mistakes with this guy. we are talking about climate change and green energy this guy is a national assets but its up to the government to believe in our talent, if we send this guy to school and upgrade his knowledge its the National that will benefit from this. Government please help this guy
Good job bro komabe I don't get it pa mbaulayo kut pali connection lanji nkhuni ndi mota ilikupasiyo I'm still confused coz moto ukayaka ikuyenera kutetha beside those motors 🙆🏻♀️☺
@@joabfrankchakhaza okay chabwino ndimaganiza kut kuchepa or kuchuluka kwa nkhuni ndikumene kungapangitse heat kuchepa or kuchuluka mu Kachangu wakeyo kkk anyway he talented ife sitingakwanitse🙏
The boy just need some advice and support.. Otherwise to use a electricity to power mbaula and kugwiritsa ntchito nkhuni.. not a good idea.. Maybe magesiwo tizingogwirisa ntchito to power a stove, ti saver nkhalango..