Mr Ntanyiwa! Yes we might blame opposition parties pazomwe zkuchitikaz but on other side we might also blame ourselves as a malawians pomangotengeka ndzlizonse. Who changed the government is it APM or a Malawi? If yankho yake ili yot a Malawi ndamene anasintha government, so why we are busy now blaming APM kut akungoyang'anila? Kodi Mesa ndtomwefe amene tinkamunyoza APM akutiuza ife kut tisayelekeze kusintha boma koma ifeyo kusanva. Lelo akuvutika ndndan pakat pa APM nd ifeyo?
Penapake osamangotinamiza zilizonse n then the funny thing is ppl jst get convinced over everything .iwenso ntanyiwa ukakhala chete ppl can say akupatsa chibanzi,BT aliyense can hv his own decisions at the end of the day basi
Zoona Dan lu ndye kt za poison zija mwina zinal zonamat umafun usapite ku kovechoni ya dpp ija anal atakukopa a mcp yeti.why malawi wathu.ambuye chitanipo kathu chonde.
I don't see any reason i can blame Dan Luh. The money is too much and iyeyo ntchito yomwe imamubweletsela bread ndikuimbako. So, in this case i feel like Dan ali ndichipani chomwe akuchidziwa ndipo kumupatsa ballot paper lero akudziwa omuchonga yekha muntima mwakemo. Ukuku akugwilako ntchito yake yomwe amadyela. 500mk olo mukanakhala inu mukanatani? Big up bambo a Daniella. Iyaaa
Komatu sirius anthu simukugona kufufuza zimwe abomawa akupanga ...u really do your best informing the public but i think the only solution we have to this problem is voting otherwise kumangolankhula zizitipwetekesa mutu...
Koma abaleeeee????ine zikundisowetsa mtendere zikucitikazi,,atimanga mu jumbo ndithu,,anthufe kungokhala ngati zidole?? Anthu akudya nyika,zitedze,eish,,mfuti zawozo ziawombere okha ndithu in Jesus Christ name
A Ntanyiwa nkhani ya Dalitso Kabambe ine sindikuikhulupilila. Nkhani imeneyi ndiyofuna kugawa mavoti ku convention. Ma voti akachoka kwa Kabambe (amene akuoneka ngati akutsogola), MCP ikufuna kuti ma voti apite kwa manganya. Please investigate carefully.