Kutanthauza kuti onse andalewa ndi mbava zokha zokhadi,akuti iwonso ndi a corruption koma awa anyanya,ngakhale akunama,DPP ndi PP ndi zimene zinanyanya.
It’s not important. MCP is strategizing day and night. What strategies is DPP putting in place. Nothing. Pangani zoti opposition iwine chonde. Malawians need to freed from this turbulance .
Ndagwilizana Nanu. Navicha anakatithandiza. Km a Chaponda ayipwetekesa DPP akunva zomwe anzao akupangira, akutidoda koma a Chaponda angoonerera. A born kalindo, mthanyiwa onsewa akuyesera kuuzira mayeso kt mwina a Chaponda azuke maganizo km aaaaa mbola bola a Navicha akanayesesa.