To be honest Hot current iyiyi yaonetseratu kuti Brian and Jona, you guys are truly investigative Journalists... I like your courageous presentation because you have hitted a nail by head. Ya Kabwira komanso ya Extended Credit Facility ndiye mwaing'aluladi... Kuswa Kuswa, kugaza kugaza, kubandula kubandula. Kkkk kkkk kufotokoza nkhani osati based on speculations but facts on ground. The media has a very important role towards politics, rule of law and good governance. Guys you are a leading analysts in Malawi, so far😊😊😊😊😊😊
Jona is right I feel the same let's no t brame ma ministers president yu ndi is incompetent he has no sense of direction hence his appointment s are also poor... Good example is bingu He was sharp upstairs as results he had ma Ministers oziwaso chomwe akuchita
I remember tsiku lina pa Sana mu Lilongwe kunabwera Richard kungokhala mgalimoto akuti akatero amwenye amangotuluka kuzapeleka ndalama n day imeneyo anachedwa,komatu mzibambo anaulephera mtima watsika kukathira fire mkati muja,mungangondikhanzika panjapa ine,do u knw whom i am ine shaaaa🤔🤔🤔
Ine kwanga ndikuyamika chifukwa cha Tv imeneyi ya Times ndi Tv yokhayo imene imatithanndiza kuunikila zambuyo komanso zakusogolo, Pitilizanikutisegula mmaso ife achinyamata. vote UTM
Vuto la usogoleri opusa opemphapempha basi azibusa ndi kukhala kwao ndie ndikukhalaso nsogoleri wa ziko aah basi m'mitu mwake ndizopempha basi kuendeza church ndi ziko nzosiyana system yake so asakaniza ati ndi yofanana to be honest kwa chakwelayu zativuta kwambili more problems
Ngati a DPP akufuna kuwinaso must follow your advice and guidance another thing vice President must be Enock Chihana and Atupele Muluzi finance minister and next President agreement
Mesa a Dpp, amayimba Kuti lozani zanu, nde a MCP asalodze zawo, a Brian ndi Jonah pena pake mmakondela DPP iyaaaah, Simufunila Dziko lino zabwino, koma Mufuna DPP yanu yokupha Ma Albino, Ma black outs aja, Miseu yogumuka ija Aaaah, inu nga DPP basi komanso mwatatsa poti Wonder ndi Bayana Chunga palibe. Aaaah inunso mumakondwela ndi DPP yanu ija iyaaa ndipo simunati, Chakwera ndi Mpakana 2030 wooooo!!!!
😂😂ndinachoka ku south africa kupita ku bluenfornteen ,,,,k kkkk mesa bluenfornteen ndiye south africayo,,,ok koma abusa mumatinvetsa kukoma lets go!!!!
Ndalamazo nde zikumapezeka ku zambia,no one to be held accountable No arrest no nothing ......aaaaaaaash why malawi every thing looks like is falling apart instead of fixing the economy ali besy kutukwanana mumisonkhano aaaaaaaaaa fwiti iyo ili kulowa malawi i think njanakazi iwenge yanalume nthe yagowoka Lord come rescue us
To times .check what dpp says kumisonkhano yowo .amaloza zinthu anapanga ndi iwowo yet ndimitsonkho ya amalawi. Don't look one side here I think she is answer the dpp party. Onsewa angosiya zoloza zomwe zikuchitika zonkhudza boma. Or dpp isiye nyimbo ya lozani zanu