Тёмный

Interview ndi Norman Chisale 

Malawi Lovers 🇲🇼
Подписаться 24 тыс.
Просмотров 230 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

6 ноя 2023

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 374   
@frankiechasokoneza5802
@frankiechasokoneza5802 2 месяца назад
Komano pa point ya human rights Peter Muthalika he really respects
@mengokumwenda3832
@mengokumwenda3832 8 месяцев назад
The lady was carefully selected to handle this interview am impressed with how she has handled this heavy interview. Professional indeed
@aloisiocarlosantonio8365
@aloisiocarlosantonio8365 7 месяцев назад
😊
@RuthNankumba-ux3sw
@RuthNankumba-ux3sw 9 месяцев назад
Big up Norman Chisale ,I love your courage 🔥 Ambuye apitilize kukumenyeran nkhondo ,,,I'm one of your supporters
@NzeruDesign-ut1go
@NzeruDesign-ut1go 5 месяцев назад
Ndpo nthawvyamayankho ikubwela big tipanga zobwezera ntoporao
@JamesKamanja
@JamesKamanja Месяц назад
God bless Mr chisale komano mokupemphani ndithu pepani uyu akufuna kut mumukhululukileyu imvani kulila kwake kut ukulu wayehova ukhalebe pa inuyo yesu anat muwakhululukile chifukwa sakuziwa chimene akuchita Musaiwale kut munthu payekha alibe vuto koma satana akamulowa amapangisa munthu kuchita zimene choipa chili mwa iyeyo chikufuna please ndikuziwa ndithu ululu ndi ochuluka kwambili koma khululukani ambuye apitilize kukupasani moyo wamphanvu madaliso avumbebe kut wamasiye apeze popumila
@user-gz9iy7sd7j
@user-gz9iy7sd7j 4 месяца назад
Mr Chisale isn't my relative but ndawamvesa he is a real soldier, BRAVO CHISALE. BULL Sheet kayun.
@paulgodfrey3361
@paulgodfrey3361 9 месяцев назад
Leah you the best journalist...well done to Me Chisale
@hectortambuli605
@hectortambuli605 8 месяцев назад
Great man Norman Chisale. Oceans of luv to you and your family.
@Catherinesmart-xk4zx
@Catherinesmart-xk4zx 8 месяцев назад
Chisale ndimunthu wabwino kwambiri wamanga ma church wachita zambiri Ambuye akudalitsen achisale long live
@mijerimasiye7310
@mijerimasiye7310 6 месяцев назад
Azodiak tamakhalani ndi ma bottle amadzi mukamapanga interview ndi anthu please
@Extratremendouszeus
@Extratremendouszeus Месяц назад
Komadi man I support 😂😂😂good
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 8 месяцев назад
Chisale akumva zowawa chifukwa cha anthu ansanje but Chisale is the best Man in Malawi he spend his money to help the orphans and community, God bless you always and protect you Mr Chisale.
@user-or8cw6md7t
@user-or8cw6md7t 8 месяцев назад
Zoonad ol evn Ines zimandiwaw, km Amalawi if nsanje😢
@Homeofpeace321
@Homeofpeace321 8 месяцев назад
@@user-or8cw6md7t amalawi amamukonda munthu akafa, that's why dzikoli lili lobwerera mbuyo,
@AubreyKennethchingamba-gq6et
@AubreyKennethchingamba-gq6et 6 дней назад
Titakhala ndi anthu 20 nziko lino ngati Mr Chisale Malawi atha kusintha I proud of you Mr Chisale ndimakunyadilani chifukwa chakulimba ntima kwanu
@thomluciouss7360
@thomluciouss7360 8 месяцев назад
The one who talk the truth doesn't fear and it's really true that the truth pains big up Mr Chisale
@samaxodala7587
@samaxodala7587 8 месяцев назад
Am agree with you 💪
@blessedmichael5124
@blessedmichael5124 8 месяцев назад
I agree with you.
@user-nn5ug7ul4d
@user-nn5ug7ul4d 8 месяцев назад
Msilikari adzakhare msilikari mpaka kare. Big up bro N. Chisare❤❤
@matembanevermind-po3me
@matembanevermind-po3me 8 месяцев назад
Gud interview love you questioner and Mr interviewer Norman
@LetsSeePlaces43
@LetsSeePlaces43 9 месяцев назад
Interviewing a well trained professional soldier should be different with interviewing a well trained professional economist💪🏾💪🏾Bravo snipper Norman Paulosi Chisale🤣🎉🎉💥💥
@user-nr2th9wu6i
@user-nr2th9wu6i 8 месяцев назад
Chisale your number 1 well trained soldier
@user-ro7rb9hj8k
@user-ro7rb9hj8k 8 месяцев назад
😂😂😂 so in love with his courage 🤦🥰
@user-sx1gr6fz1s
@user-sx1gr6fz1s 9 месяцев назад
Akuzuzika ngati yesu chisare ndi Good Samaritan athu abwino amazuzika
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Месяц назад
Am watching this interview kachikenaso Norman Chisale yu ndi #1 kwa amene alipa chilungamo akudziwa kuti big wa ndi real man osangoti mwakati poti umadana naye.
@jumazabula2908
@jumazabula2908 8 месяцев назад
Definition of having readership, fire 🔥 chisale
@mordecaikachale2497
@mordecaikachale2497 9 месяцев назад
I like the energy tht u hv Mr chisale as a soldier...big up❤
@falayichitsotso5371
@falayichitsotso5371 8 месяцев назад
Mr Chisale I hear ur story it's very bad and am very happy with u ustand with God dnt give up mukuyakhula kwako mulungu akumva ndipo mulungu amalora Kuti ana Ake andutse mmavuto ndicholinga Choti ukulu wake ukaonekere God will be with u mwaiwe muli usogoleri
@user-zg7iw8kq4r
@user-zg7iw8kq4r 4 месяца назад
Bravoooo big man chisale i salute you
@Chief-Phungwako
@Chief-Phungwako 9 месяцев назад
This was nice chisale seems a good one though ndindale
@NodiceChakwala-tz5gg
@NodiceChakwala-tz5gg 9 месяцев назад
great mtolankhani , kip the fire burning girl
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 9 месяцев назад
Powerful talking and intelligent, proud of you @Norman Chisale
@henryhenry6632
@henryhenry6632 9 месяцев назад
Intelligent ya ku machende amalawi mapanga support zingawenga bwanji, kupusa
@yamikanijames6915
@yamikanijames6915 8 месяцев назад
Mukuyamikila chisale man? After all what he did now you're embracing his work.... don't you know people lost trust in DPP and one of the biggest reason ndi iyeyu
@LetsSeePlaces43
@LetsSeePlaces43 7 месяцев назад
People never lost trust with DPP...anthu tinanamizidwa kuti tizaona zabwino...pano misozi yatha mmaso yayamba kutuluka ndi misozi ya magazi chifukwa Cha bodza la CHAKWERA ndi chilima.
@Liam-ky5cu
@Liam-ky5cu 9 месяцев назад
Bravo Bravo 👏 😁 Soldier...
@ndalamaandrew
@ndalamaandrew 9 месяцев назад
Koma Chisale uyuyu eeeeeeh 🙌🙌🔥🔥🔥
@vitumbikocobysinyiza-5116
@vitumbikocobysinyiza-5116 8 месяцев назад
Big up Mr chisale
@user-pl5pg8fp8s
@user-pl5pg8fp8s 8 месяцев назад
Watching from zambia
@TwalikiWisiki
@TwalikiWisiki Месяц назад
Mr Chisale i understand your pain please please firgive him isbus for your own good, you saud you are Christian our master jesus taught us to forgive those who do us wrong before we ask to be forgiven
@maskinmsungeni8763
@maskinmsungeni8763 8 месяцев назад
Kkkkkkkkkk Norman Chisale !!!!! Ur a big Man. Wandiwaza kwambiri Msungeni all the way from Zambia.
@chifunirosaka9077
@chifunirosaka9077 9 месяцев назад
Soldier never die chisale more 🔥
@user-pr6fm8dp1e
@user-pr6fm8dp1e 9 месяцев назад
Mr chisale attitude in this interview shows kuti bambowa ndionama..😂
@magdalenachipeta2394
@magdalenachipeta2394 8 месяцев назад
Ndipo sukunama uku ndiwabodza auze mtundu wa a Malawi kuti ma billions a chuma anawapaeza bwanji osamangobwebweta zopanda phindu, kufuna anthu akumvele chisoni.
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Месяц назад
Ndinu mabulutu guys
@paulgodfrey3361
@paulgodfrey3361 9 месяцев назад
Your the best Leah
@williammaseko8542
@williammaseko8542 8 месяцев назад
He is very emotional and trying to run away from facing justice. No one accepts to be guilty in public and whatever is doing here is normal for suspects. 42years doesn't match with the way he looks unless he tells us kuti amasamba Nyanga.
@AcacioWilsonPhezula-t8l
@AcacioWilsonPhezula-t8l 3 дня назад
Wn am the of them amene ndimamva kuwawa ndikamva kuti mwamangidwa,sinakumane nanu ,sitinayankhulako koma zimkandiwawa koopsa
@user-lx8ow6ek6k
@user-lx8ow6ek6k 9 месяцев назад
I love you Mr noman❤
@lonjiekaselera9651
@lonjiekaselera9651 8 месяцев назад
The real legend khaaa wauuza ngamo
@chimwemwenkosi-nl4zj
@chimwemwenkosi-nl4zj 8 месяцев назад
True leadership timakunyadilani mr
@Discar_mw
@Discar_mw 9 месяцев назад
This was a hot 🔥 one lol 😂
@shupikayintuwaluwa-5899
@shupikayintuwaluwa-5899 8 месяцев назад
Kkkkkkk aaa zoona. Msilikali kiching, amba chilungamo n how he's feeling with de way they r treating him
@peterbyson6269
@peterbyson6269 3 месяца назад
respect to you both you building Malawi in this interview ..
@user-rz9cr2nu1d
@user-rz9cr2nu1d 8 месяцев назад
Big up boss
@blessedmichael5124
@blessedmichael5124 8 месяцев назад
I like sir Norman Chisale he's been good in speech osamaopa pa chilungamo
@paulmakaula4937
@paulmakaula4937 9 месяцев назад
Political prosecution has ever been in existence since our independence....please follow the rule of the law always! Clear conscious is the medicine...God is watching and will judge everyone right..
@user-zg7iw8kq4r
@user-zg7iw8kq4r 4 месяца назад
One thing i like this guy he talk straight
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 9 месяцев назад
Kkkkkk ayayaya malawi tingogulisa tigawane dollar zo
@user-wc4er3lc3l
@user-wc4er3lc3l 8 месяцев назад
Courage muli nayo...komano kusa kululukako kuchita kuoneseratu kuti muli ndi mtima wakupa
@happyzumatembo2174
@happyzumatembo2174 5 месяцев назад
😢 or uli iweyo kut munthu akunamizele mulandu wa murder. Uthakumukhululukira?
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Месяц назад
Sukudziwa chomwe ukunena, sukuona kuti Chisale amuzuza popanda zifukwa?
@user-qy6nj9ii6n
@user-qy6nj9ii6n 8 месяцев назад
This lady 🙌🙌🙌🙌🙌
@user-xb2dz8vo5z
@user-xb2dz8vo5z 9 месяцев назад
Tikukuvesesani mr chisale.
@MisheckChangata
@MisheckChangata Месяц назад
Great man ,i like u
@user-lc3sw8iz2g
@user-lc3sw8iz2g 9 месяцев назад
True leadership
@sainetjackson6183
@sainetjackson6183 9 месяцев назад
Chisale ndikatumdu🤗
@yamikanichakuluntha651
@yamikanichakuluntha651 9 месяцев назад
Kulavula Moto munthu wamkulu, Lord have mercy on him
@Johnybegood260
@Johnybegood260 9 месяцев назад
This woman is brave
@stanleykaludzu-bm4pm
@stanleykaludzu-bm4pm 8 месяцев назад
Brother chisale takumvani...Proud of you now.
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 8 месяцев назад
Chisale usatiuze kuti akhale wo opa mulungu suyo chakwera wo opa mulungu akutizunza
@user-xl6jq1zw5d
@user-xl6jq1zw5d 9 месяцев назад
This guy is some how mad
@pempherokatakwala6451
@pempherokatakwala6451 8 месяцев назад
Norman chisale iweyo ndi number 1 moto kuti buuuuu!!
@magdalenachipeta2394
@magdalenachipeta2394 8 месяцев назад
1986 he was already working as a soldier but he is saying is 42 years old eeeeeish!!! 😂😂😂komatu munthuyu akuoneka ndiokakala mtima mayankhulidwewa atha kupanga zoophsya. He is saying kuti ndiopemphela koma akuti sangakhululukile aSteven Kayuni 😭😭 chonsecho amayenda ndi bible , mawu a Mulungu mwamunthuyu mulibemo.
@AlexManuelMisomali-sv1vn
@AlexManuelMisomali-sv1vn Месяц назад
Norman your statement is clear and comprehensive but what about Chthyola, Chimwendo Banda, Kunkuyu etc ??
@user-eg9tz6jk8n
@user-eg9tz6jk8n 6 месяцев назад
Leah , bravo 💪
@JosephMussa-gz9co
@JosephMussa-gz9co 8 месяцев назад
Nice interview
@Dango79394
@Dango79394 8 месяцев назад
This lady, knows how to calm somebody. Mamuna wake anapata.
@user-ps3hn4os5e
@user-ps3hn4os5e 8 месяцев назад
😂
@ChifundoKadaleka
@ChifundoKadaleka 8 месяцев назад
Fire 🔥
@patrickjoda2165
@patrickjoda2165 9 месяцев назад
Mulungu akhale patsogolo basi Mr chisale Angoni
@chrisscapper-zw5rk
@chrisscapper-zw5rk 7 месяцев назад
Bravo Mr Chisale
@user-nj4ob8jw6y
@user-nj4ob8jw6y 9 месяцев назад
Akunama uyu, wakupha komanso wakuba, chitsiru chimangidwa chisiyeni, sakudziwa kuti apita kundende.
@AndrewBiliat
@AndrewBiliat Месяц назад
Big up Soldier
@abdulsalammkwepu3321
@abdulsalammkwepu3321 8 месяцев назад
Chisale🔥🔥🔥🔥🔥
@frazerbstaffwell5083
@frazerbstaffwell5083 9 месяцев назад
Wabodza iwe umakhala kukawale pa rent bingu akulamula unalibe kanthu unaba chuma bingu atamwalira ku state house
@user-rr3il1vg7f
@user-rr3il1vg7f Месяц назад
Eeeeeeeeee ai zikomo kwambili koma Mulungu arimbariyakhe
@thokojona9686
@thokojona9686 8 месяцев назад
Fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@user-fj3pw4gk5r
@user-fj3pw4gk5r 9 месяцев назад
Lea ndi makina respect
@SheenahMwalabu-iz3pr
@SheenahMwalabu-iz3pr 9 месяцев назад
Ndamva chisoni pokumva nkhani yanu bambo Chisale 😢 koma chilungamo chilipo ndipo momwe mwadutsa inumo enanso adutsamo ili ndidziko. Abale whyyy a police athu mmatero, olo ndiliineyo ndingaophwezetu ndipo ndikanamizilidwa ndimakwiya kuposanso achisalewo 😂😂
@user-md1fc6cu7b
@user-md1fc6cu7b 9 месяцев назад
Kma this interview must be repeated even pa wailesi , nice Leah keep on going more fire
@enipherphiri207
@enipherphiri207 9 месяцев назад
Chisale oopsya eeeee. Bible mmanja koma Bullshit pakamwa mbweee ashiii
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Месяц назад
Iwe umati atani? Uzaziona ukadzapeza ndalama
@kondwamlungu8384
@kondwamlungu8384 8 месяцев назад
Yeah azayakha zomwe amamangila Norman chisale
@user-ti2ct8ts8d
@user-ti2ct8ts8d 8 месяцев назад
Once a soldier always a soldier❤❤❤
@user-rd4lf2gg7g
@user-rd4lf2gg7g 9 месяцев назад
Tamva bwana Zina ndi Zina 😂😂😂😂km eeeee ai ziliko
@alexjeremanuel2541
@alexjeremanuel2541 8 месяцев назад
Haters will always blame you my brother just because all the enemies of APM can't be happy with your speech. Even the way this woman is interviewing you just shows that she is one of the haters because of this ( I feel bad and hate those ones who are blaming APM for useless things or political reasons and I handle him as my biological father) but no stress brother you're a real and very strong soldier and you're humble man otherwise stupid questions this woman was asking you if it was I, I would just fu....k off from that interview. Your character is a real good courage and discipline soldier and we love you and everything is going to be good
@user-sf4yy6so9m
@user-sf4yy6so9m 9 месяцев назад
Aaaa😮zaka 42 ndeine ndili 15 years 😂😂awa ngabodza
@Gorilla-k8e
@Gorilla-k8e 9 месяцев назад
😂😂😂😂😂😂😂moto kuti buuuuu L malekano umatimilila koma bwinotu akubandula mbakela bwana ameneyo 😂😂😂😂😂
@yilinase2905
@yilinase2905 8 месяцев назад
Wow!!
@user-cy1vf5vz8y
@user-cy1vf5vz8y 9 месяцев назад
🔥🔥🔥🔥
@charlesmaskia9695
@charlesmaskia9695 8 месяцев назад
I understand the Pain Chisale
@user-yg3hb7jh1q
@user-yg3hb7jh1q 8 месяцев назад
Keep it up Mr chisale
@kennedymzava
@kennedymzava Месяц назад
Your such brave boss
@johnsong7236
@johnsong7236 9 месяцев назад
chisale ndiozipopa mwachamba
@user-pn7cj9hb3t
@user-pn7cj9hb3t Месяц назад
Mwana wa njoka iwe kagwere kutali
@Bushiriderick811
@Bushiriderick811 9 месяцев назад
Interview without introduction 😂😂😂😂😂😂Lea be professional plz
@Chiso2019
@Chiso2019 9 месяцев назад
Ndipo ineso ndikudabwatu interview yanji yotero no introduction
@alfredbanda1693
@alfredbanda1693 9 месяцев назад
Kkkkk I hope akuphunzira adzitolera
@chifunirokachingwe3700
@chifunirokachingwe3700 9 месяцев назад
Pajatu anthu odziwika ngati amenewa introduction sikhala yofunikira kweni kweni, komabe as far as ma dos and don'ts are concerned apopo sizinayende kweni kweni😂
@kusalaphameya3421
@kusalaphameya3421 8 месяцев назад
i was riding in your ship until i took some time to regurgitate and i learn kuti amacheza naye ngati bodyguard wa Peter, his professional, and not as him as a person brian banda akucheza ndin Bushiri, 27th may times exclusive, followed the same lane yomwe anacheza ndi a Kapito pa 7th october anatero even yomwe anacheza ndi Dr. Joyce Banda
@Taonga0ngieKalua-yc6ok
@Taonga0ngieKalua-yc6ok 8 месяцев назад
Kkkkkkk ndipo etiiiiiii inuuuuuu iiiiii
@user-yh4qx6xq7u
@user-yh4qx6xq7u 8 месяцев назад
Komatu chisale ndye akumulakwla
@quintonmutume82
@quintonmutume82 6 месяцев назад
Dpp yangoyenera kubweler 💓💓🙌🙌
@nelsonkasim
@nelsonkasim 8 месяцев назад
powerfui mr chisaie auze
@mussachimtendere5555
@mussachimtendere5555 8 месяцев назад
We wl fight until chisale be freed
@chawagondwe6404
@chawagondwe6404 8 месяцев назад
Those who are saying bravo chisale you need special prayers..this guy stole our money tax payers money....he accumulated wealth within a short period of time....hotels cars houses etc he is backing himself apa he can't admit it.....and you are busy kumunyadira 😮Malawi ndife ogona too much.....he is lucky he is outside otherwise he belongs inside
@PetrosKachingwe
@PetrosKachingwe 8 месяцев назад
Once a soldier always a soldier
@Cee-H-Cee
@Cee-H-Cee 7 месяцев назад
Exactly
@user-zh9kb2sj2i
@user-zh9kb2sj2i 9 месяцев назад
Mbavaizi aaaaaa awonongachumachamalawikwambili
@wisdomluhanga
@wisdomluhanga 8 месяцев назад
Munthu ukulempera to forgive while holding bible
@chesterphiri7523
@chesterphiri7523 5 месяцев назад
Kkkkkkkk😂😂😂😂😂😂
@alfredbanda1693
@alfredbanda1693 9 месяцев назад
Leah try to write questions to be asked and kungoti bwana chisalewo amachita kokuwongoleranso plz plz plz interview opanda introduction aaaaaaa 😂😂😂
@Dango79394
@Dango79394 8 месяцев назад
munazolowera zoloweza, muziganiza.
@esthermasamba7423
@esthermasamba7423 8 месяцев назад
Ambuye Awakhululukiredi😢😢
@samaxodala7587
@samaxodala7587 8 месяцев назад
Chisale💪💪💪🇲🇼🇲🇼
@user-to4or4jw9g
@user-to4or4jw9g 9 месяцев назад
MCP ikazachoka m'boma idzazunzika kwambiri
Далее
CRUISE 5 WITH BYSON KAULA - DEATH ROW SURVIVOR
50:51
Просмотров 92 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH ULADI MUSSA
1:01:29
Просмотров 21 тыс.
кажется, началось
00:45
Просмотров 1,6 млн
Советы на всё лето 4 @postworkllc
00:23
ELA NÃO ESPERAVA POR ISSO 🥶 ATTITUDE #shorts
00:20
EXCLUSIVE: Malawi President - Bingu wa Mutharika
7:10
Просмотров 203 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH BON KALINDO
59:52
Просмотров 60 тыс.
CRUISE 5   ELIYA NZERU WILLIAM
1:20:13
Просмотров 387 тыс.
EXCLUSIVE INTERVIEW WITH MICHAEL USI (MANGANYA) Part 2
58:38
Zifukwa zomwe Brian Banda anachoseredwa ntchito
9:55
Просмотров 118 тыс.