SKC was a general fitter analibe kuyankhula za munthu koma maso ake anali ku dziko la malawi kuti lizakhare pabwino, now Usi amayenera kuwafikira a U TM amnzake powawuza za kusankhidwa kwake
Its unfortunate that UTM has not shown any excitement on the appointment of Dr M B Usi,however constitutionally he was the appropriate choice.Had Chilima won the presidency in 2019 Usi was to be State Vice President. UTM has just to accept the situation.
Usova iwe ndiwe ndani kumuletsa usi kusakhala vp wa dziko, why did the utm owner appoint him as his runningmate at first, leaving you with no any position in the party?
Nonse munakonza program iyi ndinu anthu opanda nzeru mukuonesakuti muli mbali ya mcp mumafuna kuti a utm akapeze ku parliament chosecho president wao wangoikidwa kumene m'manda, athaphedwa ndi mcp agalu kwabasi zikanakhala kuti zachitika mnyumba mwanu sibwezi mukukamba uchisiru mukukamba apau anthu opusa opanda chisoni
Inuso mphokoso kusowa zakamba position ndikuluza munthu malamuro ndichani zachamba et manganya amafuna Kare uvp Kare that way anamupereka chilima kwa mikangoyo mukusokosa kusowa zakamba
The truth is that SKC shoes are unfittable in all the alliance...and entire country leadership currently....but the country has to move forward.....ndale sizinthu zamuyaya ... it's about servanthood ... service to the people
Onse Ali apa ndi zitsilu , how Catherine be sitting and talking while the responders they say ,they are still mourning and it's true Malawian are mourning ndale zophana basi achewa opanda Pache inu
with UTM Dr Usi has failed as leader, he always sideline himself from his fellows, previously he dont associate with Utm members to please the president, even in this dark period he has failed to take a balance step by being to the part side & government side Usi has failed as a leader
Choyamba tidziwe kuti mu zipanimu utsogoleri umasankhidwa through convention nde kusankhidwa kwa usi sikutanthauza kuti ndi mtsogoleri wa utm. By the way the government could write aletter to utm based on their agreement to prove that the alliance is still valid. Koma kungotenga munthu personally uuùuuu it's clear usi si wa utm
Koma abale manganya angakhale wachiwiri wa ntsogoleri wa dziko mmmm dziko limafuna kutsogoleledwa ndi anthu a serious uyu anthu sangamunvele akapitilize ma drama
Ine Si wachipani Koma kunena zoona a usi akuziwapo chinachake pa imfa ya achilima chifukwa khope yake achilima atamwalira kumene iwo samawoneka wokhuzidwa ndi imfa imeneyi
No need for imposing Usi on UTM. Usi has been so slippery in UTM. Let him go and we shall see if he is going to survive in MCP. UTM Executive may opt to accomodate him but as for ordinary members its a big NO! Why this time? Where was he all that time when our dear president was alive? Zachibwana a ayi. Usi safunika. Apite akachite zake aone ngati angadzatione.
Koma anthu Inu muli ndi nzeru?a utm apita bwanji kukaombela mmanja ali pa maliro?Kodi malamulo ake amtundu wanji week sinathe ena ayamba ukuvina kulumbilitsana a Malawi?which means it was planned this b4 imfa ya chilima khalani ndi nzimu waumunthu eeti
Kusankhidwa kwa Michael usi wasatila ndondomeko yake chifukwa iye anali osatila wa the late SKC.komano tingodziwa kuti usi ali ku UTM kapena ali ku mcp?
Malamulo amanena kuti for 7days pasankhidwe munthu wina,,komaso sakanankhidwa wina koma Usi chifukwa anali vp wa chipani cha UTM,,so guys I don't know why we don't understand for this issues,,,we suppose to understanding because it's a rule,, it's not opinion for someone
It not alaw, kut you must choose the vice president wachipani, that is a trap iwe manganya akupasa zingati why you didn't have time to settle and see it with your utm people
Gentlemen plzzz lets take this issue very seriously. Dr Usi z not wrong kulandila udindo kapena kuti VP. Ndizoona kuti Dr Usi anayamba kukhala ndi boma more especially president of the republic kalekale komano chomwe tingadziwe ndichakuti even The laye Dr Saulos Chilima adali pafupi ndi boma more especially to the President of the Republic. Now gents if u digest all of these it means these pple r wel organised coz they both take one step at a time. Now lets not talk a lot of things when its not time to do so. Time will tell whereby will will proof Dr Usi that is a member of MCP or He z still with us in Almighty UTM.
Choyamba tiwunikile Kaye kuti Kodi chakwera poziwa kuti usi ndi vice president wa UTM anawawuza za appointment ya usi? Ngati adatelo ndiye a UTM analakwisa kusapita koma ngati sadawauze za kusakhidwa Kwa usi adachita bwino kusapita chifukwa usi wangokhala vice president wa UTM koma ndi member wa UTM,executive ikanaziwisidwa mwa dongosolo and then invited kukalumbilitsa vice president. Nde anthu musamangofutsa mafutso mwina mufutse chakwera yo. Ndamene angalongosole momwe adayendesela ndondomeko yake.
Amalawi let's move on zinazi tichedwa nazo mulungu salakwisa kodi amalawi mpaka liti tijusungabe mangawa look at APM for not accepting the fact someone is ruling now aaaa moti a UTM amafuna kufunsidwa maganizo pomwe thawi yochita appoint veep itakwana and azichedwa ndizosangala munthu mmmmmm. Malawi my country learn to accept God's plan
Manganya iwe ndiwe yudas chitsiru chachabechabe ndiwe unagulitsa chilima kamutu kako choka apa mzako wafera pomwepo basi iwe ukhalapo wapereka picture bwanji ku anzako a utm?u was vice to chilima who was killed by mcp tundalama tumene akupatsato tukutipitse mimba garu iwe no longer ku utm
Dziko La malawa amipingo ndamene anasokoneza ndi athila kuwili amasokoneza athu iwo ananena sakhani tsogoleri asakha akubweraso mwasakha thawi yolakwika kkkk koma guys mavuto Eni Eni and manganya anali wachiwili kwa wachiwili anayenera akhala iye kaya😢