I think Chakwera he must resign guys because he lie to us us a Nation He give us a long information about the death of Chilima He didn't speak the truth on the whole sanga that been happening
Nanunso chotsani Ndale za Udani,be more civilized. Chakwera has nothing to do pa Ngozi ya Ndege yomwe yachitika ku Malawi. Remember at first zimamveka kuti Chakwera force Chilima kuti apite ku Maliro ku Mzuzu kenako MDF ndikudzalongosola zonse momwe zinakhalira nthawi yomweyo Adani a Chilungamo ndikudzasintha Tone. Tiyeni tiike kuopa Mulungu pa TSOGOLO.Tsikulina we will be answerable pa zomwe tikulankhula ndikuchita pa Dziko pano. Mulungu akuona
Jane Assah ananena kuti a MCP anapita kunyumba kwake kukamuophyeza kut akapanda kuwina pa yenda mwazi.People never believed her but today see what they havee done to our Chilima
Munthu wanzeru zake akamvere iwe munthu wakuti sulikuno, umbuli uwu, black box imatengedwa ndi eni omwe anapanga ndege, nobody else muziwanamiza ma cadet anzanuwo achisiru inu
Koma inuyo muli ku joni ndiyeno mukutiwuza kuti tipite ku mademo mmmm iwe awuze abale ako ayambise mademo popeza ntchuma amadya ndi anthu andale ife tifele zayeni
Time. Everything has the right time. Speak truth, and if you can defend it, stand ready to defend it with evidence. These videos will surely speak in your defence if at all they contain truth.
Big boss you have freedom to tell as what you know osabisa pano wina aliyense chakwela sakukondwela naye chakwela is fack man munthu oipa kwambili ndiponso mulungu amulange kapolo ameneyo wapha chilima noh kubisa pano we will fight with him kut tikhale ndi freedom yabwino atill end of life
Kusankha kukhulupilira zonama kusiya Dala Chilungamo. Wake up MALAWI tisamapusitsike ndi phokoso akuchita Anthu ngati awawa ndi ZOPANDA nzeru izi. Winnie Nyondo anatulutsa Uthenga omwe Chisomo Chimaneni anamutumizira pa nthawi ya 10 : 10 AM kulongosola za Nyengo yoipa inaliko tsiku limene lija. Ine ndi wa UTM koma za uchitsilu zomwe CHITSILU ichi chikulankhula mmmmmmmmmmm I can't and I will never buy.
Chilima has become another God in Malawi and Malawians can not manage him, nkhani ya chilima azangoipondeleza ndikuwapatsa chi banzi alipansogolowo😢😢😢😢
Following closely until full information is shared & our action as malawians is required. Black box tiyiwone and hopefully, the data shouldn't have been tampered with by then .... Mawa following live kunonso
Zikuonesa kuti a DPP mukuziwapo kanthu zaimfa ya SKC chifukwa ma propaganda Anu awonjeza agalu inu mutu ndi mphuno zonyasazo agalu inu, Chakwera amumenyera nkhondo ndi Yehova, mukuopa kukamuchosa pa vote mwayamba kukamba zopusa
Where is Timothy Mtambo? Amene anathandizira Chakwela kukhala president, come and speak you devil 👿. Munthu oyipa mtima unaphesa anthu ndi kuwonga katundu wa anthu chifukwa chofuna kuikapo pa upresident Chakwela. Panopa aMalawi azindikila kuti Peter anali gentleman komaso akadali gentleman. Safuna ziwawa.
Zikhale akapitilize kugulitsa kaunjika...kunkuyu akapitilize zake za ulonda....Chimwendo akapitilize ulimi w fodya...enawo akudziwa komwe anachokera!....
Ndiyambitsa Boko halamu ya Ku Malawi apapa ndaona kut Malawi mfuti munasephana nayo ndinali Ku Afghanistan kophunzila sniper since 2002 ndaphumzila zambili zimene olo n'silikali wakumalawi sakuziziwa ndiphulisa mutu wa chakwela any time a Malawi osadandaula Umu ndi Mene wayakhulila nsogoleli wa gulu la Boko halamu wa kuno kumalawi
Chilima musiye apume mumutendele. Inuyo ngati mujambula tumizani zinthuzi tiziwone zomwe amachotsa blackbox. Ndiponso ukunama donier kampany inatha coz was declared bankrupt. So to which Donier company did you write the later to? Some of us are well informed Sir, unlike a malawi enawa omwe amakhulupilara bodza.