Тёмный

Kuyakhula mosaopa Chakwera wamupha Chilima. Chifukwa cha udindo 

Jay Kawere Mw
Подписаться 14 тыс.
Просмотров 38 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

23 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 214   
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i Месяц назад
Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py Месяц назад
Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa
@DorrahBanda
@DorrahBanda Месяц назад
Zoona
@LamieTiger
@LamieTiger Месяц назад
Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako
@MercyKachenje
@MercyKachenje Месяц назад
Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too Mulungu apitilize kitiululira zinsisi
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa
@user-iu6mr5xu6r
@user-iu6mr5xu6r 2 дня назад
Cilungamo madala. Dziko la Usi ndi utsi basi. Onse woipa amafuna anthu aziti ndi abwino. Mtima onyenga ulibe maciritso.
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem Месяц назад
Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo
@OsmanBakali-s5x
@OsmanBakali-s5x Месяц назад
💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭
@paulinekayuni1621
@paulinekayuni1621 Месяц назад
As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
@InnocentMlowoka-ew4lo
@InnocentMlowoka-ew4lo Месяц назад
Chilungamo kuwawa
@GiftKananji
@GiftKananji Месяц назад
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
@VeronicaChirwa-ct4os
@VeronicaChirwa-ct4os Месяц назад
Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
@manfredzalirabetha2440
@manfredzalirabetha2440 Месяц назад
Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
@mariamahamadu8402
@mariamahamadu8402 Месяц назад
Nawoso mayiko usi mbusi yamunthu kukonda ndalama kumeneko mpaka kulolela Kuti munthu ampedwe ndalama abale God bless you mukutidzegula mithu
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du Месяц назад
Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢
@PaulMinofu
@PaulMinofu Месяц назад
On point❤❤❤❤
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Месяц назад
Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera
@ibrahimalfred6539
@ibrahimalfred6539 Месяц назад
The power of massage and the power of prayer indeed
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 6 дней назад
❤❤ that's why ndinasiya kumvela ma radio station akumalawi
@user-yo9rw8tr4s
@user-yo9rw8tr4s Месяц назад
Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile
@ChimwemweBottomani-hc5ju
@ChimwemweBottomani-hc5ju 28 дней назад
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
@ThomasKaphwiti
@ThomasKaphwiti Месяц назад
Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅
@samueljuma4452
@samueljuma4452 Месяц назад
Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka
@isaihmagani5697
@isaihmagani5697 24 дня назад
Nde ngati mayi ngaku Zimbabwe bambo ku Malawi tinene kuti simu Malawi? Bodzatu inu
@Hellenistic109
@Hellenistic109 12 дней назад
Kkkkkkkk
@cacksygustarf6260
@cacksygustarf6260 Месяц назад
Voice ya nzeru❤
@YusufuKaifa-fr4wt
@YusufuKaifa-fr4wt Месяц назад
❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out
@ruthkundwe7448
@ruthkundwe7448 Месяц назад
Yesu anapelekedwa chifukwa cha ndalama yochepa,God have mercy
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du Месяц назад
Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢
@Hellenistic109
@Hellenistic109 12 дней назад
Ndipo Mapwala Ake Zoona 😢😢
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 Месяц назад
Mulungu akuona zonse,,, ndipo samagona tulo. 😭😭😭😭😭
@ThomasKaphwiti
@ThomasKaphwiti Месяц назад
Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢
@user-mw3kj4qz7b
@user-mw3kj4qz7b Месяц назад
It's true my brother that's sad
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s Месяц назад
Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu
@user-er7ub4ug7y
@user-er7ub4ug7y Месяц назад
Osaopa osafooka tiime pa chilungmo dziko lino nditose ndopo mbendera yake ndiii🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼situkukuopami😢😢😢😢
@LovelyBlini-cu3iu
@LovelyBlini-cu3iu Месяц назад
Mau amphamvu
@GodisoneNoel
@GodisoneNoel Месяц назад
Zoona ❤❤❤❤❤❤❤
@HameedahMasambuka
@HameedahMasambuka Месяц назад
Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm
@user-jn2oc3cn3q
@user-jn2oc3cn3q Месяц назад
Kkkk km support iyi
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
​@@user-jn2oc3cn3qkkkkkkk kwachema
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
Chilungamo chiyende ngati madzi 😂😂😂
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 Месяц назад
Inu ndiye mwanena zoona brother mmmmmh ulemu wanu Inuyo shaaaa Ndamva nanu kukoma zedi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@MtokomaYohane
@MtokomaYohane Месяц назад
And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions
@FelisterNgwira-op7rr
@FelisterNgwira-op7rr Месяц назад
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
@BensonChilundu
@BensonChilundu Месяц назад
Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu
@FrynessMoyo-to2du
@FrynessMoyo-to2du Месяц назад
Amalawi ndi amantha size😢😢😢
@user-gk6bf7xe9g
@user-gk6bf7xe9g Месяц назад
manganiso anu ameneyo okay alibwino
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 Месяц назад
Ambuye tipheleni Chakwera 😂😂😂😅😅😅
@Hellenistic109
@Hellenistic109 Месяц назад
AMEN 🙏
@AmandaConstance-fx8cr
@AmandaConstance-fx8cr Месяц назад
Not all days are Sundays God is watching and may there souls rest in peace 🙏
@CatherineDesire
@CatherineDesire Месяц назад
Chi Michael usi manganya that why amuika pa mpando iyeyo kuthamanga kukakwera pa mpando pakamaso gwaaaaa manganya
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma Месяц назад
Koma izizi tu we are praying kuti Mulungu alange aliyense amene anatenga gao lokupha chilima pompano asadikile chiweluzo
@mollymasangano473
@mollymasangano473 27 дней назад
Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e Месяц назад
Zoonadi manganya ndi munthu oipa sanayakhulapo za imfa ya chilima
@CatherineDesire
@CatherineDesire Месяц назад
Sanayankhuleponso amangophwisa mkhutu wa udindo usi
@user-mw3kj4qz7b
@user-mw3kj4qz7b Месяц назад
So heartly broken dear
@Aisha-db6ds
@Aisha-db6ds Месяц назад
Iponden fadah 🎉
@Pangolinimw
@Pangolinimw Месяц назад
Zoonadi inenso ndikusiwa cho cho
@LoveHawabwa
@LoveHawabwa 29 дней назад
Inu mwayakhula mawu ife tikuwopa kuyakhulapo mwatilakhulira mulungu awakanthe kopotsa
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa
@ackimChiumia
@ackimChiumia Месяц назад
U are talking sense
@georgejere2922
@georgejere2922 Месяц назад
You will pay for it, what's wrong did our SKC do to you😭😭😭😭😭 the day will come 😢😢😢
@MichaelWilliamsNyirenda
@MichaelWilliamsNyirenda 25 дней назад
Powerful message Duuu may their souls rest in peace ✌️
@Mervic-vm8eo
@Mervic-vm8eo Месяц назад
Osawopa osatopa osafooka 💪🔥🔥🔥
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Месяц назад
Enanu mudakangosiya kucommenter Ngati sizikukumvekelani bwino Ife nde tikumva kusekemela chipepeso chathu timachipeza kuzela kwaanthu amenewa chilima wathuuuu tizamfela
@Sabina-hw4js
@Sabina-hw4js Месяц назад
Ndi Ana omwe akudziwa
@EllinaBitto
@EllinaBitto Месяц назад
Osaopa osafooka tizafera mbendera yathu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@user-ml8lk9dr7t
@user-ml8lk9dr7t 26 дней назад
Yes may God perform wonders that the truth must prevail
@user-uv5rf4zt5q
@user-uv5rf4zt5q 24 дня назад
Chilima anaphedwa chifukwa cha jealousy eishiii Malawi will never change for better.
@MirajiYusuf-vx5ux
@MirajiYusuf-vx5ux Месяц назад
Zoonadi brother ife tikulira ndithu esh infa ya chilima mmmm😢😢😢😢 mulungu 😢😢😢😢
@user-rk4ch1ly3z
@user-rk4ch1ly3z Месяц назад
Iwe ndiye walasa!
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i Месяц назад
Zoona awa ndiye mau bro end I love you so much brother ❤🎉🎉
@WellingtonHowahowa
@WellingtonHowahowa Месяц назад
Basi poti kulibe mulandu okupha ndimphezi ...mudiyeni chakwelayo azasowa omusumila
@Trancy-xt4py
@Trancy-xt4py Месяц назад
Atola khani afikapodi apasidwat ndalama kut akhale chete ndipo mulungu agwesere mulili mkabudura mwawo Kuti zokozera zawo zinyenyeke kuti AZIWE phamvu ndiukulu WANU mulungu wanga chilimat sadakwake ,osalakwq kwambili ndiuyu chakwerayi
@user-do2cs8nf4b
@user-do2cs8nf4b Месяц назад
Komad manganya anatidabwitsatu palibe chimene anayankhula pa za imfa ya Chilima an angokhala pheeee ngt sizikunkhudza zombvetsa chisoni kwabasi Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse
@CatherineDesire
@CatherineDesire Месяц назад
Eyadi ndemweyooooo
@KhwipsFilm5050production
@KhwipsFilm5050production 22 дня назад
Kkkkkkkkk ati ufiti wazaza pa danzi
@user-qn8ey6pq4c
@user-qn8ey6pq4c 19 дней назад
🙌🙌🔥fact papa
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 18 дней назад
Achakwera azasowa mtendere mpaka liti pa imfa ya achilima garu wamkota sakandira pachabe God will judge about this 1day is 1day
@Marymahendra
@Marymahendra 26 дней назад
That’s true brother if it was khozi ya ndeka suit no trousers no shoes my
@lyiemanganjira9708
@lyiemanganjira9708 Месяц назад
Ili ndi pemphero la Ana a Mulungu,, ndipo akuona ndi kumva msozi wa aliyense... Mudzalira nonse munatenga gawo pa imfa Ya anthu amenewa 😭😭😭😭
@YamikanChirwa
@YamikanChirwa Месяц назад
Ndpo mabala akutiwaw
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
Manganya umuziwe yesu ndiukachenjede wakoyo kupusa kwako Michael usi Mzimu wa chilima ukusate ndikukantha kwambiri
@paulphiri-fz9me
@paulphiri-fz9me 24 дня назад
Well spoken my brother but Michael usi ndi mfiti yoipa ameneyu 😢anandiphera munthu wabwino
@user-so7wg6ii5m
@user-so7wg6ii5m 26 дней назад
Bambo inuo ambuye akutetezeni mwayankhura mau amphamvu kwambili ndipo mizimu yanthu amene anamwalira pangozi imeneija iwazuze achakwera komaso onse amene anatenga po gawo ambuye muchite nawo
@InnocentnMbale-zq8pk
@InnocentnMbale-zq8pk Месяц назад
Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
@NaomieBanda-t6g
@NaomieBanda-t6g Месяц назад
Ndava chisoni
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Месяц назад
Yes ambuye atithandize abale eesh💔💔so sad
@jamessheki4293
@jamessheki4293 Месяц назад
Iwe ndiye munthu, Malawi tulo anthu kutipusitsa chonchi,tingoyang'anila ngat nkhuku mkhola ikaphedwa imodzi zina zimangoyang'ana. Mmmmm
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 28 дней назад
Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..
@AbnormalMk
@AbnormalMk 26 дней назад
Nkhani ya Straight 200%
@FelixBoss-yn9pe
@FelixBoss-yn9pe Месяц назад
Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man
@PraiseCedar
@PraiseCedar Месяц назад
Unali bho koyamba kuja koma zalowa nsanje kwinako
@ChilangoNdalama
@ChilangoNdalama Месяц назад
@AjudantFombe
@AjudantFombe Месяц назад
Mudziwa bwanji chilungamoa Malawi ambili ndi osaphuzila ndipovuta
@user-gi1gh9ry6h
@user-gi1gh9ry6h Месяц назад
Zoona anthu oyipa kwambiri magazi alimanji mwawo 😅😅😅
@NoelLangwani
@NoelLangwani Месяц назад
Ndipoh zoonadi mwalakhula bwino ndithu broz man
@user-wl4nd7ic1s
@user-wl4nd7ic1s Месяц назад
❤❤
@MabvutoMichaelPanagona
@MabvutoMichaelPanagona Месяц назад
Bambo ndithu mwapeleka mitu akanakhala kuti amawelenga kapena kumvela ma media mwina akanaphuzira zina
@HopeSaka
@HopeSaka Месяц назад
Mwatilankhulila father 😢😢😢
@SolomonNjolomole
@SolomonNjolomole 22 дня назад
Ndipo sitinganamizidwe zoonadi anena braz zomvetsa chisoni.
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 Месяц назад
Ndifiti Manganya mwana oyipa kwambiri chisilu chamunthu ichi galu kwabasi nkhankhankha uyuuuuuuuuuuu ndimapulani awo opusawo abvutika okha mitima mwawomo
@harrisbanda5891
@harrisbanda5891 Месяц назад
Kulankhula chilungamo mopanda kuopa
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 28 дней назад
Ameni amen misonzi ya wanthu osalakwa simapita pachabe
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 19 дней назад
Ndipo inu😢😢😢
@SebastianSauwa
@SebastianSauwa Месяц назад
Akuopa kumangidwa
@TressLuka
@TressLuka Месяц назад
Nkhaniyo ndiyonaaa kapena 😂
@juniortsegula3847
@juniortsegula3847 17 дней назад
😂😂 powerful msg
@user-wl4nd7ic1s
@user-wl4nd7ic1s Месяц назад
🔥🔥🔥
Далее
would you eat this? #shorts
00:23
Просмотров 1,9 млн
Викторина от МАМЫ 🆘 | WICSUR #shorts
00:58
would you eat this? #shorts
00:23
Просмотров 1,9 млн