As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo