If what is being said on Limpopo FM is true,then Chakwera has no right to continue running the affairs of Malawi. By now ,he was supposed to be out of state house.Malawi get united and replace Chakwera with someone who is ready to lead Malawi with passion. The kind of politics is exposing are of olden days. People must not wait for 2025 to vote out mcp just deregister this political party if what is reported on this platform is true.(My Opinion)
Du u think is this is true bro? If it is true, how came this people are says this to day cos chilima has died while all this days amamunena chilima-yo? Don't trust this bro......
Ineyo ndikanakondano a Malawi tikanasiya kumangodandaula koma osapangapo ma actions izi ndizomwe amationelera nazo Action is what supposed to be taken than kumangodandaula pamene maumboni okwanira Malawians please lets woke up and take ma actions Please!
Mkulu wanga pitiliza kuvumbulutsa china chilichonse.Vuto maboma omwe tisankha masiku ano amatitenga ngati zitsiru zawo koma tsopano adziwe kuti tinasukusula kumaso ndipo china chilichonse chikhale pa mbalambanda.Mr Comrade,ndakuvulilani chipewa ndipo pitilizani kuphulisa mabombawa.Ndafunanso kukulimbikitsani kuti menyani nkhondo kufera abale anu kuno kumudzi omwe akuvutika ndi chipani cha congress chomwe mtsogoleri wake ndi Chakwera
See gone are days when Malawi was blind. Gvt must know that today they kill one but tomorrow ten will rise against you and you kill ten tomorrow the next will come hundred unti everyone become your enemies.
The people surrounding the president didn't advise him correctly because of their selfishness!. They shouldn't have advised him to stand for the second term after signing an agreement. They would have changed the constitution to suit the agreement.