Chakwera ndi wakuba, kusawukitsa dziko kuti anthu a m'dziko akhale ngati opempha polandira zithandizo zake pomwe Ali wakuba, wakupha, Mizimu igone ku malawi congress pate and tiyeni tiwonelere chisangalaro cha satana kunamiza anthu ku Balaka pomwe akudyetsa Kasiya yokha, Shame to u Mr Lazaro😢
You deliberately forgot that you are the same people who remove DPP and UDF and you said APM failed to govern you and now you want APM and Atupele to do what ?
Koma akunama awa olo angawe chimanga chawocho anthu olo ali osamva koma apa amva kuti akubwera ndikunamaso komanso mr tanyiwa mumanena nthawi ndi nthawi
Big mmalawi sazatheka sitichedwa kuyiwala ife wolo muthayakhula motani koma mukutimasula ndi kutiwonetsa koma chimanga chimenecho chikangopelekedwa ayamba yemweyo
Inu manyaka osewa ndi opposition party palibe yemwe akuwoneka pa ground pano opposition yose ya makape sakusiyanaso ndi MCP amandinyasa a opposition nawo
Just you go and be the opposition so that things will be working according to how you like because you're the same people who voted for Chakwera and now what you want opposition to do for you ??