Chakwera akudziwa bwino za zigawenga Zomwe zimatumidwa kuti zizikhapa anthu azipani zina, watero Lytone Mangochi.
Zigawengazo zimapatsidwa ma K30,000 ndimunthu wina wamkulu mimba wa MCP.
Ndi chifukwa chake Chakwera salankhulapo kena kali konse.
Lytone Mangochi wati sakuwopa imfa ndipo adzafera ufulu wa a Malawi.
#malawi #foryou #southafrica #everyone
21 окт 2024