Uyu ndi satana weni weni ife anaphedwa aja si abale athu koma nafe tikulila isiku ndi usana ndipo mulungu ngati akuiona misozi yathu achitepo kanthu ndithu, anapha anthu osalakwa 😭😭😭😭😭😭😭
Anthu amati peter ndi woyipa mulungu ndi wabwino chifukwa amalawi akuziwitsani munthu wabwino ndi oiyipa amalawi ndi anthu wosayamika peter amalakwa chani lerotu ndi izi
Zowonadi chemwali sumukunama achoke ndipo akundinyasa ndikamamuwona A MCP anagwila Mbuzi ya Agogo anga nthawi ya Kamuzu ndi makumbukilabe ine a yuth ndimakumbukilabe maina mpaka sindimayiwla chipani Cha nkhaza ichi