God have mercy please Ana Ana kumaphala chochi makolo awo alimoyo zoona kumangoziwa kubeleka bansi afunika afunika chilango makoloso nawoso bushiri thandizani apa please 🙏 anawa awone kuwala pa town
God bless you brother man it's not easy... Bambo wa anawa komwe aliko adziwe kut azawafuna anawa tsiku ndi limodzi Mulungu simunthu.. God bless you more
Eshhh💔 kom anawa akukhala moyo ovutika kwambili ndisaname nditaonela video yii ndalira mumtimamu Plz ku bomako athandizeni ganyu yomwe akugwirayoso mmmm ayi sizoona abale, We all human beings let's assist each other while we are still live.
Zandkhuza kwambiri ndpo ndalira kwambiri ndakhuzika, anthu ena akusowa ana ,ena akusiya ana opezeka kale why god, mulungu chitanipo kanthu kwa ana awa yehova muwonesere ukulu wanu kut tikuziwen kuti inuyo ndi mulungu amene simulephera