Тёмный

MICHAEL USI LERO WAKAKAMIZIKA WAYENDA NDI MKAZI WAKE KU MWAMBO WA CCAP OMWE UKUCHITIKA KU LILÔNGWE 

Makosana
Подписаться 116 тыс.
Просмотров 36 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

28 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 55   
@MarkoChikoko
@MarkoChikoko 2 месяца назад
But VP akupangisa akazi awo ngati achilendo, beautiful couple
@GoodluckVithumbiko
@GoodluckVithumbiko 2 месяца назад
sopano zodabwisa kwambiri zamapemphero kuretsa kujambura zovetsa chisoni mwakhara ngati muri ku zachipani za yesu zimenezo kukaniza anthu zaziii
@ChisomoMsiska-oi2vg
@ChisomoMsiska-oi2vg 2 месяца назад
Koma awusi akumulakwira nkazi wake bwanji akumuchitisa manyazi ndi nkazi wokongola kwambiri bwezi akumayenda Naye azizolowera nanga
@DavidPhiri-o6w
@DavidPhiri-o6w 2 месяца назад
I love you my Vice president
@SophinerWilliamFrank
@SophinerWilliamFrank 2 месяца назад
May the good lord guide in everything, blessed event
@MsondaBanda
@MsondaBanda 2 месяца назад
Mwachita makola kuzilekeska izo zikujambula na maphone za maboza
@FathimaMaulana
@FathimaMaulana 2 месяца назад
Munthu aima ndi mkazi wake komatu mpaka gap ya 2 meters 😂😂
@MathewKalinkhu
@MathewKalinkhu 2 месяца назад
Mai wokongola kusiyana ndi a mrs. Chakwera a nya Gondwe, 😂😂😂😂😂😂, eish! Kukhala ngati anachi kuwapatsa a Chakwera mkazi.
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo 2 месяца назад
Kkkkkk angosinthana akaziwo
@iangondwe6857
@iangondwe6857 2 месяца назад
more fire vice president
@YunusuABdullah-e7g
@YunusuABdullah-e7g 2 месяца назад
Michael Usi ndi Galu kwabas zichani izi..aaaa anasowa zochita awaaaa
@stevenmakwinja9648
@stevenmakwinja9648 2 месяца назад
Kodi mai Skono mawawona?
@RK-xw1of
@RK-xw1of 2 месяца назад
Mmmmm HHhH anthu muli pa ntchito yoposaso yolembedwa bwanji osamangogona kkkkkkkkk
@MaxonKambazithe
@MaxonKambazithe 2 месяца назад
Kuima ndi mkazi wache bwanji
@RitaBan-t7c
@RitaBan-t7c 2 месяца назад
Kkkkkkk komatu ziliko mpakana kukaniza kujambula mukuopa chani mbanva iziiii ndiye ndakujambulani kaye kungoona kuti mutani😅
@lawrencemakina2882
@lawrencemakina2882 2 месяца назад
Mkuluyu mene akuyang'anira mmmm anachenjeresesa
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo 2 месяца назад
Kkkkkk akungoti cheucheu ngati wakuba mwachiona
@juliussamson6212
@juliussamson6212 Месяц назад
PANYAPANU USI
@ShearstonNyirenda
@ShearstonNyirenda 2 месяца назад
Takunyadilani avp
@Jele-mk9ip
@Jele-mk9ip 2 месяца назад
Si Kembo Mohadi winayo?
@MiddayDeleza
@MiddayDeleza 2 месяца назад
Koma ma church nde akuhongedwatu, dziko lapansi ndi anthu ake mmmh
@GoodluckVithumbiko
@GoodluckVithumbiko 2 месяца назад
kuti muremekeze azi busa ndiye ana chakwera nanuso ac.c.a.p ndarama zikuphani ambuye akuyendereni ndithu
@CatherineDesire
@CatherineDesire 2 месяца назад
A VP Ngati Galu WA 😇
@smartjilamu8026
@smartjilamu8026 2 месяца назад
Dzoka lawina ndi mwai wawina😢
@RaphaelKweve-u5s
@RaphaelKweve-u5s 2 месяца назад
Nanuso mukumatumiza zopusa bwanji nanga pali chani apa zojamula mdi ka phone ka 8 Gb
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 2 месяца назад
Wanda ndamake sikono😮😮😮
@WilfredMwale
@WilfredMwale 2 месяца назад
Madam moni kumangowasemphatu
@MarkoChikoko
@MarkoChikoko 2 месяца назад
A VP ndipamene akumupepelesa madam.
@EstherZintambira-sq3yy
@EstherZintambira-sq3yy 2 месяца назад
Sakuwaziwa anthu haha
@StoneckJali
@StoneckJali 2 месяца назад
Jelasi
@YellowmanMalawi-qe8zh
@YellowmanMalawi-qe8zh 2 месяца назад
Usi wa mcp leave us the Utm alone
@BFWCPHIRI1978
@BFWCPHIRI1978 2 месяца назад
UHule onse uja tere uli ndi bomba kan?
@JustinChilinda
@JustinChilinda 2 месяца назад
Koma izi palibe chazelu ndatolapo yesan kumalanga post zinthu zot tikhoza kuvako Za zelu
@SoldierWilison
@SoldierWilison 2 месяца назад
Ngati bonza MN kungo tithela madata
@SteviePatrick-g2p
@SteviePatrick-g2p 2 месяца назад
Uthenga wa ndioy chan pamenepa omwe ungatipindulule ife anthu
@BrianAmbeswa
@BrianAmbeswa 2 месяца назад
Ambeye ziibwela za ziiiiiii
@AwandeOkuhle
@AwandeOkuhle 2 месяца назад
Komamwawuze.aziyakhula.ndiakazi.awo
@GoodluckVithumbiko
@GoodluckVithumbiko 2 месяца назад
kuwapatsa uremu achakwera ndiye zayesu zimenezo mwayara masanja paripose payende achakwera ndi manganya azikupasirani zimuzimu zoyipa kumeneko 😂
@JessicaManda-zm1ug
@JessicaManda-zm1ug 2 месяца назад
😂😂😂😂😂😂😂🎉🎉🎉
@MaryChavula-jz3di
@MaryChavula-jz3di 2 месяца назад
Uyu ndi chizeleza zinangochitika kuti ulamulilo wa dzikowu umapezedwa motelo kutu vp adzitenga malo otsogolelayo akafa koma a usi ndi oyaluka
@NyirongoMexonyoba
@NyirongoMexonyoba 2 месяца назад
Koma anthu muyakhura
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin 2 месяца назад
A vice kutafuna chingamu mhhhh komatu ziliko Munthu wamzelu tafutafu kopandaso disprin
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj 2 месяца назад
Umoyo wasanje umenewo vuto lako ndi chani adalemba pati kuti munthu asatafune
@GertrudeChifupa
@GertrudeChifupa 2 месяца назад
Lero anali ndi make Sikono
@KumbukaniChimbalanga
@KumbukaniChimbalanga Месяц назад
Mavuto kwabasi
@BeatriceProfessor
@BeatriceProfessor 2 месяца назад
Koma boma ili likungowononga ndalama ya misokho yathu zaziiiii
@RoseMkandawire-e2g
@RoseMkandawire-e2g 2 месяца назад
Zaziii sizikuveka iya
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 2 месяца назад
Dziko ndi anthu ake
@GodfreyMbiri-x8s
@GodfreyMbiri-x8s 2 месяца назад
Kufupikako.kkkkkk
@GloriaKaduya
@GloriaKaduya 2 месяца назад
Kodi magalasiwo amavinavina kk😂
@kadijhahaji
@kadijhahaji 2 месяца назад
Komatu zoona aaaaaakkkkkkkkkkk koma kumeneko
@isaaczuze
@isaaczuze 2 месяца назад
Manganya koma ziko ili ndilama drama basi
@paulmanyamba5437
@paulmanyamba5437 2 месяца назад
Asayambepo kuvinatu uku kkkkk
@HopesonLyman
@HopesonLyman 2 месяца назад
Paja samachedwatu
@stevenmakwinja9648
@stevenmakwinja9648 2 месяца назад
Kodi mai Skono mawawona?
Далее
🎙А НЕ СПЕТЬ ли мне ПЕСНЮ?🕺🏼
3:06:10