Тёмный

Mkangano wa Kamuzu Banda ndi Samora Machel. 

Bakili Muluzi TV
Подписаться 100 тыс.
Просмотров 191 тыс.
50% 1

Udani komanso chimkulirano pakati pa Kamuzu Banda ndi Samora Machel.

Опубликовано:

 

18 окт 2020

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 240   
@chifundoveluwa1184
@chifundoveluwa1184 3 года назад
Samora machel was a hero that's why his statue can be found in many parts of the world.
@mr98556
@mr98556 2 года назад
Imagine learning the history of Kamuzu from Bakili Muluzi News Channel...This is ridiculous
@sukatijere4392
@sukatijere4392 11 месяцев назад
VERY RIDICULOUS INDEED.
@MaryKana-vt3hc
@MaryKana-vt3hc Год назад
One great. Statement by Kamuzu was: I don't mix politics with economics. Hence Capital Hill and many other developments!
@aidaomicaia2430
@aidaomicaia2430 3 года назад
Good history, so amazing .
@chimmukono7102
@chimmukono7102 3 года назад
Kamuzu was genius He was choosing them just to make things work in Malawi He knew how we think and how we can easily destroy
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Ng'ona ku Stella Maris, Young Pioneers, gwirizano ndi apartheid.....ma card, kupha omuzuzula, kusokoneza ku Mozambique......kupondereza ufulu wa2..... education system yovutikira ....nzeru mukuzitama ndiziti ??? Most of chitukuko anachipeza and he stayed unchallenged for 31 years ...
@djmakedzana9917
@djmakedzana9917 3 года назад
Brown Mpingangira anali Chief Informaion Officer, atapita ku Zimbabwe anakumana ndi anthu matchona kumufunsa kuti ku Malawi kuli bwanji ? anati ku Malawi kuli njala , chimanga akungopasa a RENAMO. sanadziwe kuti anthuwa anali ma spy a kamuzu. Pobwera kufika pa Chileka anafikira unyolo
@pililani_blessings
@pililani_blessings 9 месяцев назад
😂😂😂
@AlinafeNdalama
@AlinafeNdalama День назад
Wow, what a very good history
@francismsowoya278
@francismsowoya278 3 года назад
To tell the truth, K. Banda did great things in Malawi. Most infrastructures which use today were done by him. We usually remember bad things someone did to us and not good ones. Even now people are killed because of political motivation in all states of Africa and the entire world.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Which infrastructures Kamuzu build? Ma infrastructure ambiri adamanga anali atsamunda koma umbuli ndi omwe ukukuchititsa kuti uziganiza mopusa choncho. Queen Elizabeth central hospital, Blantyre high court, Zomba central hospital, dedza secondary school, malosa secondary school, Blantyre secondary school, natural resources college, domasi TTC, Soche TTC, polytechnic college, ma community day secondary schools around Malawi, maofesi a agriculture Ku Lilongwe, nsanje, mulanje, thyolo, Zomba,mangochi, mzimba and so fourth. Zonsezi adamanga anali atsamunda not kamuzu. So don't be a fool
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Kamuzu anali munthu woyipa basi
@lucaswhite4279
@lucaswhite4279 Год назад
@@charlesmuyaya8839 P
@ahmadjamahiryajuma6456
@ahmadjamahiryajuma6456 Год назад
Kamuzu adapanga adopt zomwe a Zungu adapanga. Komaso zomwe a Zungu Adayamba Iye kumati wapanga ndiiye. Kamuzu adali oipa
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
You know nothing
@osamabinraden9391
@osamabinraden9391 3 года назад
🙋🙋🙋 👏👏 mbili ilibwino👍👍👍👍👍👏👏👍👍👍👍
@johnkaitano5081
@johnkaitano5081 3 года назад
ZIKUONETSA, KAMUZU SANALI MMALAWI analibe chikondi ndi Amalawi Satana anamugwiritsa ntchito kuika, amalawi mu mdima Inu mukunena, mbiri zotere PITIRIZANI Mulungu akusunge ndi moyo wautali kwambiri 👌👌👌👌
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 года назад
Boza limeneli ukukambali
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 года назад
Anali obwela ndi kape wakupha komaso okhesa mwadzi
@abdulmalikissah6979
@abdulmalikissah6979 2 года назад
@@kassimjuma8822 tsono zoona nde ndi ziti?
@user-rf4br1fv2z
@user-rf4br1fv2z 2 месяца назад
Pena a big ma history anuwa muziwatenga bwino zina zomwe mumanena za ku Mozambique atati adzikuvelani kuti kamuzu adapha samora kodi mumadziwa tikhoza kukhala pa mavuto akulu zina zimafunika kuziona bwino koma mumadziwa zithu zambiri timalandilila ku Mozambique ifeyo tilibe port yolandilila please think b4
@aubs4321
@aubs4321 3 года назад
Kamuzu anali oipa koma pa nkhani iyiyi he was right, do you think Malawi would be as it is without RSA providing the grant to build Lilongwe? Kamuzu was not backing the whites but 1. he believed dialogue was the best remedy to sort out the apartheid issue osati violence. 2 he was advancing his own interests for the sake of developing Malawi. 3. Those years after independence Malawians lacked skills to run the govt that is why Europeans were still employed. Documentary iyi wapala aise try not to take sides
@africulturetv6498
@africulturetv6498 2 года назад
Man bodza inu what was the point of getting independence while not knowing how to deal with it How can you get independence kenako nkuma sapota chitaganya cha mayiko ena zazi
@khodotech6481
@khodotech6481 2 года назад
Good
@elliotchisalanga12
@elliotchisalanga12 2 года назад
Wapala uyu Zina angolankhulapo
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
You are the one not making sense. We wanted to remove white rule in order to run government on our own ...we fought whites. Why did kamuzu support white rule in another country?
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Point number......it requires two parties to do dialogue....south Africa inaona ndipo idakaona khaza za azungu....what dialogue would you do pamene ukupandidwa ndikuphedwa chifukwa ukushala pakwana and you want you person space?? 2. Point yachiwiri....kod what was the fight those days ?? Ngati mukuziwa the Zina zoyenera kusapota azungu?? Kod inu mukafuna kutukuka zimatathauza kuti enafe tifinyidwe ?? Mwina munatero kwanuko zikhale choncho.... 3. Kod Angwazi ankaxiwa chomwe amafuna kapena ai.....John chilembwe ndia mazana mazana achikuda anaphedwa ndi kuzizika ndi white regime.....mumaiziwa slave trade?? Mukazavesesa zomwe a2 anaona kuli azungu muzavesesa kuti mzungu sanali m'bale koma yes it's ok to use two or three abwinowo koma azungu akamuzu ubwino palibe chifukwa amamugeirisa ntchito ngat puppet.....u can Google meaning ya puppet kuti mumvesese
@timeyomzumala
@timeyomzumala Год назад
Kamuzu anali wa nkhaz.this story is good
@promisekwenda4556
@promisekwenda4556 3 года назад
Kamuzu wachamba bas
@perlinsmhone5472
@perlinsmhone5472 3 года назад
He did very well to grow the economy. Forget about those who killed during his term. It is happening even here in S.A. people are killing each other due to politics. There was no hunger in his term.
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
My friend kamuzu was a dangerous killer and dictator. That can't be taken away. Malawi was not free
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Pilizi tamafufuzani bwino mbiri ya dziko lanu
@sidickbadat1086
@sidickbadat1086 Год назад
If Kamuzu was still alive and ruling Malawi 🇲🇼 all these corrupted politicians and Indians wouldn’t stand a chance.
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Mwinaso anakakudyeserani ku ng'ona inuyo
@charlesmbale7739
@charlesmbale7739 2 года назад
Kamuzu Banda is the one who was supporting Mugabe financially.... Mugabe once mentioned this even KK mentioned the same at SADC summit in Namibia which former head of states attended. ...
@najereeliya7761
@najereeliya7761 3 года назад
This is amazing
@user-ll7hz7uy3q
@user-ll7hz7uy3q 8 месяцев назад
Komatu Mozambique inatengadi malo ambiri ku Malawi
@bkelly3053
@bkelly3053 3 года назад
kamuzu he was not malawian
@brianmwizagondwe1321
@brianmwizagondwe1321 3 года назад
If I was Kamuzu, I kamuzu have allied with SA as well. Samora was a threat to Malawi..
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Kamuzu was a puppet to the white imperialism. He was a hypocrite
@snathan99
@snathan99 Год назад
Kamuzu, the father figure of Malawi, you will never erase this history whether you like it or not...
@sydneysakala7246
@sydneysakala7246 7 месяцев назад
Achitsiru inu
@adamkaisi6954
@adamkaisi6954 3 года назад
Indeed Kamuzu was a doubtful President, not even one day he surprised the Malawians by speaking the vernacular .he gave influential posts to whites in his government Good research brother
@botaclive5898
@botaclive5898 3 года назад
Kamuzu spoke tumbuka fluently
@mwai72
@mwai72 2 года назад
There is no research...this is not even history...this is done at a slant AGAINST Ngwazi. From his early days Ngwazi would speak for minutes about how the Bible has been translated poorly into chichewa. He spoke the real chichewa, cha ku central region. This is propaganda...Mandela would later say "Kamuzu was right" look it up!
@sydneynyirenda7745
@sydneynyirenda7745 Год назад
We shall not have as patriotic a president as Kamuzu was. Unlike our neighbours, our country was the least developed at the time of our Independence and it was Kamuzu who kick started development from scràtch.
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
@@botaclive5898 which tumbuka? Tumbuka he banned?
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
​@@sydneynyirenda7745aaaaaa koma mavuto tili nawo ndi2
@patumaabiti2415
@patumaabiti2415 3 года назад
Ada awawa mukuti a Kamuzu anali chigawenga
@oziledambula9107
@oziledambula9107 3 года назад
According to his history that guy was gangster 😂😂😂
@elymsliehara6280
@elymsliehara6280 Месяц назад
Good history
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Mukukaika 😅
@mrmustdeDj
@mrmustdeDj 2 года назад
Koma the narrator si munthu wamba..🙌🏿😂..white people in public sectors was ideal..that’s why Forex wise tinali nyatwa
@chancyshaba3664
@chancyshaba3664 3 года назад
Nice one
@modiejonathan8547
@modiejonathan8547 3 года назад
Your enemies are not my enemies.
@StanleyWachazaBanda
@StanleyWachazaBanda 8 месяцев назад
Africans, let alone Malawians, are adventurous they have and still continue to travel to South Africa even before Africa started to gain independence and Dr Banda knew that Malawian being landlocked country we needed South Africa to access their ports. He believed in contact and dialogue and not boycott and isolation. When he went to South Africa, he challenged them that you white people you were under Roman Empire for ages and do you think these Africans will want to be under you forever. He even advised UNGA that you can not be talking about South Africa when there was no delegation from RSA. For your information Dr Banda supported ANC that the more reason when .Mandela was released he came to Malawi and other countries to acknowledged the support. Mugabe sought refuge in Malawi when he was fighting with Smith.Dr Banda was a freedom fighter. Malawi Zambia Zimbabwe when they were fighting for independence and went to England with Kaunda Joshua Nkomo Dr Banda was their spokesperson. Mozambique Zambia and Zimbabwe opted for boycott and isolation during the day while at night they were eating food from RSA Dr Banda didn't subscribe to this way of thinking
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 3 года назад
The story could be true at some point but my advice to the narrator is that are some stories that are so sensitive,secretive for the safety of the nation.ngati izi za ubale wa Mozambique ndi Malawi.that story is sensitive
@innocentmpoto
@innocentmpoto Месяц назад
Great job Mr
@mrmustdeDj
@mrmustdeDj 2 года назад
Ati kamuzutu anali chigawenga 😂🙌🏿
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Kamuzu anali chigawenga mapeto. I am sure komwe aliko panopa akuwotchedwa ndi moto wa gahena
@zumahmedison9672
@zumahmedison9672 12 дней назад
Zoona mbava
@zumahmedison9672
@zumahmedison9672 12 дней назад
Zoona mbale
@asiyatumilera7349
@asiyatumilera7349 3 года назад
Kamuzu Banda was a traitor
@oziledambula9107
@oziledambula9107 3 года назад
Kamuzu was sellout just imagine nkhaza zonse zinkachitika zija
@jonathancox4189
@jonathancox4189 3 года назад
But there was no rapes,murders,uchigawenga ,we were united one Malawi. I am glad the MCP et Al will revive those sweet old days.
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
​@@jonathancox4189 pena zimachita kudabwisa kuti history yosabisika ngati iyiyi mu2 ukaime pachulu kubakira kamuzu ati kunalibe murder .....mwatani kodi ???
@gesusgegangphray7689
@gesusgegangphray7689 3 года назад
Mwambetani, kanyama chiume was helped with my own father in njombe Tanzania. Bishop aipa was kamudzu agent i know all the secret meeting.. but bishop aipa dint betray kanyama chiume,
@djmakedzana9917
@djmakedzana9917 3 года назад
1986--1988 Kamuzu appointed Hans Joachim Lesshaft as governor of the reserve bank to replace Chakakala Chaziya. Chaziya anamangidwa koma boma linalengeza kuti wapita ku school
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Kamuzu was so evil
@jaffarzacharia9011
@jaffarzacharia9011 3 года назад
Kamuzu was a sellout
@duncanosman10
@duncanosman10 3 года назад
Mwatitsukula mmaso maka za Samora ndi Kamuzu
@brianmwizagondwe1321
@brianmwizagondwe1321 3 года назад
So kamuzu knew that the dude was dying in 2 weeks time. Dzikoli chinachilichonse ndi ndale
@isaacbanda2973
@isaacbanda2973 3 года назад
Kamuzu Banda just wasted our time and inali mbava cause when amkamwalila Anali 22 billion kwacha just imagine
@yobembewe7078
@yobembewe7078 3 года назад
You don't what you are talking about.
@jaffarzacharia9011
@jaffarzacharia9011 3 года назад
kamuzu anali ofoira
@kwangujaidi1020
@kwangujaidi1020 2 года назад
I would agree, this guy was very rich and his people still have it komaso kunalibe omufufuza chuma chake ndiye anali mfulu wathe!!!!
@joebrown1158
@joebrown1158 Год назад
Kamuzu was wealthy of 422billion chakwa you people you need to do more research
@JamesChaponda-em7op
@JamesChaponda-em7op 3 дня назад
1971 Gaddafi was not president by then
@madalitsomachira7477
@madalitsomachira7477 Год назад
Leaned where Malawi was and now is.
@user-dn8pt4uz3q
@user-dn8pt4uz3q 6 дней назад
Kamuzu anali wakupha🙌pano ali ku moto😅
@ernestmkanthama7329
@ernestmkanthama7329 2 года назад
Kamuzu amakatukwana azungu man
@mosesgeorge9016
@mosesgeorge9016 3 года назад
During Kamuzu Photocopiers were not in Malawi. Tamanenani zoona. I think narrator was not even born.
@motomoto5588
@motomoto5588 3 года назад
Koma kuno kumbali Kamuzu Banda ndi Galu
@khoofficial4789
@khoofficial4789 3 года назад
Kkkkk koma ndaseka
@FutureBeatzStudioz
@FutureBeatzStudioz Месяц назад
He went their for the benefit of Malawi...
@kingstonephiri5495
@kingstonephiri5495 2 года назад
Please try to take out the background sound most sound like this comes from our country video only it’s making noise
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 года назад
Kamuzu amadya chamba moipa ndikumidziwa
@isaacganizanikaziputa4901
@isaacganizanikaziputa4901 3 года назад
kkkkkkk madyera limodzi?
@kassimjuma8822
@kassimjuma8822 3 года назад
Anali munthu wachabe kamuzu kwambiri oyipa mtima
@ishmaelhero6160
@ishmaelhero6160 3 года назад
kamuzu anali wakupha basi mzungu wausilu...
@catherinemtunga2259
@catherinemtunga2259 3 года назад
Still Malawi was a better country to live in. We had all the good living standards. Kamuzu wa still a genius.
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Which living standards are you talking about? During Kamuzu azimayi ambiri ankaberekera kwa azamba, ana ankanyentchera chifukwa cha kusowa zakudya, there was kwashiorkor, marasmus in the villages. Anthu ankadalira ma missionary schools,Kamuzu failed to build schools and hospitals in Malawi. Ma secondary school a boma amene analipo were built by colonial govt. Look at domasi college, natural resources college, polytechnic college, malosa secondary school, soche technical college, mpemba administration college, dedza secondary school, Blantyre secondary school, Zomba central hospital, queen Elizabeth central hospital, chichiri stadium zonse ndi zitukuko za atsamunda. Ndi chani chimene Kamuzu anamanga for 31 years? Ambiri mmanena zitukuko za atsamunda because you know nothing about it.
@danielmaluwa7896
@danielmaluwa7896 3 года назад
Kamuzu was very cruel and bad. He didnt nothing in this country except stealing 250 billion kwacha
@kannandhanukkodi8548
@kannandhanukkodi8548 3 года назад
Very sad that malawi was ruled by a foreigner who was more cruel than a wild animal
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
There is nothing like good living standards. Kamuzu was a dictator and killer . He was selfish too!
@edwardnsapato8840
@edwardnsapato8840 3 года назад
Aluta Continua!!
@joebrown1158
@joebrown1158 2 года назад
Just in short Kamuzu was not Kamuzu from kasungu that one was from Ghana his real name was Richard Armstrong his father was an American, his mother was a Ghanaian.
@adam6kazembe642
@adam6kazembe642 Год назад
A theif
@mcandrewsmaunda7921
@mcandrewsmaunda7921 Год назад
We care less about that.We care more about the fact that he did a lot for Malawi
@joebrown1158
@joebrown1158 Год назад
@@mcandrewsmaunda7921 What really more Kamuzu did that time by keeping people in captivity making people so much suffering is what you tell people that he did alot? How I old are you during the reign of Kamuzu?
@mcandrewsmaunda7921
@mcandrewsmaunda7921 Год назад
@@joebrown1158 Yes.During his time, there were both good and bad things.We must acknowledge both sets of things.We must not be selective.You will find someone seating on a bus travelling on M1 that Kamuzu built but denying the fact that Kamuzu developed Malawi.I wonder what we should call that.
@mcandrewsmaunda7921
@mcandrewsmaunda7921 Год назад
@@adam6kazembe642 Whatever!
@basiliochiueteca6239
@basiliochiueteca6239 3 года назад
Kamuzu Banda was a traitor and a liar, in a poor country being able to deceive his people and humiliate him like nothing would happen if his people lived together.
@frankcassim
@frankcassim 2 месяца назад
Kmaso anachita bwino amozambeque kutilanda Malo ambiri
@jackson866
@jackson866 10 дней назад
You don't know the politics of Kamuzu Banda very well he was ahead of his time. While Kamuzu was working with the white South African government for economic reasons openly in the day he was helping the ANC privately at night. Many of the ANC soldiers used Malawi passports to go to Russia where they were trained to fight the Apartheid government. That's why when he went to SOWETO in RSA he was received like a hero, they knew how he was helping them with the mabhunu's money. I know this because I was in the system. Ndale za Kamuzu simungazimvetsetse mwachepa nazo bambo musanamize wanthu. Kamuzu ananthandizana ndi Kenneth Kaunda wa ku Zambia ndi Joshua Nkomo wa ku Zimbabwe kulimbana ndi a tsamunda kuti maiko amenewa alandire ufulu, Mugabe mukutchulayu asanabwere. Zina mukulondola koma zambiri simukuzidziwa. I remain.
@danielkhinguirossejuliasse6106
Malawi ndi Mozambique sadzamwerana madzi mpaka kare Komasso tidzangolanda dziko lamalawi kukhara provincia ya 11 kuno kumozambique
@kuziririzaisabatosiitegeko7088
Malawi idagali mumanja ya atsamunda!
@AlexKaunda-ny2eg
@AlexKaunda-ny2eg 20 дней назад
Kamuzu anali opusa ngati chakwera
@simonchilala4138
@simonchilala4138 Год назад
Like it
@isaacchipatala9143
@isaacchipatala9143 3 года назад
Ndizoona zikachitika
@user-cl5pi4nb1e
@user-cl5pi4nb1e 4 месяца назад
Pano chipani cha MCP chasitha chikupha powapasa njala amalawi, kusapezeka makhwala muzipatala, kuba ndalama za boma katangale
@zachariahlungu3577
@zachariahlungu3577 2 года назад
Zikomo bwana
@charliepoulaliecky5687
@charliepoulaliecky5687 3 года назад
Kamuzu banda sadali Mmalawi ayi ndi chifukwa chake anthu ambiri akumalawi adalikuzuzidwa
@eunicemoyo5808
@eunicemoyo5808 3 года назад
zoona sadali abale ake
@cphiri8035
@cphiri8035 3 года назад
Wa khuta mgayiwa uko nkumakamba zopusa pa media tandi tchulile present anachitachitukuko kuposa kamuzu
@kwangujaidi1020
@kwangujaidi1020 2 года назад
Chakwera
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Akukamba nkhanza ndi unkhutukumve wa kamuzu zinene zili zowona
@BornwellNurd
@BornwellNurd Месяц назад
Sharp
@madakumanga4395
@madakumanga4395 3 года назад
Mmmmm koma yah
@siyaninansolo1375
@siyaninansolo1375 3 года назад
But also I hear that Samora was targeted by Kamudzu banda & Nelson Mandela bicoz here in south africa there's a place called Samora where that airplane that was with Samora was attacked by those two president so can I get help on this so that I can over stand
@brianmwizagondwe1321
@brianmwizagondwe1321 3 года назад
I think this was before mandela. I understand Kamuzu allied with the arpatheid government.
@jermiasfranciscofrancisco5453
@jermiasfranciscofrancisco5453 3 года назад
Ndikanakhala ndinalipo ndikanapha Kamuzu banda
@rodglae6657
@rodglae6657 5 месяцев назад
@NJELEKA
@NJELEKA Год назад
Kamuzu was a destroyer and he made most of Malawian not to have freedom in other countries
@josephmaster4367
@josephmaster4367 Год назад
Continue
@patrickphiri5334
@patrickphiri5334 3 года назад
Very sad history indeed
@princemanda2642
@princemanda2642 Год назад
Fake story
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
@@princemanda2642 nothing is fake here chief . Kamuzu and mcp killed so many people in malawi. We can't forget
@kalimawandale7161
@kalimawandale7161 Год назад
In conclusion this is a clear cooked history of Kamuzu cooked up by his haters, Kamuzu remains our hero no one can change that
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Kamuzu is a hero to who? Kamuzu was an idiot dictator
@chimwemwenkute3839
@chimwemwenkute3839 Год назад
Aluta continuea
@donaldj.kufankomwe1254
@donaldj.kufankomwe1254 Год назад
My dear, ideology difers. Never think that the way you think others will think in the same way. Appreciate differences.
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Zomwe akunena apapa sikuti ndi opinion kma ma facts. Ndi zomwe kamuzu amapanga. Records are there. Kamuzu was a serial killer and dictator
@user-pg9yl8jq8p
@user-pg9yl8jq8p 9 месяцев назад
Thats it
@user-yt9gc5ur8b
@user-yt9gc5ur8b 8 месяцев назад
Kamuzu was a hero
@JamesMuhango-yd3ie
@JamesMuhango-yd3ie Год назад
Yes kamuzu anali wawupandu
@aubreywallo1987
@aubreywallo1987 3 года назад
Kamuzu was the greatest!
@gesusgegangphray7689
@gesusgegangphray7689 3 года назад
I cant give u my name .. but i schooled in malamulo benson ligenda time... Malawianí get ready of me. I will save u from man-made poverty. And musiye kulozana and truating asing'anga.. we will change first this.. i know I every 2 malawian 1 trust nyanga ...how many mukufuna chitukuko
@alexanderhastingsc2211
@alexanderhastingsc2211 3 года назад
Lets talk
@FidelisNthenda-qq5sg
@FidelisNthenda-qq5sg 6 месяцев назад
Zaubwekabweka 😂😂😂
@modiejonathan8547
@modiejonathan8547 3 года назад
Kamuzu amalankhula chichewa
@jonathancox4189
@jonathancox4189 3 года назад
I miss PRESIDENT DR BANDA, I have been here in UK for 33years 2 years ago I visited home for the first in 31 years I decided to visit His Mosleum, I couldn't hold myself, I cried and cried to a point that the Gentleman who is stationed there asked people to leave for 30 minutes and told me that I can take pictures. I was so distressed that couldn't hold my camera and I ended up leaving empty handed . I was shaking and wailing on top of my voice . I must admit that I never knew that would be my reaction. I took me totally by surprise. MY name is Mrs Chrissie Spencer-Cox ( née CHRISSIE KUNKAPUNDA) from Chikwewo Village ) Ntaja
@amaryllishotel
@amaryllishotel 2 года назад
Do you have fond memories of him
@abdulmalikissah6979
@abdulmalikissah6979 2 года назад
I think something wrong with you bro
@richardrwizamlendo843
@richardrwizamlendo843 Год назад
Shame on you
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
Shame on you!
@yusufbonomali4222
@yusufbonomali4222 10 месяцев назад
There is no secret under the sun
@lazaruskamangira8730
@lazaruskamangira8730 Год назад
Three if not four positive things about Kamuzu's visit to RSA then 1, FREEDOM TO CHOOSE. He wanted a loan to build Capital Hill. He refused the IMF loan which comes with conditions and interest to devalue our currency and enslave Malawians 2, AGAINST APARTHEID. He was the 1st Black president who told Black South Africans to go with him into white-only shops and toilets. 3, POLITICAL SUPPORT, On kamuzu's death, Nelson Mandela personally said " Kamuzu was a good man because he used to send me money when I was in prison at Robin Island. 4, GREAT ECONOMIST. It is documented in the Book " Who Is Who" that Kamuzu Banda and John Tembo as ministers of finance managed to Hold Malawi Kwacha 1to1 with British pounds. Look today at 1:1226.09 and it's still in free falling into the next hyperinflation like Zimbabwe. 5, CORRUPTION. Most of his leadership was less corruptive than it is today. These are my perspectives. This was world politics and not religion. Kamuzu was as bad as any other leader that followed him. Let's talk about The good and the bad of Kamuzu, just like everyone else in a position of Power.
@user-jf8zt3pe8p
@user-jf8zt3pe8p 3 месяца назад
Mmmmmmmmm
@enwoodmlotha6318
@enwoodmlotha6318 3 года назад
Kamudzu Banda was a British man his real name was Richard amstraw
@pachalojailoskincaidphiri4545
@pachalojailoskincaidphiri4545 3 года назад
There has never been such a name as Richard Amstraw since....please do your search properly before u commit ur stories to platforms such as this.
@abdulmalikissah6979
@abdulmalikissah6979 2 года назад
@@pachalojailoskincaidphiri4545 kamudzu was not real we are not Children, that guy was rechard and he hard British citizenship including the United States
@joebrown1158
@joebrown1158 Год назад
@@abdulmalikissah6979 Richard Armstrong that was his real name all the way from America to Ghana his father was American and his mother was the Ghanaian people need to understand the biography of that man so called Richard Armstrong/ Kamuzu Banda the imposter
@AnishaMoosa-ej7yr
@AnishaMoosa-ej7yr 6 месяцев назад
Chipan choipa
@laitonkamanga7679
@laitonkamanga7679 Год назад
Samora Machel
@nyobomba
@nyobomba 3 года назад
muluzi news indeed ... tell history non partisanly pilizi
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
Zonse wafotokoza apa is a true story. The problem is you who thinks otherwise.
@humbleyuzyx7150
@humbleyuzyx7150 Год назад
May God gives him severe punishment where ever he is , Jonathan Smith was a bad person
@alexanderkaunda9554
@alexanderkaunda9554 3 года назад
Kamuzu sizinali zinthu
@smithsaidi9237
@smithsaidi9237 3 года назад
Kunena zoona kamudzu Banda sanali was kumalawi
@bestonjoseph2193
@bestonjoseph2193 3 года назад
Nchifukwa Malawi inali yolemera azungu ankayendatsa ndalama
@joshuamusaa
@joshuamusaa Год назад
Why many stories are coming after the death of a person
@hi-profileltd
@hi-profileltd Год назад
Munthu mku mbuyo...the beggining has nothing but the end...how wil you finish your journey thas wht matters heaves and hello..depends on your ending lets finish good so that we enter heaven
@lastonekaponya7675
@lastonekaponya7675 3 года назад
Muluzi zidankanika bola achingopitiriza azunguwo now south African pano yikusauka
@pachalojailoskincaidphiri4545
@pachalojailoskincaidphiri4545 3 года назад
Very true Lastone...awa zawo ndi ma propaganda basi....Kaya akudziwa kuti ndale ku Malawi zinasintha kaya...Anthu tikumawerenga ndikumadziwa chenicheni....Sizoti poti mwalemba apa nde tikukhulupilirani ayi. Bring your sources here, no propaganda apumbwa inu
@amoshepson66
@amoshepson66 3 года назад
Wabanda uyu zampweteka
@yobembewe7078
@yobembewe7078 3 года назад
Samola is dead
@catherinemtunga2259
@catherinemtunga2259 3 года назад
😂😂😂😂😂
@catherinemtunga2259
@catherinemtunga2259 3 года назад
Pano mwana ky primary akulephera kuyankha How are you? Weni weni yu
@AnishaMoosa-ej7yr
@AnishaMoosa-ej7yr 6 месяцев назад
Is not Malawian
@mikewilzmphundi4927
@mikewilzmphundi4927 2 месяца назад
iwe ndiwe wabodza. besides Dr Banda being friends with RSA white gov. On the other side he was helping ANC. that guy was a genius. why are you giving out only negative info? za zii
@mayesokulea2445
@mayesokulea2445 3 года назад
Kamuzu was good ,ada awa ngofoila maboza awowa they think angabuleke good news of kamuzu Banda njeeee!! Akunamiza this kamuzu we know sungasinthe history yake , everything you say is bad of kamuzu what a fake history?? Akupusisa akuuza kuti ulimbane ndi mzimu wakamuzu iweyo sudzatchukapo nchabwa😜😜😜
@beketemoyo9279
@beketemoyo9279 3 года назад
Kamuzu ubwino wake unali pati munthu wakupha ngati ameneyu. Mwina kwanuko sikunaphedwe anthu nchifukwa chake ukulankhula zopusa apa. Kamuzu anali galu wakuba, wakupha, he is rotting in hell now
@bolakunthazi589
@bolakunthazi589 3 года назад
Iweyo ndie ofoira. Zoona mpaka kumasapota chigawenga ngati kamuzu? Ukuoneka mutu ndiwe mwana palibe chomwe ukudziwa chokhudza kamuzu banda. The guy was evil.
@mayesokulea2445
@mayesokulea2445 3 года назад
@@bolakunthazi589 kamuzu was good only adzigogozi ndadzibambo akwanuko adakuuzani zoipa zakamuzu ,ndipo to everybody ali ozindikila though ntapange ma Cv anu mukuipisa mbili yakeyo mungochedwa , that man alrdy created good Cv the whole world, mudzingodya deya kwanuko
@mayesokulea2445
@mayesokulea2445 3 года назад
@@beketemoyo9279 umafuna akapangile chitukuko pakhomo pakwanu?? Everything you see mu malawimo mesa that's dzitchito dza kamuzu Banda?? U are too late nkulu , that man created nice Cv alrdy ,inu dzikandani ndiuphawi adzandale akupusisaniwo mukungodya machenjewo
@charlesmuyaya8839
@charlesmuyaya8839 3 года назад
@@mayesokulea2445 you are just a bunch of nonentity. How can you say everything we see is for Kamuzu? For 31 years analephera kumanga zitukuko. Ndi misewu ingati imene Kamuzu anamanga ? For 31 years analephera kumanga zipatala. Look at Queen Elizabeth central hospital and Zomba central hospital zomwe anthu ankadalira; zonse zija anamanga ndi atsamunda. Look at secondary schools, ndi angati amene anamanga? Poti ma Secondary masukulu ngati malosa secondary, Blantyre secondary or even dedza secondary schools anamanga analinso atsamunda. Kamuzu wakoyo anapanga chani pa 31 years choposa kudzilemeretsa yekha?
@user-zk5nu5gp5u
@user-zk5nu5gp5u 3 месяца назад
Kamudzu was not a Malawian,he lied to true Malawian
@felixmasamba4657
@felixmasamba4657 Год назад
Is this man, is he a Historian or he wants to support someone?
@juliusnkhoma755
@juliusnkhoma755 10 дней назад
Ngati akukupangani point kusayenera mutsikeni .....koma ngati mukuona ngati ndi ngamo akothakayi pangani chiganizo chabwino basi
@kondwanitembo386
@kondwanitembo386 3 года назад
Zaziiii
@tamandachokotho7793
@tamandachokotho7793 3 года назад
Anali galu Kamuzu wakoyo. Paja iwenso unali mmodzi mwa anthu akuba eti, abale ake a John tembo inu
@bensonphirimalotabrighton2779
@bensonphirimalotabrighton2779 3 года назад
Ndipotu zosatentha bro kondwani Tembo ndakunyadirani bro
@catherinemtunga2259
@catherinemtunga2259 3 года назад
Ndititu olo nchere mulibe. Za ziiii ndithu
@duncanchizizi6543
@duncanchizizi6543 Год назад
@@tamandachokotho7793 ndi abale Ake ozizira mutu kkk
@gibsonnachiye2549
@gibsonnachiye2549 Год назад
This story is full of lies about Kamuzu. Where did he get this information?
@bakilimuluzitv3371
@bakilimuluzitv3371 Год назад
Can you explain the lies you have heard in this video please?
@kalimawandale7161
@kalimawandale7161 Год назад
@@bakilimuluzitv3371 Kamuzu ankayankhula chitumbuka bwinobwino
@valdimiroandresozinho
@valdimiroandresozinho Год назад
Wachikwulile tatiyinemuziponya pipani thu
@valdimiroandresozinho
@valdimiroandresozinho Год назад
@@bakilimuluzitv3371 zinelanga vadi ndi mafunemuzipo nyazapwili
Далее
Samora Machel visits Malawi (Complete)
18:26
Просмотров 1 млн
Stray Kids <ATE> UNVEIL : TRACK "MOUNTAINS"
00:59
Просмотров 685 тыс.
SHANIL MULUZI  DZIMBIRI PROFILE
2:57
Просмотров 35 тыс.
BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.
58:38
Mwazi wa Chilima wayamba kugulidwa ndi ndalama
17:07
Просмотров 33 тыс.
Kamuzu Banda House|Ngulu ya Nawambe
2:36
Просмотров 76 тыс.
Stray Kids <ATE> UNVEIL : TRACK "MOUNTAINS"
00:59
Просмотров 685 тыс.