Tiyambe kufufuza imfa ya Chilima ndi Witika. Chifukwa ndiwa MCP ndiye imfa imeneyi ikhale yowawa? Ai kupha ndikwa MCP. Musalire lero. May the soul of Mabvuto rest in peace. Kunkuyu siyani kuononga dziko
Ifesotu tinamva pa misonkhano mukunena zoti pavute bwanji Dr Chilima salamulira ndipo munanenetsa kuti papangidwe sacrifice and munamuphadi pomaliza pake and up to now mukukana kupanga commission of inquiry meaning mukudziwapo kathu amfiti inu achabechabe mwapangitsa Anthu kukhala amkwiyo mdziko muno chifukwa chosachitapo kathu pa zaimfa ya Dr Chilima, witika ndi chipongwe chapa Mbowe omwe anapanga mukuwadziwa koma osawamanga
Iwe ife za imfa iyiyi sikutiwawa kwenikweni koma nkhani ndi ya Biyeni SCK ndi anthu 8 aja osati zoduka mutu ukukambazi ayi Kodi a chipatalawo atayeza thupilo alipeza ndi madala? Kapena kuti mwina anachita kuombeledwa? Lelo mukuti mukufuna mufufuze zoona zenizeni za imfa imeneyi bwanji simukufuna mufufuze za imfa ya yemwe anali wachiwili wa chikangawa lion 🦁🦁🦁🦁
koma maliro tisamawa pangile ndale ndizowona wagona.musayike kuti adale ndi omwe akutele akukuyu khani zaifazi zilipo zingati ku ntcheu ku thyolo ku mangochi ku balaka anthu akufuna kuziwa zoziwika koma tisasatengele ndale ndithu
Inde abwana izi mukuyankhulazi sizikusiya ndi zomwe mumayankhula chilima alimoyo kod inu akubanja la k .s .c .inuyo Akukuonani motani popeza inu ndye ndi mwana yemwe akuchita kudziwiratu kuti .m c p ndiyomwe yapha anthu 9 anja