Тёмный

Ngongole za Malawi zachulukitsa. Abwana anapita kunja kopempha ndalama. 

Bakili Muluzi TV
Подписаться 122 тыс.
Просмотров 29 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

11 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 168   
@ibrahimalfred6539
@ibrahimalfred6539 Год назад
Usogoleli olilisa kwambiri wa chakwera😢😢😢 Malawi will never forget you
@georgechikafutwa1334
@georgechikafutwa1334 Год назад
😢😢😢😢
@salomaoernestoernesto4573
@salomaoernestoernesto4573 Год назад
Ambuye siyani Dr chakwera agwire nchito mukuoneka kut za mboma simuziziwa mbwerera basi za ziii
@johnman4619
@johnman4619 Год назад
Zikumveka ndithu munthu wankhuru kumeneko ulemuwamu bwana ...ndizoona ndithu kutikodi awa analindani .big guestion sir
@isaacfesani2357
@isaacfesani2357 Год назад
Perfect
@josephgabriel1016
@josephgabriel1016 Год назад
Chitini chopanda kanthu chimatsokosa kwambiri ndiye mwazioneratu nokha. Ndimayesa amanama that an empty tin makes noise. Thanks bwana pakusakatula maganizidwe aa anthu
@PromiseBarton-em1ll
@PromiseBarton-em1ll Год назад
Boma ili nde zero pa zero.😢😢😢
@georgechikafutwa1334
@georgechikafutwa1334 Год назад
Zelo pa ten
@khalidwetchaua24
@khalidwetchaua24 Год назад
I like you Bro , you know how to analysis things . keep it up !
@anafieintuka8090
@anafieintuka8090 Год назад
🙏🙏🙏 timakusangalalilani achikulire
@chrissygama8678
@chrissygama8678 Год назад
You are king 🤴 of history in our country 'kma chilungamo China kupweteka ndithu
@mussamapira801
@mussamapira801 Год назад
Achakwela angogwidwa kwachotsa pa u president 90 minutes eterber wakuba
@KingsleyWakusa
@KingsleyWakusa Год назад
My man,,,,,,,,,,you deserve,,, much respect,,,,achakwela atipha awaa
@johnkayisi4043
@johnkayisi4043 Год назад
😢 iiih koma ine chakwera 😢😢
@subederamado1977
@subederamado1977 Год назад
Dr chakwera and doog aaaa
@georgemponda
@georgemponda Год назад
Koma iwe ndikatundu madzi😂😂😂😂😂😂😂😂🎉🎉
@mustafayohane6582
@mustafayohane6582 Год назад
🤣🤣🤣🤣🤣
@irenechirwa9710
@irenechirwa9710 Год назад
Bwanji angotula pansi maudindo awowo tatopa nawo ife anthuwa
@andersonmaster8055
@andersonmaster8055 Год назад
The king of history
@luciomodestosimao6650
@luciomodestosimao6650 11 месяцев назад
Dziko lingatha zimayenda ngati Baibulo. Mwawonjezatu pamenepo
@nelsonmacken7662
@nelsonmacken7662 Год назад
Well conclusion bro, that is the fact and reality let's bring people who have something better not mulimi all the way from asamunda no man please Mr president
@milajimussa4120
@milajimussa4120 Год назад
Kkk big man kutsitsa mfundo zabwino
@rodwellmwenekitete8974
@rodwellmwenekitete8974 Год назад
Wa udindo aliyetse adziba,, akhulukidwa zili ku Malawi,,,pano palibe kuopa kuba chifukwa chikhululuko chilipo,,,koma tsoka ili kwamuthu ovota palibe chimene chikumukomela muthu otsauka.
@hughmankalonga3769
@hughmankalonga3769 Год назад
Amakakumana ndi Sattar ameneyi
@rodwellmwenekitete8974
@rodwellmwenekitete8974 Год назад
Achakwela mukhululukiletso ma prison amene alibe mulandu wakupha,,ogwililila,,ndi opyanya nyumba please atuluseni
@GastonElias-rn2so
@GastonElias-rn2so Год назад
Bro i see you a very good analyst, kunena zoona tikifunikadi ma investor enieni kut tiseve zambiri
@wisikitiyesi1224
@wisikitiyesi1224 Год назад
I like you brother thanks you so much
@BladesBullets-pu5uw
@BladesBullets-pu5uw Год назад
Zomwe zimandimvetsa Chisoni ndizoti mtsogoleri wadziko akamalephera kugwira bwino ntchito yake pali anthu ena osaukisitsa omwe akuponderezedwa ndi mtsogoleriyo, muwaona akuimbira mmanja ndikumamuchemerera mtsogoleriyo. Ndife olilitsa zedi.
@phillipstamaley7901
@phillipstamaley7901 Год назад
Always I disagree with you but now totally! totally agree with you accordingly
@johnchilima6351
@johnchilima6351 5 месяцев назад
Tenaon amenyo nchewa wasiru amneyo wanonga Malawi 🇲🇼 akuyesa kuvena gule
@edwinrobert5346
@edwinrobert5346 Год назад
Well done brother koma tafufuzaniko za ma passport please malawi wawonongeka wuyu pakufunika ma demo anyone chakwera ndi mphawi wa chabe amene sangatukule ziko
@johnshaka3
@johnshaka3 Год назад
We need to vote again awa zikuoneka Kuti zawakanika basi
@kelvingremphiri565
@kelvingremphiri565 Год назад
Komaso trip ya President ya ku Malawi anthu ambiri,there is no war on Malawi but security yambiri
@staceycossam5933
@staceycossam5933 Год назад
Salute bro
@mollymasangano473
@mollymasangano473 Год назад
Mupange video yoti ma donating a Cyclone freddy anabwera angati ?kikikiikiki Malawi 🇲🇼 😀 🇲🇼 wanthu akulowera ku ntchire. ♥️ Mapeto ake mitengo it itha, koma nawonso they are failing to empower Malawi 🇲🇼 😢 Shaaaaa.
@thegreens9075
@thegreens9075 Год назад
Kusowa kolima chifukwa choberekana ngati ntchentche ...palibe chomwe amalawi angapange pawokha .
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 Год назад
Kkkkkkkkkk Eeee!!!!!! Koma ndie kwapephedwatu...kungozolowela Chachikhumi.mpaka kukapepha Company yopanga juice.
@princedetbozsmallboy1749
@princedetbozsmallboy1749 Год назад
Mr Atupele anayankhula kale kuti lenara samupasa bus or galimoto, Chimene tizawakumbukile agaluwa ndi kuba kowopsa basi ndikupempha pempha. Sindisintha Chichewa changa, kuti mwa Chakwera mulibemo ubwino, munthu wotumidwa ndi satana angapange zokhumba anthu? Mesa akupanga chimene tate wakeyo akufuna? Dont expect anything good from this heartles presdent.
@user-zk7jw9up6m
@user-zk7jw9up6m 3 месяца назад
Malawi tili ndi madzi ponsenponse koma boma limangoganiza zokuba ndalama zathu iwo kumalemela
@jamesmadalitsomchenga5308
@jamesmadalitsomchenga5308 Год назад
Atsogoleri a mu africa lero ayamba kutseka zitseko za atsamunda ndipo ali pa mgwilizano wochotsa US dollar mma bank mwao. Pomwe President wa Malawi Ali busy kupempha kwa ma oppressors. A disgraced man. Experience alibe zoona.
@Vava-up5dc
@Vava-up5dc Год назад
Kodi awa anali ndani?😂😂😂😂 Yankho mulipeza nokha😂😂😂😂
@BwanaGD
@BwanaGD 5 месяцев назад
Anazolowera kusonkheledwa ndi mpigo kumati zabusa kuparsidwa chopeleka kudya zachinkhumi
@piliranimphepo1920
@piliranimphepo1920 Год назад
Uyu mumati chakwerayu ndi chitosi basi aah!
@symonyohane6989
@symonyohane6989 Год назад
nothing to say you man you deserve medo koma ndimafuna nditakuona uli ndimawu aboh
@aggogokina8992
@aggogokina8992 Год назад
Big man ndinu katundu omanga ndi mawaya afukuleni musasiye tiziudziwa usiru wawo akupangawu
@AnordThomson-iw5ny
@AnordThomson-iw5ny Год назад
Ntundu umenewu sibwino kuwupatsa u president m'malawi muno chifukwa ndidzilombo, a malawi tinapanga mistake
@cassimyusuf6683
@cassimyusuf6683 Год назад
Kwathu kuja amene anatiloza akanatikhululukira 😢
@georgechikafutwa1334
@georgechikafutwa1334 Год назад
Akanatileka koma mfiti ameneyi😢😢😢
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 Год назад
Mwayi okwela ndege alibe kkkk
@user-ep7gu2td6y
@user-ep7gu2td6y Год назад
Koma nkhawa zanga ndi ndani yemwe angatipulutdr
@Shaabann
@Shaabann Год назад
Thanks God bless you
@dhaoudhiabedinegomaseko2363
Chakwera ndi anthu ake nzeru alibe ndipo kaya ndinene bwanji?pena ndimalakalaka ntakhala ujeni ndikuthana nawo andale opusawa
@eliaskachali-xn2ve
@eliaskachali-xn2ve 11 месяцев назад
Boma likulamulidwa ndi zigewenga chakwea ndiwakuba
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e 5 месяцев назад
President cakwera tidzamukumbukira kuti anali wakuba wakupha oononga.
@ziwani3682
@ziwani3682 Год назад
BIG 👍
@totaln12potchefstroom98
@totaln12potchefstroom98 Год назад
Chakwela ndi mbudzi😅
@giftgannet6871
@giftgannet6871 Год назад
Mumatha abwana awa anali ndani awa😂
@bayview4554
@bayview4554 Год назад
Bomali ndilasatanik coz ngongolezimenezo azabweza ndimagazi amalawi ndichifukwa akusowesa mankhwala zipatala ndi chakudya Kuti amalawi azimwalila azipeza ziwalo ndimagazi sure
@machonabanda5752
@machonabanda5752 Год назад
I think in future Malawi will be part of zambia because it's too much now
@user-dv7zg5vq7i
@user-dv7zg5vq7i Год назад
Ichi ndie ayi chichoked 😢😢
@jimmyharris1330
@jimmyharris1330 Год назад
Respect to you my brother
@rowanziya1561
@rowanziya1561 Год назад
Mmmm inupenapake paja Ndinu audf
@richmondkilembe5449
@richmondkilembe5449 Год назад
Chakera awononga ku malawi bwanji mulungu tutandizen tuuu koma ndalama zimenez abweza ndan kod 😢😢😢😢😢😢😢😢😢
@dilmayankam4052
@dilmayankam4052 Год назад
Sibola atsamundawo asatenge malo anga 😢ndikuopa
@Marialongwe-nzlib
@Marialongwe-nzlib Год назад
Tikusowa Mpapaya Mkumat Amakambilana Ndi Company zopanga Juice 😂😂
@MosesLusale
@MosesLusale Год назад
Koma ndiye Malawi tifapo 2 chifukwa anthu amenewa akungoba ndalama basi anyway big timakunyadirani
@user-yt2op5rl2q
@user-yt2op5rl2q Год назад
Kupempha like akupenpha chachikhumi ,he must go!!
@ibratime
@ibratime Год назад
Iyeyo anali mbusatu basi kenako president
@elidajuma5207
@elidajuma5207 Год назад
kutipweteketsa basi olo misewu ya mamidzimu osapalanso yakumbikakumbika nde ndalamazo akungodya kwawoko ayiwala kuti adzafunaso anthu
@sammyjonnes
@sammyjonnes Год назад
I wish to have chakweras number so that I can send this to him, # this is the most corrupt government in Africa
@wilsonmsoke2060
@wilsonmsoke2060 Год назад
Mumatha man keep it upp
@rabisonpias5131
@rabisonpias5131 Год назад
I used to LOVE Boma ili mbuyomo koma pano.. Aaaaaaaa Zosayenda uyu or atangoyerekeza kuyenda wapasi nditha kusanduka DAVID . mwala utha kugwira ntcito
@pastonmoda6588
@pastonmoda6588 Год назад
Akhululuke ndithu Chonde mulungu dalitsani Malawi
@patriciakenmuir
@patriciakenmuir Год назад
Muluzi anali makina mseu wathyolo mulanje its like built yesterday
@chrissygama8678
@chrissygama8678 Год назад
Kmans mumamunyoza kut sangapange kanthu koma mwamva lero zimene muluz anapanga ķwa anthu amene amazitsata
@ishmaelamadu6425
@ishmaelamadu6425 Год назад
Chakwera mtayeni opanda nzeru
@BizweckMasamba-pe5bu
@BizweckMasamba-pe5bu Год назад
Munthu wankulu ulemu wanu 👏👏👏
@user-rb6qo4my3r
@user-rb6qo4my3r Год назад
Anali mkulu wampingo uyu apite akatumikile nkhosa zake
@aggogokina8992
@aggogokina8992 Год назад
Kudzavuta kumuyiwala chakwera ndi team yake wagwiritsa a malawi mafuwa a moto kudzera mu bodza. Ndithu anthu awa palibe choti angapange choposa kupemphetsa nkumagawana ndalamazo mu team mwawo
@MacmillanMakombe-sz4iy
@MacmillanMakombe-sz4iy Год назад
Kkkkkkk koma ndasekaa kkkkkkkk
@sayidimisessa
@sayidimisessa Год назад
Program iyi imandisegula maso, ndikunditsuka ubongo
@issabwanali29
@issabwanali29 Год назад
Keep it up big
@Alu-v9x
@Alu-v9x Год назад
Simumati mukufuna kuona zina ndizimenezotu
@brightbautbright8028
@brightbautbright8028 Год назад
Ine sindizabweraso ku malawi kulimose kulimanda ku malawi ndizataniko ndizafe. Ndi njala ine ayi Malawi 🇲🇼 anavunda kwambir chakwara zeru alibe wawononga malawi
@ibrahimwezely-pn6te
@ibrahimwezely-pn6te Год назад
Kulimbana ndi chakwera bola kumwa temeki
@frezarphiri3480
@frezarphiri3480 Год назад
😂😂😂😂 ati kodi awa anari ndani ?? Yakho mulipeza nokha 😂
@mafukenimasangwi5487
@mafukenimasangwi5487 Год назад
Mwayi okwela dege analibe kkkk
@georgethole3813
@georgethole3813 Год назад
Ubulutu wa chakwera suzatha hahaha
@christopherbottoman9131
@christopherbottoman9131 Год назад
Big mumakwana koma ndaseka mpaka nthiti kuwawa🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 ndiye mwati chakwela amaganiza bwanji???? Eeeeeee
@chitimbethegreat-pc1bp
@chitimbethegreat-pc1bp Год назад
Ndinanena kale kuti mmutu mwa mkulu ameneyo muli mamina okhaokha komanso okuba ndalama za a Malawi
@ibratime
@ibratime Год назад
Chekwela ndi mbudzi yamunthu mutu wake sumakoka mutu mwake mawaya anaduka
@MaxBello-nc2gl
@MaxBello-nc2gl Год назад
Kodi awa adali ndani?
@user-ep7gu2td6y
@user-ep7gu2td6y Год назад
Koma nkhawa zanga ndi ndani yemwe angatipulutsr 2:43 2:46
@hopeskafumbiphiri6011
@hopeskafumbiphiri6011 Год назад
akungofuna ma angodya ndalama basi
@simonpaul6567
@simonpaul6567 Год назад
Please president chakwela leave presidency and go
@giftmapilaherbalist6803
@giftmapilaherbalist6803 Год назад
Tcheya mani wa anthu ovutikaa kkkkkk
@powercharios2087
@powercharios2087 Год назад
Chakwera asiya dziko la malawi lili pamoto
@gideonkella5451
@gideonkella5451 Год назад
Mnyamata wamzeru uyu, ulemu wanu
@DonaldchiefsonKamanga
@DonaldchiefsonKamanga Год назад
Kodi iwowo anali ndani kikkkkkkk
@bubakalimustafa
@bubakalimustafa Год назад
Thanks u boss
@icelenzoaustin9513
@icelenzoaustin9513 Год назад
Chakwera why 😢😢😢
@aufjames7377
@aufjames7377 Год назад
Chakwela ndi galu yamunthu
@victorbanda9039
@victorbanda9039 Год назад
Usaiwaletu Paja dpp yakoyo imanama kupereka ma figures ndipo ndalamaso paja amkangogawana pachilomwe pawo kumangopatsa muli ndalama azigulila gondolosi
@BladesBullets-pu5uw
@BladesBullets-pu5uw Год назад
Zoona m'bale siukunama koma ubwino wake tili nacho choloza chomwe pitalayo anachita, kusiyana ndi achakwera osabawa tikungoloza ngongole zokha basi.
@abumussah9766
@abumussah9766 Год назад
Is true he think like mana like time of Moses
@Razarusmbavachakwera
@Razarusmbavachakwera Год назад
Ngatikuli program yomwe imandinyasa ndimeneyi yokhuzana mcp ndachizawowa
@joicemartin-ji5zu
@joicemartin-ji5zu Год назад
Kkkkk k zoopsa abuse opanda nzeru okuba cisiru mbava yachabe chabe mbuya wakumidima okumwA MAGAZI
Далее
Faites comme moi
00:14
Просмотров 1,1 млн
Как подписать? 😂 #shorts
00:10
Просмотров 536 тыс.
Ngakhale mphamvu zimatha
5:29
Просмотров 4,8 тыс.
America inakhala bwanji Superpower
19:12
Просмотров 34 тыс.