Тёмный

Nkhanga zaona Chakwera. Mzimu wa Chilima ukwazuza 

Jay Kawere Mw
Подписаться 6 тыс.
Просмотров 46 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

25 июн 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 123   
@MoosaChirwa
@MoosaChirwa 2 дня назад
😂😂😂😂😂 vice President yemweyo kuvomelezana naye karindo kuti akunena zoona akusata malamulo amalawi akuti❤❤❤❤❤
@EmmanuelKaipa-rg1lj
@EmmanuelKaipa-rg1lj 3 дня назад
Ndpo ine tsiku singathe ndisanamve nkhanga zaona""""
@MadalitsoMugemezuru
@MadalitsoMugemezuru 3 дня назад
Mmativesa kukoma bwana ndichilungamo chanu
@HusseinMoffatt-mi1fl
@HusseinMoffatt-mi1fl 3 дня назад
Osadanda James tipha ameneyu tilikomkuno tibwanyula ameneyu
@user-wx1jt5fd2j
@user-wx1jt5fd2j 2 дня назад
Ambuye akuchizeni ndi zanja lake lamphamvu
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 2 дня назад
apolice army ndizitsiru zanthu chakwera pantumbo pa make ndithu satana chigawenga cha chikhrisitu
@CharlesmakveliNyirenda
@CharlesmakveliNyirenda 3 дня назад
Uyu chakwela watikwana khope kunyasa ngati ku matako kwa chi zikhale ng'oma
@madalitsomisomalih5411
@madalitsomisomalih5411 3 дня назад
Azangofa ulele ameneyo this is south africa
@kumbukanimasonga4770
@kumbukanimasonga4770 3 дня назад
Keep on updating us Mtanyiwa
@SteveTigu
@SteveTigu 3 дня назад
🎉🎉🎉🎉🎉🎉 More 🔥
@user-nf3ik3ff6y
@user-nf3ik3ff6y 2 дня назад
Chakwela you mast go watikwana
@user-wl4nd7ic1s
@user-wl4nd7ic1s 3 дня назад
Don't warry your being protected, by blood of Jesus!!!
@ThokozaniSaiti
@ThokozaniSaiti 2 дня назад
May the good Lord protect you mr Munthanyiwa and God will fight all your battles All the hidden will be out ndipo nonse munya mubweza one by one
@user-rz8qp8tj8e
@user-rz8qp8tj8e 2 дня назад
2025 woza ku Malawi tipanga ngati kenya nyawo kwawo 😂😂😂
@WezzieChimuzi-ek7bk
@WezzieChimuzi-ek7bk 3 дня назад
Takulandilani Mr Mtanyiwa kuno ku Botswana koma pepani wa zifuwa
@user-yo9rw8tr4s
@user-yo9rw8tr4s 3 дня назад
Makwana big beg up
@DickisonyusufChiwalo2
@DickisonyusufChiwalo2 3 дня назад
Ws missing u brother
@DuntumaziyaDuntumaziya
@DuntumaziyaDuntumaziya 3 дня назад
Boma lizunzika kwambiri
@user-mk9ro8fd4u
@user-mk9ro8fd4u 3 дня назад
We're with you comrede
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 2 дня назад
Big alike cape Town yo tatitumiziren number
@madalitsomisomalih5411
@madalitsomisomalih5411 3 дня назад
Boma la malawi likusewelesa ndalama powapasa anthu azifwamba chonsecho anthu akuvutika kwambili kumalawi shame on u guys .
@GraceZumazuma
@GraceZumazuma 2 дня назад
We are praying for you comrade tikufuna zinsisnsi za imfa ya chilima ibwele poyera ,may God keep you safe
@meganabigail-ye7fw
@meganabigail-ye7fw 2 дня назад
Ambuye ayime ndi Brian koma so Cathy musalole kupusisidwa kumwamba kukuyang'anileni
@PatrickMailos
@PatrickMailos 2 дня назад
Ntanyiwa osadandaula ayi ifeso timakhala komkuno ku Cape town see point tipha ameneyu
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j 3 дня назад
Bwana wanga nyimbo iyo ndani anayiba ili koyambirira
@JayKawereMw
@JayKawereMw 3 дня назад
Nyimbo tiyiponya popano masana uno
@witneymunthali8371
@witneymunthali8371 2 дня назад
Mulungu anapambanisa David nkhondo Aimanso pa a Malawi.
@CharlesmakveliNyirenda
@CharlesmakveliNyirenda 3 дня назад
Kodi chakwela iwe misala imabwera chifukwa cho koko nyemba ya Monica first lady kapena bwanji
@MaryAaron-nn8ec
@MaryAaron-nn8ec 2 дня назад
😂😂😂😂
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 2 дня назад
You are cursed ndiwe wovesa chisoni, iwe ndi ana ako ndinu otembeleredwa.
@MacleanKwacha
@MacleanKwacha 3 дня назад
Inesotu ndine mmodzi wa Malawi first.
@kennethkaunda3636
@kennethkaunda3636 2 дня назад
I love this type of humanity ❤❤
@user-xx4jb9se3z
@user-xx4jb9se3z 2 дня назад
God is with you Mr mtanyiwa .asiyeni awa mcp ikupita basi
@KhareedOsman
@KhareedOsman 3 дня назад
Cape Town, see point
@AbdullahSaeed-tg1cm
@AbdullahSaeed-tg1cm 2 дня назад
Welcome back buddy.... missing u ❤
@promixphotography8056
@promixphotography8056 3 дня назад
Manganya is talking truth and we have to capture because if we fail tidibwa sure
@DoreenEmmanuelj
@DoreenEmmanuelj 3 дня назад
Pepani muchira bwana
@user-hx6jl2jq9j
@user-hx6jl2jq9j 3 дня назад
Koma tiphana chakwera uli kunva. Iwe uli kuno sth africa tkulonda zivute zitani komanso tithana nawe.ukufuna usokoneza mntanyiwa
@FrankAdonis-zl6qc
@FrankAdonis-zl6qc 2 дня назад
Ofunika aphedwe tipatseni map timakhala cape Town muno
@DoreenEmmanuelj
@DoreenEmmanuelj 3 дня назад
I missing you dear❤
@HarrisAckim
@HarrisAckim 3 дня назад
Ys
@chimwemwenkute3839
@chimwemwenkute3839 2 дня назад
We're always proud of you bwana mtanyiwa comred
@PrinceBlessings-bv5bs
@PrinceBlessings-bv5bs 2 дня назад
Tili Nanu mn ife tikufuna chilungamo
@DanielBeston-xo9fv
@DanielBeston-xo9fv 2 дня назад
Kun ku ndix tikumvela Limpopo fm
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 2 дня назад
Ambuye akuchiritsen mukuimira dziko❤
@NomvelisoMnguni
@NomvelisoMnguni 2 дня назад
Umatiyimirira ntanyiwa❤
@zimmekapachika6784
@zimmekapachika6784 2 дня назад
Iwe ndi galu okoba Osama bin laden mfiti yokupha osowa mtendere sunati iwenso 2025 sutiwonayi okupha iwe
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 2 дня назад
Ifeyo big tinabadwa kotana ndiadani
@AkayikosyagaMarsha
@AkayikosyagaMarsha 2 дня назад
We are waiting for them no nyumwitsa
@JelemiaMaseko-tn5sb
@JelemiaMaseko-tn5sb День назад
Koma amalawi mkafuna kupaka zitosi munthu osalakwa mmatha chakwera zikumukhudza ndi chani
@LuciasSimione
@LuciasSimione День назад
Maso ngati abaya ndizingano taonani taonani 😅😅😅
@LeonardWalinga
@LeonardWalinga 2 дня назад
MALAWI AKUPITA KUTI KODI GUYS😢
@user-wg8tp8in1v
@user-wg8tp8in1v 2 дня назад
Koma inu pena pake ndikuwona ngat munangodana nd Chakwela. Kodi zimenezi zot Chakwela wapanga ichi daily zitipundulila chani amalwi. Kondi simukutizala mtima wankhaza mumitamu? Pena pake ndikuwona ngat mukukolezela kut anthu azipanga zosokoneza Kumalawi. Tatiuzeniko zazipani zina kut tinkhale ndi picture yoyenela yazipani zonse kut povota tizavote mwa nzeru. Ndi dzina zomwe zingathe kusintha myoyo yathu.
@godfreymbelele6166
@godfreymbelele6166 2 дня назад
Koma akutumaniwo Ali pa chintchito choyipitsa ena. Ndege ikaphulitsidwa imaoneka chonchija? Ukuti yaphulutsidwa koma onse osafa ndiye mumakong'ontha kuti afe enawo kupha umboni ukuuza ana? Ukundiuza kuti ndege imeneija inatera pa malo ngati ameneaja? Mwafatsakotu ku Botswana ko mpaka mumalankhula ngati wokhudzika ukufuna kugwetsa wina. Guys olo mutaipitsa chotani ngati MCP ikudzawina idzawinabe mufune musafune chifukwa ifenso we have the brains to reason. Keep on decampaigning MCP but the results will be against your will and that will bring instability to this beautiful nation.
@maxwellchilima5440
@maxwellchilima5440 3 дня назад
Mumangolankhula kuli kutali olimba mtima amayamayankhula ayi kuno
@HarrisAckim
@HarrisAckim 3 дня назад
Owoo
@mosesnyirenda5010
@mosesnyirenda5010 2 дня назад
Man pitiliza umakwana
@GanizaniKamvazaana
@GanizaniKamvazaana 2 дня назад
Ndi chitsiru ameneyo ngopusa tangomutsirani moto amenewo ngopusa kwambiri chitsiru Tathawa ekha ameneyo adzipita kumalawiko akaone zopusa zomwe athuwo akupanga chitsiru kwambiri ameneyo
@BeatriceRobert-jq6ci
@BeatriceRobert-jq6ci 2 дня назад
Akupatsani chibans 😂
@DoreenEmmanuelj
@DoreenEmmanuelj 3 дня назад
Kkkkkk mukukwanira
@victorauwana7258
@victorauwana7258 2 дня назад
Antanyiwa i follow u all time.. do you remember munati muli ndi ma information angazi ? Now mukufuna mutipase ma number anu tikupaseni ma information?
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 2 дня назад
This guy is mad... he is doing this for nothing.. how much are you pocketing mntanyiwa to do this?
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw 2 дня назад
Pepani a mtanyiwa muchile mwansanga ,,,takulandilani kuno ku Botswana
@user-xy4hq6sx7v
@user-xy4hq6sx7v 2 дня назад
Mulungu oziwa kuteteza azikutetezani
@JaxyKumwenda
@JaxyKumwenda 2 дня назад
Mumatiyimilira bwana
@MuhammadSamson-yz1kl
@MuhammadSamson-yz1kl 2 дня назад
Comrade sangakugwire ife tilikonkuno asiyen abwere kuno ngati angabwelere wamoyo kunoko siku Malawi kuno umuuze abwere Nda asilikali omwe onse tiwaphera konkuno
@LysonMtalika-tb6fk
@LysonMtalika-tb6fk 2 дня назад
Zomvetsa chisoni muboma ili la MCP
@MeniyaMikaya
@MeniyaMikaya 2 дня назад
Awa akuchitatu misala ndithu sure aaa km anthu ngati mukunamizana kt 2025 boma mukutenga ndinkhalamba yanu ija mukunama mcp 2030 wooooooooooooo🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@GiftJulius-gx2kb
@GiftJulius-gx2kb 2 дня назад
Ndiwe mbuzi sumaganizila anthu ena ndi mcp yako
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 2 дня назад
Ukunama ase
@Creslevison-vj2sl
@Creslevison-vj2sl 2 дня назад
Mbuzi yamunthu ase
@petertaulo
@petertaulo День назад
Mukuchedwatu
@user-wi9pe2hz7e
@user-wi9pe2hz7e 2 дня назад
Bas musiyen munthu apume😅
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 2 дня назад
Abambo inu a bodza loopsya.. kodi mukupasidwa zingati? Ayi mulemera nawo ma bodzawo ndipo nde mukuyesetsa
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 2 дня назад
Komatu amene akufuna kupanga chipongwe anthanyiwa atsazikiletu ku banja lake komanso akozeletu siwa akwawo asananyamuke chifukwa akufuna kutsata anthu 8 aja ..... omwe boma linawapanga nkhazza. Komanso samalawi okha amene akumuyang'anila mthanyiwa Amazulu,mavenda makhoza komanso masutu kkkkkkk ndeno obwela pafupi ndi Limpopo mw fm alimbe ⚒😜☠☠☠💀
@MiracleMalichi
@MiracleMalichi 2 дня назад
Sakanamupha nzake adalakwanji chilima Mzimu wa chilima umufyanthee chakwera asiye naye kumukwera Monica wakeyo bolo yake
@user-bt3me2pn5q
@user-bt3me2pn5q 2 дня назад
koma munthuyu kwathu asabweleko ndikapha Ngati njoka manyi Ake chakwelayu😮😮😮😮😮
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 2 дня назад
Anyaaaa zifwamba zikufuna zibise chilungamo
@user-db3mh9wr9v
@user-db3mh9wr9v 2 дня назад
Chakwera machende amako galu iwe ndipo 2025 ikuchedwa mboliyako
@HenderesoniNdau
@HenderesoniNdau 2 дня назад
Tiuzeni zoona
@BeatriceRobert-jq6ci
@BeatriceRobert-jq6ci 2 дня назад
Zikomo kwambiri achimwene ambuye akufungatireni ndimapiko ake ndalama akupatsa anthu zo moti azithandiza Ana am asiye or azigogo mizimo koma abale
@staceycossam5933
@staceycossam5933 День назад
Let them come
@amosnyirenda-pl1ss
@amosnyirenda-pl1ss 2 дня назад
chisilu chamunthu iwe unamize ana ako
@JafaliAkimu-ll1bf
@JafaliAkimu-ll1bf 2 дня назад
mfiti iyi chigawenga chitsiru chigawenga cha chikhrisitu kubisala ku ubusa machende amake
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 2 дня назад
Apa zakhala bwino aliyense waziwona yekha kuyipa kwa MCP.
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r 2 дня назад
Inu anthu opanda umboni ndi amene mukuzuzika mumtima chifukwa zomwe mukufuna sizikuchitika ndiye mukhalila yomweyo 😅😅😅😅😅 keep it up Ngati satana wanuyo akukupatsani chipulumutso 😂😂😂😂😂😂 mbuli za mmalawi muno ndi zimenezo kuphatikizapo ma prophet 😅😅😅a ndale
@JosephMwambe-rz2oy
@JosephMwambe-rz2oy День назад
Iwe pangopamako awamvakaziziiwe mboliyamakonso ukakhalawina usalembenso umbon wake wakunyelo kwamako ukasuzumile kunyelo kwamakoko ukapezako umbon ukufunako kazz iwe
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r День назад
@@JosephMwambe-rz2oy ukolola zomwezo nthawi yako ikafika yopita kumanda kkkkkkkk tulutsa umboni mupite nawo ku Court basi osati kutulwana munthu sakufa ndi kutukwanidwa palibe comwe wapindula lapa msanga tsiku lako lisanafike ngati chilima ambuye akusalitse I love you sweetheart
@user-ky2fs3zr8y
@user-ky2fs3zr8y 2 дня назад
Sea point kkkkkkk
@AlbertDuke-of9nn
@AlbertDuke-of9nn 2 дня назад
😮😢
@EmmanuelKaipa-rg1lj
@EmmanuelKaipa-rg1lj 3 дня назад
Nyimbo yokhayo eee palibenso
@amosnyirenda-pl1ss
@amosnyirenda-pl1ss 2 дня назад
chi lima si baliwakeo iwe usamusewelese
@GodfreyMitiyani
@GodfreyMitiyani 2 дня назад
Mbambande
@owenmoses9434
@owenmoses9434 3 дня назад
Komatu ka music 😮 kali bho heavy absalom😢
@TressLuka
@TressLuka 3 дня назад
Mumatiimiliraaa😢😅😅😅
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 дня назад
Antanyiwa mwasala pang ono kulangidwa nmulungu mabozawo musiye mulungu wakwiya ndi maboza anuwo mulungu simtanyiwa ayi mau wogothawo anthelathu mlape
@meganabigail-ye7fw
@meganabigail-ye7fw 2 дня назад
Munya nonse a Mcp kuphatikiza ndi president wanuyo mumaona ngati kupha munthu chophweka Muziona ngati si iwe yembekeza Ana kapena azukulu ako they will be in for it, Mwazi mwazi mwazi n mwazi again every where mukuona ngati mulungu angakondwe nazo.
@LeendaDeborah2005
@LeendaDeborah2005 2 дня назад
@@meganabigail-ye7fwexactly
@ShmazLodney
@ShmazLodney 9 часов назад
Nanunso fundo zanu zauchinsilizo pano ayi kapenamuli gulu lokupha nawo
@dicksonmlera2777
@dicksonmlera2777 3 дня назад
Ndikufuna yemwe anayimba nyimbo yomwe ili koyambilirayi
@JayKawereMw
@JayKawereMw 3 дня назад
Tikuponyeran nyimboyo masana pano
@dicksonmlera2777
@dicksonmlera2777 3 дня назад
@@JayKawereMw thanks brother
@JayKawereMw
@JayKawereMw 2 дня назад
Nyimbo ndaponya ku channel kuno
@dicksonmlera2777
@dicksonmlera2777 2 дня назад
@@JayKawereMw ilipatipo man?
@JayKawereMw
@JayKawereMw 2 дня назад
@@dicksonmlera2777 taonani ku ma video apangidwa upload lero yalembedwa ndani sanalire and wafela chipululu
@BeatriceRobert-jq6ci
@BeatriceRobert-jq6ci 2 дня назад
😂
@MeniyaMikaya
@MeniyaMikaya 2 дня назад
Mmalawi wopusa atha kutelo km woganiza bwino galu ndimtanyiwayi amabweletsa nkhani za bodza chitsilu chamunthu ichi iyeyo osangotulitsa umboni wakew bwanji ? Kd atakhala mb'ale wake bwezi angoyankhula zopusaz ? Km ameneyi ndichitsilu kwabas akuuza mbuzi za anthu ndipo mulungu amukanthe iyeyi
@Macrina-vv3us
@Macrina-vv3us 2 дня назад
Gule kwao iwenso ndichitsiru kwambiri imfa imene ija ndiyoti wina adzibwera mkmayankhula mopusa apapa
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 2 дня назад
Mkulimbana ndi chakwela amene anapha chilima ali pheeee kufuna kuyipisa mcp wokufa saziwika inuso mkhoza kufa tisayiwale kuti kuli mulungu amene akufunila zoipa mzako mulungu amabwezela nkhondoyi siyanthu ndiyamulungu
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 2 дня назад
Ona polekela
@yamikanichinganyama6607
@yamikanichinganyama6607 2 дня назад
NTHAWI A REF, NANU INGOTIPASANI MA VIDEOS AJA MUMATI MUKUSUNGA AJA
@JayKawereMw
@JayKawereMw 2 дня назад
Akudikira umboni wa boma
@sedicmuzammil8530
@sedicmuzammil8530 2 дня назад
@malawi tiyeni panseu...lets do it like kenya
@edwinchipikamtambo6686
@edwinchipikamtambo6686 2 дня назад
yambitsa tilipambutopo
@user-yc6wr6ui6b
@user-yc6wr6ui6b 2 дня назад
True
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc 2 дня назад
Useless government
@MeckMdoma
@MeckMdoma 7 часов назад
Za ziiiiiii angamvere ndani zimenezo? Mudzakhumudwa 2025. Musaone ngati aliyese ndiopanda nzeru ngati inu
@JelemiaMaseko-tn5sb
@JelemiaMaseko-tn5sb День назад
Garu iwe unamva kuti wakufa ndi wamoyo amayankhulana wamisala iwe mulungu wake utiyo chisiru cheni cheni ndipo uzakhala chisiru mpaka kale munthu otembeleledwa iwe kaguru kofuna kuukira ndi kulanda boma mwaupandu pogwilitsa ntchito anthu osazindikira Kodi foni yanji yosunga 25 m kkkkkkkkk umbuli ndi matenda chisiru iwe nde ukuona ndani angakujoine ndi kalindo wakoyo mbamva inu kalindo amangofuna kutibera misonkho yathu pogwilitsa ntchito fake news zomwe zamveka ngati zoona cholinga boma pozisungila ulemu azimpasa ndalama agaru inu akuba ndinu nde sikuti uzinyozesa malemu chilima koma ulindizimu iwe uziti chilima spirit ikufungatila osati mulungu uzimvere chisoni ukuputa mkwiyo wa mulungu chisiru muuzane ndi nkhululu zakozo
@LilyMbewe
@LilyMbewe День назад
Hahaha ndi inu modzi okudya ndalama za chakwera eti,?mutu ako sukigwira upenga unya manya uonaso sunati kulira, leka kumvela ndikumupanga follow basi, galu chule iwe😊
Далее
LIMPOPO FM WITH COMRADE NTANYIWA
41:25
Просмотров 2,6 тыс.
He turned a baseball into a stylish shoe😱
00:59
Просмотров 534 тыс.
A Simbi Phiri Akhuza Imfa ya Dr. Saulos Klaus Chilima
22:44
BON KALINDO LERO PA 28 JUNE NDETU KULI NKHANI |
17:01
Oyimba Omwe Amayimba Mosiyana Ndi Ena Onse
7:12
Просмотров 2,2 тыс.
Chimtengera - Iwe Malawi (Stool Session)
8:42
Просмотров 3,8 тыс.
Asilikali akuulula momwe anamuphera Chilima
3:23
Просмотров 74 тыс.
Pwedo at it again! School Days crew
5:46
Просмотров 547