Тёмный
No video :(

Nkhanga zaona Chakwera watumiza Asilikali kuti Akamuphe Peter Muthalika lero. 

Jay Kawere Mw
Подписаться 16 тыс.
Просмотров 102 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

12 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 436   
@johnmpatama1461
@johnmpatama1461 26 дней назад
This is the beginning of the end of Chakwera government.
@user-mr2mh4gq8w
@user-mr2mh4gq8w 26 дней назад
AMbuye mutisogolere Peter ndi salimo 91 ambuye mupase I mzimu wachiziwitso
@user-ev6bi7jr7g
@user-ev6bi7jr7g 26 дней назад
Ndiye MCP tikuidziwa ife ndimeneyo ndale zake ndi zakupha
@stephankamyata3862
@stephankamyata3862 26 дней назад
Achisale pls motsongozedwa ndambuye protect our APM
@augustMag
@augustMag 26 дней назад
Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥
@miketholiwa1762
@miketholiwa1762 25 дней назад
Asamale kwambiribe koma
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 дней назад
Eti
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 17 дней назад
@@augustMag ndipo kwambiri tu mmm
@BrownMainje-sh7hj
@BrownMainje-sh7hj 26 дней назад
Shame on MCP
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb
@ExcitedBreakingWaves-oh3zb 26 дней назад
Ngati iyeyo akuphanso Pieter nayenso ayenera kusogozana naye.
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 дней назад
Ndipo kwambiri tu mmm
@MayamikoBanda-jh8bn
@MayamikoBanda-jh8bn 26 дней назад
I love the way momwe mumachenjeza Malawi kwa zigawenga . Ndiye nimamutsatilani kwambiri pa RU-vid Kono ku Zambia
@MaggieMujuma
@MaggieMujuma 26 дней назад
Eeeee mayo ndalama yanga ine Peter munthalika iwe ndi Wilson msemanjira iwe anthu okuba inu
@chimeraJonathan
@chimeraJonathan 24 дня назад
L
@AiameAdamo-su1nt
@AiameAdamo-su1nt 26 дней назад
I'm here following you step by step each and everyday.
@PhilipMatolino
@PhilipMatolino 26 дней назад
Kom guyz chakwera khani ndiyotu wina kungofanso kukhala ma demo anyooo!! Mwatitola mcp kwambiri
@cynthiakananji1608
@cynthiakananji1608 26 дней назад
Ndipo apitilira Aku Kenya kuvutatu owo
@KhalideNerve-mu1eq
@KhalideNerve-mu1eq 26 дней назад
Mission impossible God is watching 😢
@KennedyPhiri-h9h
@KennedyPhiri-h9h 26 дней назад
Thanks for your information Mr Limpopo FM 🙏 we always with you
@louisgolden
@louisgolden 26 дней назад
May Allah protect APM
@user-ew4dm8yy3b
@user-ew4dm8yy3b 26 дней назад
Achisale motsogozedwa nd mulungu please protect apm
@chrisschikozera7271
@chrisschikozera7271 26 дней назад
That's end of mcp in this country again.....God ll protect Amp
@lovenessmuthiya3513
@lovenessmuthiya3513 26 дней назад
May God protect APM
@user-be5fc3ed1i
@user-be5fc3ed1i 26 дней назад
Nyimbo imeneyo ntanyiwa ukamabwera pa Limpopo FM usayisiye chonde Limpopo FM moto kuti buuu 🔥🔥 🔥🔥🔥
@JosephyMakunganya
@JosephyMakunganya 26 дней назад
Apa ndiye alimbana ndi achina chisale 🔥🔥 Malawi wafika posauzana
@CharlesMaloya
@CharlesMaloya 26 дней назад
Chakwela and Rwanda foreigner based in Malawi you will get what you want warning to Rwanda you will see
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 26 дней назад
APM SANGAPITE NGATI CHIWETO .YEMWE UJA MUNAPANGA UJA BANSI .. APM ATUPELE CHIHANA ANTHU AWAWA SANGAPANFIDWE NTINTINI NEVER
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 дней назад
Eti
@AjibuTwalibu
@AjibuTwalibu 26 дней назад
Mwachita bwino Comrade mtanyiwa Tili nawenawe sitingakutaye
@RobertNedson
@RobertNedson 10 часов назад
Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏
@AlexMbewe-p7y
@AlexMbewe-p7y 26 дней назад
NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 26 дней назад
Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse
@StelliaSangaya
@StelliaSangaya 22 дня назад
Zoonad
@Emmanuelisraelsimbi
@Emmanuelisraelsimbi 26 дней назад
Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys
@user-dn3gp6yi4y
@user-dn3gp6yi4y 26 дней назад
Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo
@VeronicaChirwa-ct4os
@VeronicaChirwa-ct4os 26 дней назад
Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera
@HamzaMkwanda-bh8dc
@HamzaMkwanda-bh8dc 26 дней назад
We don't have any police in our country
@ChifundoNinje
@ChifundoNinje 26 дней назад
Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam
@preciouskadembo1932
@preciouskadembo1932 26 дней назад
Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva
@user-tw2zf7bj3e
@user-tw2zf7bj3e 26 дней назад
May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina
@AndrewDinala-d9j
@AndrewDinala-d9j 26 дней назад
Yes
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 26 дней назад
In Jesus name, God protect APM
@PeterJames-i8y
@PeterJames-i8y 26 дней назад
Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.
@VungaQueen
@VungaQueen 26 дней назад
Amen ❤❤
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 26 дней назад
Amen
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 20 дней назад
Amen
@salimmkumakumakitombi-yc7pw
@salimmkumakumakitombi-yc7pw 26 дней назад
Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate
@harrietmkusangombe
@harrietmkusangombe 26 дней назад
God have mercy on our country
@AhmadShariff-bk3rr
@AhmadShariff-bk3rr 26 дней назад
Mission impossible
@OnenessLestas
@OnenessLestas 26 дней назад
Zamaboza basi mulungu akuwoneni
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 26 дней назад
Prayer Malawi
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w 26 дней назад
End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.
@IbrahimPhiri-ky5jk
@IbrahimPhiri-ky5jk 26 дней назад
Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o 26 дней назад
Lord have mercy on us
@wangachindeya8577
@wangachindeya8577 26 дней назад
Amen
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r 26 дней назад
Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa
@PatrickSomanje
@PatrickSomanje 26 дней назад
I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r 26 дней назад
Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo
@GRACIOUSKENAN
@GRACIOUSKENAN 25 дней назад
Ntanyiwa ndiwe one, continue ,tilibe asilikali angakhale police, kulibe ndattttiii aaaaaaa !!!!!! Agalu alipowo ntchito ndi zigololo bas😰😭😭
@vituveggah7619
@vituveggah7619 26 дней назад
Osazamuphwekesa comrade
@AndrewChilambo
@AndrewChilambo 26 дней назад
Antanyiwa pitilizani kuchenjeza amalawi zazigawenga za mcp
@AiwaMedia-sh6vx
@AiwaMedia-sh6vx 26 дней назад
Limpopo FM and BAKILI MULUZI TV mukuyesetsa ndithu kutitsegula mmaso koma amene alikutsogolo kwathu n'gokhumudwitsa. A Opposition aliko????
@GrinTemboh
@GrinTemboh 26 дней назад
Continue with good news we always listen u ukutimvetsa kukoma ntanyiwa
@benjaminjobo3525
@benjaminjobo3525 26 дней назад
Nyimboyi ndaikonda Antanyiwa cain ndi abelo
@tiwongehojaney5873
@tiwongehojaney5873 25 дней назад
God will protect Peter ❤❤❤😢😢
@ThivadoartistDyson
@ThivadoartistDyson 26 дней назад
Akangopha peter l tell you chakwela we come by the trip cross the country kukathana ndi iweyo alu continue.
@user-ky4ce9gb6j
@user-ky4ce9gb6j 25 дней назад
Ndipo kwambiri tu mmm
@kennethkaunda3636
@kennethkaunda3636 26 дней назад
Can I come to Malawi and show my position to chakwera government?
@user-sw8bb3iz7x
@user-sw8bb3iz7x 25 дней назад
God protect APM
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 26 дней назад
Yoo alipachintchito eti
@BlessMnyenyembe
@BlessMnyenyembe 26 дней назад
Thanks
@AllanKamphata
@AllanKamphata 26 дней назад
Mwasowa nkhani, akaphe nkhalamba ngati imeneyi
@BenPhillip-fw8hi
@BenPhillip-fw8hi 26 дней назад
Mmmm
@FrolenceKochelannkhata
@FrolenceKochelannkhata 26 дней назад
Ndipo inu!mabodza basi
@user-vq5fe6mo6o
@user-vq5fe6mo6o 20 дней назад
Nipamene wina akt chakwera 😢😢koma zowawa izi menyeren nkhondo Ambuye titan padziko pano
@UsenLashid
@UsenLashid 26 дней назад
Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus
@MatemangaMoyo
@MatemangaMoyo 26 дней назад
Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali
@Janaphiri
@Janaphiri 26 дней назад
Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji? Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti
@user-mi2xf3sw1i
@user-mi2xf3sw1i 26 дней назад
Ku kholo kwa amako wamva
@dalitson3558
@dalitson3558 26 дней назад
Pantumbo pa mayi wako galu iwe
@WisdomMaseko-fi5sv
@WisdomMaseko-fi5sv 26 дней назад
Koma mtanyiwa ndi masewero ako ukuzuza anthu kwabasi ona ena ayamba kale kupempherera APM kkkkk
@kensonmbewe6692
@kensonmbewe6692 24 дня назад
I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad
@nyanguoipa6996
@nyanguoipa6996 26 дней назад
Anthu amenewo asamale mangochi sigawa ma sweet
@AREFRIEDNELSON
@AREFRIEDNELSON 26 дней назад
MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara
@ChristopherManase-s1f
@ChristopherManase-s1f 26 дней назад
Eeeee koma ma cadet muli pa ntchito. Kkkkkk
@adrianobrigida3402
@adrianobrigida3402 26 дней назад
Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.
@kidneyblessingschilinguloj7292
@kidneyblessingschilinguloj7292 26 дней назад
Keep it up
@piliranimalama6090
@piliranimalama6090 26 дней назад
Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza
@FamousJohnathan
@FamousJohnathan 26 дней назад
Yanjiru simatani..?
@WilliamMasauko-su1wx
@WilliamMasauko-su1wx 26 дней назад
Siiswa
@JohnFrank-g6e
@JohnFrank-g6e 14 дней назад
Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus
@macdonaldkorea2928
@macdonaldkorea2928 26 дней назад
Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi) Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA
@cliftondad3816
@cliftondad3816 24 дня назад
Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza
@user-od6eo5zc4h
@user-od6eo5zc4h 26 дней назад
Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye
@christophergibson72
@christophergibson72 26 дней назад
Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi
@JosephyMakunganya
@JosephyMakunganya 26 дней назад
Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko
@EliasKawuwa
@EliasKawuwa 26 дней назад
A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo
@user-gd6zb2bv8f
@user-gd6zb2bv8f 24 дня назад
CHAKWERA tamachita manyazi zinazi popanga, nawenso Manganya ndiwe katukule, Mulungu wakumwamba, achite nanu mwapadera ndipo asakusiyani chonchi
@patrickkusailemp3769
@patrickkusailemp3769 26 дней назад
Longlive APM ..God is in control !!
@ibrahimalex7137
@ibrahimalex7137 26 дней назад
We're here my brother ❤
@MalawianMediafm97
@MalawianMediafm97 26 дней назад
🤣🤣🤣🤣 this is Comred ntanyiwa on Lipompo FM
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv
@AbdulmajeedJbanda-oz3jv 26 дней назад
Timakunyadilani big
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj 26 дней назад
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏yomweyo chikangawa
@GodifureRifa
@GodifureRifa 25 дней назад
Mulungu mumutetezere peter muthalika kulikose komwe apita 🙏🙏🙏
@SmileMalanda
@SmileMalanda 26 дней назад
Akuluwa misala chani kapena mwaz wachilima nd anthu ena aja zikuwazunguza😂😂😂
@NDIZOTHEKABANDA
@NDIZOTHEKABANDA 26 дней назад
Mabozatu amenewo
@mellipherjohn7158
@mellipherjohn7158 26 дней назад
mumakwana bwana wanthuu🎉🎉🎉
@marryphili5419
@marryphili5419 24 дня назад
Shame you chakwera fiti Yopanda manyazi wunapha chilima Pano wayamba kusaka Peter wupha anthu angati iwe
@AgnessMita
@AgnessMita 25 дней назад
Ambuye akutetezeleni APM
@MaureenBanda-t2q
@MaureenBanda-t2q 26 дней назад
Asiyeni akafa ndiiwowo ili ndi dziko
@user-gm3cx2xn9o
@user-gm3cx2xn9o 23 дня назад
Inu anthu akungofuna kutchuka ndiye inu muli busy 😂😂😂😂😂
@BenjaminCharlie-md3fk
@BenjaminCharlie-md3fk 22 дня назад
Umakwana ntanyiwa koma akangopha muntalika nafe tipha ndimiyala chakwerayo
@GraceMbengo
@GraceMbengo 25 дней назад
We pray for God's intervention. Mission iyi Ambuye alowererepo.
@chadreckchibwithala1493
@chadreckchibwithala1493 26 дней назад
koma mmm ntanyiwa boza ngati mnthu wa nkazi aaaa mnthu oti si wa dpp akagula ticket mnthu wachilendo aaa
@kangungufoundation2020
@kangungufoundation2020 25 дней назад
Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing
@user-uk1tt7ho9t
@user-uk1tt7ho9t 26 дней назад
May Lord for everything please protect our beloved president
@CatherineDesire
@CatherineDesire 22 дня назад
Asilikali nanuso bwanji otsangomupha iyeyo wakutumani Kodi anzako sakufuna moyo
@JabiluWaiti
@JabiluWaiti 25 дней назад
Mmmm koma akachoka kwa Peter abwera kwa inu a UDF inunso mukuyenera kukhala osamala
@user-kc7sd3te3d
@user-kc7sd3te3d 26 дней назад
Kodi asirikali athu bwanji ku Malawi uko mwangokhala pheeee 😂😂😂
@gladysbonongwe1038
@gladysbonongwe1038 26 дней назад
Kulandira ndalama
@CharlesMaloya
@CharlesMaloya 26 дней назад
Adadya chimbanzi
@user-zs7yq3tj7n
@user-zs7yq3tj7n 26 дней назад
Asiya chilungamo asogoza ndalama.
@patrickndojime1632
@patrickndojime1632 26 дней назад
Koma aPrasident opuma ananenatu kuti Doom sumafayira mkamwatu ndizitu pano tubwelera ku ulamuliro wa chipani chimodzi
@user-gm3cx2xn9o
@user-gm3cx2xn9o 23 дня назад
Anthu akamatenthedwa zolankhula zake zimakhala ngati zingatheke 😂😂😂😂 mulira simunati
@user-je6wk8ew6g
@user-je6wk8ew6g 26 дней назад
Moti chikangawa yalusa sikugawanso masweet 🤣🤣🤣🤣 atimaliza
@MuhammadBAKILI-kl2mj
@MuhammadBAKILI-kl2mj 26 дней назад
My bsst ladio station limpopo
@user-bh2ei4os8w
@user-bh2ei4os8w 26 дней назад
Iyiyi ndiye akufuna Kenya Kenya tsopano 🏹🏹🏹
Далее
MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSI
40:43
ПОМОГЛА НАЗЫВАЕТСЯ😂
00:20
Просмотров 6 млн
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔
20:45
Просмотров 63 тыс.
Amalawi ndi mbuli, asiye kudzudzula Chakwera;
7:24
Просмотров 64 тыс.