Тёмный

Omwalira apezeka wa moyo 

Malawi Lovers 🇲🇼
Подписаться 23 тыс.
Просмотров 70 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

2 сен 2023

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 68   
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 3 месяца назад
Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni
@user-yy6rj5lc4i
@user-yy6rj5lc4i 10 месяцев назад
Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri
@IvvyMakuluni
@IvvyMakuluni 10 месяцев назад
Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂
@user-lc7ji1gn9w
@user-lc7ji1gn9w 10 месяцев назад
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka
@nimrodkapingatheu5475
@nimrodkapingatheu5475 23 дня назад
Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....
@user-eu9xe6wl8b
@user-eu9xe6wl8b 9 месяцев назад
Great work prophet❤🎉
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx 10 месяцев назад
Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ
@user-lz1ry1sm4j
@user-lz1ry1sm4j 8 месяцев назад
Too bad. The name of the Lord is a strong tower
@Felix-ln4ql
@Felix-ln4ql 12 дней назад
Koma padziko pano pakuchitika zinthu eeh ndagoma
@JosophineSolobala-hp5ds
@JosophineSolobala-hp5ds 4 месяца назад
So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢
@CatherineDesire
@CatherineDesire 27 дней назад
Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?
@collinstrevor
@collinstrevor 10 месяцев назад
Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo
@CatherineDesire
@CatherineDesire 27 дней назад
Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?
@MadalitsoHope
@MadalitsoHope 9 месяцев назад
Zamphavu 🙏👏 prophet
@mordecaikachale2497
@mordecaikachale2497 10 месяцев назад
Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh 10 месяцев назад
Ukulu wa Mulungu tauona
@esthermakwinja3207
@esthermakwinja3207 10 месяцев назад
Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke
@richsambakusi424
@richsambakusi424 10 месяцев назад
Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa
@oswardmwale216
@oswardmwale216 8 месяцев назад
Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo
@rachealphiri3416
@rachealphiri3416 10 месяцев назад
It happened in Zambia twice
@ephraimphiri5789
@ephraimphiri5789 9 месяцев назад
Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...
@user-rv8gi4ro6r
@user-rv8gi4ro6r 10 месяцев назад
Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya
@user-lc7ji1gn9w
@user-lc7ji1gn9w 10 месяцев назад
Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya Месяц назад
Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed
@tonyteixeira2463
@tonyteixeira2463 14 дней назад
Tolo Thoko😅
@BaxterChipofya
@BaxterChipofya Месяц назад
Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B
@JohnChibalo-wf8gr
@JohnChibalo-wf8gr 10 месяцев назад
Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 8 месяцев назад
koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please
@user-zc9ku5fw4n
@user-zc9ku5fw4n 5 месяцев назад
Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏
@dondamissonchdziwe3958
@dondamissonchdziwe3958 10 месяцев назад
Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje
@peterbakuwo1249
@peterbakuwo1249 10 месяцев назад
🙆🙆🙆🙆
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 10 месяцев назад
Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk
@oliviaolivia4979
@oliviaolivia4979 10 месяцев назад
Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 10 месяцев назад
Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji
@florencebonga3211
@florencebonga3211 10 месяцев назад
Ambuye alandile ulemu 🙏
@MussaIbla
@MussaIbla 10 месяцев назад
Eish zovesa chisoni kwambiri
@BlessingsBanda-qn7xr
@BlessingsBanda-qn7xr 10 месяцев назад
Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu
@chimwemwemaquesuwell5841
@chimwemwemaquesuwell5841 10 месяцев назад
Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo
@josephnanyanga2012
@josephnanyanga2012 8 месяцев назад
ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha
@adamusaidih8570
@adamusaidih8570 10 месяцев назад
Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti
@user-ek7vg7ld8h
@user-ek7vg7ld8h 9 месяцев назад
chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?
@user-dt8nr1zx6e
@user-dt8nr1zx6e 10 месяцев назад
Taona nawo zikomo
@AmusedSakura-dx1nw
@AmusedSakura-dx1nw 6 месяцев назад
Lord have mercy
@liki-likiladies---lilongwe6963
@liki-likiladies---lilongwe6963 10 месяцев назад
Divine postmortem
@ChisomoKapanda-jg2uf
@ChisomoKapanda-jg2uf 10 месяцев назад
Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku
@JusticeMakwinja
@JusticeMakwinja 2 месяца назад
Tikufuna busayo ndithu
@user-zk5nu5fh6l
@user-zk5nu5fh6l 10 месяцев назад
Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga
@CostaCasimiro
@CostaCasimiro 7 месяцев назад
Blassa semanal agovati ndi agedo
@KINGMANMAKALA-hb9gs
@KINGMANMAKALA-hb9gs 10 месяцев назад
😂😂😂😂
@mcsellahntv6896
@mcsellahntv6896 10 месяцев назад
Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.
@BdhfbHdhe-pd7nh
@BdhfbHdhe-pd7nh 10 месяцев назад
Abelo ukutiona kupusa
@hawabanda-xs5fx
@hawabanda-xs5fx 10 месяцев назад
Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 9 месяцев назад
😂😂 Paja timafera ma jekete... Koma awawa voice yawo ikuchita kumveka kuti ndi a prophet di
@patriciacraiton-sf5vu
@patriciacraiton-sf5vu 8 месяцев назад
😂😂😂😂
@AleksaWilliams-qc6cn
@AleksaWilliams-qc6cn 10 месяцев назад
Shame😢
@mbawabuliyan9704
@mbawabuliyan9704 10 месяцев назад
Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike
@YusufMolesi-vr4pn
@YusufMolesi-vr4pn 10 месяцев назад
Hy
@user-ux8qz1tg7l
@user-ux8qz1tg7l 10 месяцев назад
Number ya abelo pls pls ol ya abusa
@SaidShop-nf3qu
@SaidShop-nf3qu 3 месяца назад
Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo
@AriohChauluka-lm9oo
@AriohChauluka-lm9oo 10 месяцев назад
M
@patrickjaenda8288
@patrickjaenda8288 10 месяцев назад
Zomvesa chisoni kwambili
@user-fq3jz4hl4c
@user-fq3jz4hl4c 10 месяцев назад
Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo
@rooseveltmtemula2643
@rooseveltmtemula2643 9 месяцев назад
Ineso ndikuifuna ngati munaipeza please share
@marthacassam
@marthacassam 10 месяцев назад
Zaulendo uno tiona zithu
Далее
Kijito Choir - Simba wa Yuda (Official Video)
9:44
Наше обычное утро 💕
00:42
Просмотров 741 тыс.
Maybe a little TOO much gel 😂
00:12
Просмотров 12 млн
Как вам наш дуэт?❤️
00:37
Просмотров 500 тыс.
MOÇAMBIQUE EM CONCERTO |28|07|2024
Просмотров 376
Kangawude Amuna folo
26:38
Просмотров 49 тыс.
Izeki ndi Jakobo-Njinga
16:46
Просмотров 754 тыс.
Continu.. Part 2
37:28
Просмотров 140 тыс.