Тёмный

PROF, ARTHUR PETER MUTHALIKA WALAVULA MOTO LERO PAMENE ATOLANKHANI ANAPITA KWAO KUKAMUFUNSA IZI 

Makosana
Подписаться 87 тыс.
Просмотров 14 тыс.
0% 0

Опубликовано:

 

4 сен 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 87   
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
💙💙💙APM you're my vote today. Kaya upanga kampeni kapena ayi. Ndidzabwera ku Malawi only to vote for you. But now start looking for a successor to maintain the party.
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Me too i will vote for him Ndipo ndikuona kuchedwa❤❤
@VungaQueen
@VungaQueen Месяц назад
Ineso ndikuona kuchedwa kwambiri 🔥🔥​@@user-uc1pd1tc2x
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d Месяц назад
Waiting for you guys​@@user-uc1pd1tc2x
@MartinGausi-rl5hb
@MartinGausi-rl5hb Месяц назад
Gud thinking man,god blles you dad
@WistonMphande
@WistonMphande Месяц назад
APM my vote. Tinanena Ife Kuti APM is a calm and visionary leader. 2025 APM BOMA
@EmanuelMuotcha
@EmanuelMuotcha Месяц назад
God bless you dad
@LamseyLazarous-dl5qd
@LamseyLazarous-dl5qd Месяц назад
Watching from Port Elizabeth
@user-ww9rj2wx8d
@user-ww9rj2wx8d Месяц назад
My vote
@jamiajafali6619
@jamiajafali6619 Месяц назад
APM MY VOTEEEE
@user-dp7bc7yy6s
@user-dp7bc7yy6s Месяц назад
Apm my vote 2025
@Jessica-pg6ep
@Jessica-pg6ep Месяц назад
My vote❤DPP
@ephraimphalawala4720
@ephraimphalawala4720 Месяц назад
President in waiting...This is the kind of President we want. Intelligent and focused
@ancientnkhata1137
@ancientnkhata1137 Месяц назад
Paja munavoteranso yemweyu last time
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Our chiyembekezo❤❤❤❤❤❤
@Layton-o3u
@Layton-o3u Месяц назад
Time to focusing on new generations , he done his part already "Pamene anali boma sakaona zomwe a Malawi timasowa"
@mastermindmanyozo5853
@mastermindmanyozo5853 Месяц назад
Our votes
@YellowmanMalawi-qe8zh
@YellowmanMalawi-qe8zh Месяц назад
We adore u,one in a million 😊
@KateteMussah
@KateteMussah Месяц назад
Watching for cape town south Africa
@SaidMkonongo
@SaidMkonongo Месяц назад
Tidyenso chimanga chaulere❤
@user-co3wr3rn4h
@user-co3wr3rn4h Месяц назад
APM my favorite😍💕
@Littlefair7
@Littlefair7 Месяц назад
With all due respect, APM, Biden, Trump, Museveni and other older leaders need to pave way for the youth.
@TopoTopo-bm4vw
@TopoTopo-bm4vw Месяц назад
Watching from Botswana
@user-kh4qp1ji1i
@user-kh4qp1ji1i Месяц назад
Waiting
@user-kh4qp1ji1i
@user-kh4qp1ji1i Месяц назад
Watching from Cape Town!
@VincentRobert-c5c
@VincentRobert-c5c Месяц назад
Ayenda ownawna APM
@ChrisLessie
@ChrisLessie Месяц назад
Watching from Durban
@EllahChikwatu
@EllahChikwatu Месяц назад
Mosongozedwa nd mulungu a dad ndinu ciyembekezo chathu
@MalkamuErgogo
@MalkamuErgogo Месяц назад
Watching from JHB
@GiftJulius-ro9ev
@GiftJulius-ro9ev Месяц назад
Tinakutuluka ....Namalomba ndi anzako masomwaa mutizunzilenso abale anthu alubino .....mbolizanu...
@FrankKowera
@FrankKowera Месяц назад
Ziiiiiii
@EmmanuelNgamuti
@EmmanuelNgamuti Месяц назад
He has handled a certain crucial question well.
@JabesAlfaiate-t4v
@JabesAlfaiate-t4v Месяц назад
Ifenso pano pa Mozambique tili pambuyo panu bwana Peter mulungu aku sungeni mpaka tsiku la vote ndi
@LydiaManzy
@LydiaManzy Месяц назад
Ndipotuu ndikuona kuchedwa kut ndikuvotereniii dadiiiiii❤🎉
@MustapherLino
@MustapherLino Месяц назад
Adad woooyeeeeee
@CostancioFrancisco-lp6xg
@CostancioFrancisco-lp6xg Месяц назад
Udindo uwu ndikuona kuti adzaudyelele ndi vice president wake awa atha akula
@hanifahmponda8711
@hanifahmponda8711 Месяц назад
Thanks so much malawi to support you 💙💙💙💙🙏
@KondwaniGronyonyo
@KondwaniGronyonyo Месяц назад
Apm basi
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf Месяц назад
Well done
@EsnartGirivin
@EsnartGirivin Месяц назад
Kodi anthu mudzingoti kupita kutsogolo kenako kubwelela mbuyo Momwe anthu munamtukwanila nthawi ijayo panoso aaà komatu Bola angolamulila Yesu dzikoli
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np Месяц назад
Ayi koma Pali zinthu Zina Mulungu kuti zichitike kuti anthu atengelepo phunziro
@user-uc1pd1tc2x
@user-uc1pd1tc2x Месяц назад
Our Baba father Malawi ❤❤❤❤❤❤❤❤
@LynessSuluma-gi2jp
@LynessSuluma-gi2jp Месяц назад
Waiting baba
@CatherineKamsare-cy3yo
@CatherineKamsare-cy3yo Месяц назад
Our president
@PatrickKaphesi
@PatrickKaphesi Месяц назад
Amalawi ataya zaka zisanu zaulele chopanda phindu president anagwila nchito kuchipiku vice sanajgale mp muyendesa bwanji dziko apengatu ndi mwazi wa kuchikangawa
@user-lw4hw9ce4w
@user-lw4hw9ce4w Месяц назад
Adad akubweranso wina afune asafune
@user-mf7hf7we2u
@user-mf7hf7we2u Месяц назад
Uyiwaleko mr pulezidenti
@PhillipNyaugwe
@PhillipNyaugwe Месяц назад
Chimwemwe chanthu waseza nthumba ndiuyu chonde amalawi tiyeni timunthandize ponganiza ndiupangili kuti mwina antha kuzati pasa munthu oyenela ambiliwa agofuna kutchuka ndikuba bc
@LilianKachala-yz2xf
@LilianKachala-yz2xf Месяц назад
DppTu BASI my vote
@rodglae6657
@rodglae6657 Месяц назад
😊
@lucianogeoffrey4275
@lucianogeoffrey4275 Месяц назад
Background sound muzitsitsako wez ikusokoneza voice please
@damianokachingwe3531
@damianokachingwe3531 Месяц назад
Kulakalaka chigwa cha madzi chidulo chilipo udzayambe kugulanso mbalr imodzi ya mkaidi k100 ,000 ukuona ngt tidaiwala
@Patgregorymanyumba
@Patgregorymanyumba Месяц назад
Mchikulire ❤❤❤❤
@OnenessLestas
@OnenessLestas Месяц назад
Asamatinamize ice zaboza zimezo
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Месяц назад
Unakanika kale wabodza iwe suwina 😅😅😅
@Pangolinimw
@Pangolinimw Месяц назад
💙💙💙💙💙💙💙
@user-bd5kw8oq1r
@user-bd5kw8oq1r Месяц назад
Palibe zowina awa koma pa social media awina 😅😅😅
@LeoLongwe
@LeoLongwe Месяц назад
Choka iwe chikangawa
@Samu-q3z
@Samu-q3z Месяц назад
Boma ilooo
@ChiefJustin-cl8jl
@ChiefJustin-cl8jl Месяц назад
Munthu wamkulu ndi inuyo ulemu wanu
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Месяц назад
Chachekula ichi siziveka zimene akuyankhula akapume
@tasmania527
@tasmania527 Месяц назад
Koma ndiye, kukakamira mtunda wopanda madzi- za zii!
@user-gq6nj6yo6f
@user-gq6nj6yo6f Месяц назад
❤❤❤❤
@PatrickViyache
@PatrickViyache Месяц назад
Ulemu wanu adad?
@bysongeorge3243
@bysongeorge3243 Месяц назад
Yes , he is our hope but he is surrounded by some ill mannered individuals who also participated in bad behaviours during their past rule of government. They are quietly hiding behind him..
@tasmania527
@tasmania527 Месяц назад
Very true brother and they're the main beneficiaries of APM's presidency. We don't need a leader who is as good as senile and who is being controlled by selfish minds. His time is past.
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
A professor nawonso analephela zinthu zina kuzikomza zimene Chakwela wazikwanilisa padzuko palibe wabwino Maka a ndalewa onse ndi zunkhanila zikha zika...
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e Месяц назад
Munthawi yawo Magetsi amavuta vuta kwambili lero ndi mbili yakale ikakhala njala pa Malawi ndi culture yaba Malawi no wonder
@LamseyLazarous-dl5qd
@LamseyLazarous-dl5qd Месяц назад
Suka. Wen uthetha kaka
@Shelifibraheem
@Shelifibraheem Месяц назад
Dzikolathu ndilomweli ena akuesela kung'amba koma bwana mulisoka
@Randy-er2xo
@Randy-er2xo Месяц назад
Adzalowanso amcp ayamba kusanza😂😂😂😂😂😂😂
@BwanaGD
@BwanaGD Месяц назад
Ndilipano daaaa
@martinsailesi1731
@martinsailesi1731 Месяц назад
Please when you upload the videos make sure you take the shit sound out, doesn't sound sense.
@MaggieMuhone-r7m
@MaggieMuhone-r7m Месяц назад
Tikukudikililani. Apm
@SaidiMbawa-st6bj
@SaidiMbawa-st6bj Месяц назад
Azikoza munjila yanji ngati sadali mu boma koma malubino kumangofa ngati nkhuku
@user-vl8uw8mc3u
@user-vl8uw8mc3u Месяц назад
Chiyembekezo cha amalawi chokhachi basi
@WhiteRichard-cw2fo
@WhiteRichard-cw2fo Месяц назад
Athu. Akudikila inu adad
@user-ez1kc7zp9m
@user-ez1kc7zp9m Месяц назад
Sizikumveka ntaaa
@MynessChirwa
@MynessChirwa Месяц назад
Boma iloo
@ImranAlisen-zb9sz
@ImranAlisen-zb9sz Месяц назад
amalawi taphuzira sitidzayesanso
@spargomw
@spargomw Месяц назад
Ndipo tachimina😂😂😂 komaso tachilàpa, boraso kuika munthu osapemphera pa mpando😂😂😂😂😂.. Adad my vote❤❤❤❤❤
@OwenNyangu-nv1yt
@OwenNyangu-nv1yt Месяц назад
Kkkkkkkk salankhula zoveka abwanawa
@VungaQueen
@VungaQueen Месяц назад
Akuyankhula chizungu simungamve ndinu achewa ndevuto 😂😂chikanakhar Chichewa bwezi mukumva🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼😀😀
@Lee-lee-w1r
@Lee-lee-w1r Месяц назад
Ine ndikunva 😂
@WilliamMasauko-su1wx
@WilliamMasauko-su1wx Месяц назад
Adadi omwewo
@user-rm2xv8ys1i
@user-rm2xv8ys1i Месяц назад
My vote
Далее
لدي بط عالق في أذني😰🐤👂
00:17
Просмотров 2,3 млн
CRUISE 5 WITH MOSE WA PA PHIRI LA BUNDA
1:14:37
Просмотров 111 тыс.