Тёмный
No video :(

Rev Alexander Kambiri preaching at Malawi Immigration Head Office -Lilongwe Malawi 

Rev. Alexander Kambiri
Подписаться 20 тыс.
Просмотров 39 тыс.
50% 1

It was morning devotion service which happens every Monday at Immigration' office

Опубликовано:

 

25 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 82   
@blessingkamanga1781
@blessingkamanga1781 6 месяцев назад
Maybe they can stop corruption. The one who organized this program may God bless him or her abundantly.
@ceciliasibande7936
@ceciliasibande7936 6 месяцев назад
Kupezeka ku immigration ndi chisomo cha Mulungu zoonadi Mulungu adasankhadi inu kuti mupezeke pa maudindo muli nawowo. A big Amen
@user-fd6oh2vc1c
@user-fd6oh2vc1c 6 месяцев назад
Please continue organizing this program frequently as very helpful to such.God bless you Rev.Kambiri
@user-pf1xd3lp2u
@user-pf1xd3lp2u 4 месяца назад
May God bless you pastor powerful message wakhutu wamva
@marypatriciamakuru226
@marypatriciamakuru226 6 месяцев назад
Amen Amen Amen. Mwina asinthe mchitidwe wa corruption. Abusa mudziwayendera kawiri kawiri.
@user-xd5bp8wr1m
@user-xd5bp8wr1m 6 месяцев назад
Sipangakhale kusintha because pamwambapo pali mbava yeni-yeni Shakwera ndi afalisi azinzake
@catherinechisale9567
@catherinechisale9567 5 месяцев назад
Good initiative by Immigration Department. May good Lord bless you. Zikungofunika kulapa basi, mgt Pampanga mbali yake.
@enipherphiri207
@enipherphiri207 6 месяцев назад
Wow! This is the divine definition of grace to individual staff at immigration. Review yourself and stop maladministration. The spirit has spoken. Thank you pastor Kambwiri
@MaggieKapalamula
@MaggieKapalamula 5 месяцев назад
This is beautiful may God bless immigration office for honoring God words
@VictoriaWilliam-ms2ft
@VictoriaWilliam-ms2ft 5 месяцев назад
Amvekere Amen ngati za nzeru mbava zachabechabe izo ndipo alape anthu amenewo
@mchipengule
@mchipengule 6 месяцев назад
Mau a Mulungu sasankha Malo. God is everywhere!!
@user-qf4oc1xj8d
@user-qf4oc1xj8d 6 месяцев назад
God continue talking to us through the ones you have chosen So that we can know why we are in our positions Amen
@user-lb6ek3ee6d
@user-lb6ek3ee6d 5 месяцев назад
Tadalitsika kwambiri Pastor
@suzyomanda4359
@suzyomanda4359 6 месяцев назад
Amen, thank you for the word of encouragement Abusa. God bless you
@robertrichman9376
@robertrichman9376 6 месяцев назад
Best place to preach, next time to our Parliament
@user-ke7cd1et5k
@user-ke7cd1et5k 6 месяцев назад
Zinyengo ameneo zili mitu bibi
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 6 месяцев назад
😂
@LimbanChasasaThawi
@LimbanChasasaThawi 5 месяцев назад
Amen man of God
@bensonnkhatatonje6007
@bensonnkhatatonje6007 6 месяцев назад
Amen
@bensonnkhatatonje6007
@bensonnkhatatonje6007 6 месяцев назад
May I have it please
@user-kv8fq6im3v
@user-kv8fq6im3v 6 месяцев назад
Anthu akatangale opondeleza ngati awa until they change that God has nothing to do with them
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 6 месяцев назад
I always agree with this man.He knows how put sense into people mind.
@abdulrafiquekalembo469
@abdulrafiquekalembo469 6 месяцев назад
Anthu amenewa uthenga aumve ndithu.Ma past port athu ali mmanja mwa ma Burundi,Ma Nigeria ndi Amwenye pomwe ife anuwake timavutika kuti tipeze passport.
@user-cb2cv9fz7m
@user-cb2cv9fz7m 6 месяцев назад
Mbava za kuba MULUNGU awakanthe onse awa fire 🔥🔥🔥🔥 pano tilibe mtendere ndipo zoonadi akayamkhadi
@user-uz7wp8mf6b
@user-uz7wp8mf6b 6 месяцев назад
To God be glory, ndadalitsika nawo uthengau ndipo wandikhudza
@LinesiKanzota-fw7sj
@LinesiKanzota-fw7sj 2 месяца назад
Amen 🙏
@user-zp6eq4br7t
@user-zp6eq4br7t 6 месяцев назад
Abusa zilingati mukulalika palibe coz muli pakati pa nkhosa zosochela😂😂😂
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 месяцев назад
Amen Abusa awuzeni kwambili ave masozi ya anthu ili pamutu wawo
@user-vi4ge5lq8t
@user-vi4ge5lq8t 6 месяцев назад
More blessings to you pastor
@user-dx6jm4yx2e
@user-dx6jm4yx2e 6 месяцев назад
Ndizoonadi abusa amthu anenewa amati zuza ndi tauzika kudedza mulungu atithandize awakhululukike ambili akulila😢😢
@mphatsojosephynyamatawakun3965
@mphatsojosephynyamatawakun3965 4 месяца назад
amen
@quespeykatame2595
@quespeykatame2595 6 месяцев назад
Ma uthenga akumveka ndithu 😊
@user-wr7rm6yw3j
@user-wr7rm6yw3j 6 месяцев назад
Amen man of God 🙏🙏🙏🙏🙏
@dumisanimoyo3152
@dumisanimoyo3152 6 месяцев назад
That is a very corrupt ministry in Malawi government plz from there kambiri go to traffic department
@PaulMungoma-rs2st
@PaulMungoma-rs2st 6 месяцев назад
Amen tadalitsika nawo
@Dan-Buleya
@Dan-Buleya 6 месяцев назад
Anthu awa eeeeeeh ambuye awayendere
@andrewchirwa2193
@andrewchirwa2193 6 месяцев назад
mwina angasiyeko chinyengo
@e.r.mchanel1460
@e.r.mchanel1460 6 месяцев назад
Munasowatu a Rev
@PirtekDriver
@PirtekDriver 6 месяцев назад
Will the corruption stop????
@ChikondiLameckPhiri
@ChikondiLameckPhiri 6 месяцев назад
Thus Great
@sweeneykamwendo6251
@sweeneykamwendo6251 6 месяцев назад
Ada awo anadya 100pin yanga...maofesara achinyengo😅
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 6 месяцев назад
Kukonda ndalama a immigration
@AlliUsuman-mj1mr
@AlliUsuman-mj1mr 6 месяцев назад
Km musiye kuba anthu inuuu aku immigration
@mphatsojosephynyamatawakun3965
@mphatsojosephynyamatawakun3965 4 месяца назад
lapan anyamata Inu aku immigration mukuba kwambiri tikamapangitsa ma passport
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 6 месяцев назад
Mrs luhanga ndakuonani number yanu bwanji
@masterkachingwe7448
@masterkachingwe7448 6 месяцев назад
Ma officers chinyengo awa alibzyoli anyenga okha okha mwina kumaalalikira Daily
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 месяцев назад
Ingakhale mukuwalakhula choncho,sakumva kanthu ai ndithu"moti enawo angokutukwanani,angoti Galu iwe mumtimamo. tikakudyera kuti.
@adsonphiri6497
@adsonphiri6497 6 месяцев назад
Awa akufunikadi mapemphero,mbava zotheratu
@user-ps9nu6se9k
@user-ps9nu6se9k 6 месяцев назад
Amen man of GOD
@UchiziNyirenda
@UchiziNyirenda 6 месяцев назад
Preach on man of God
@user-xk5se7ot8d
@user-xk5se7ot8d 6 месяцев назад
Kumapetoko munakawapemphelela
@AminaPhiri-pp9tw
@AminaPhiri-pp9tw 6 месяцев назад
Abusa nthuwa Alape kaye katangale amanyanyila kwambili alape ndithu
@user-ty6cs9ic5w
@user-ty6cs9ic5w 6 месяцев назад
Madalayo wosapanga retire bwanji akapume
@ruthnangwale
@ruthnangwale 6 месяцев назад
Powerful 🤝
@user-ec3xh4pc6t
@user-ec3xh4pc6t 6 месяцев назад
Amen 🙏 🙏
@mwale1154
@mwale1154 6 месяцев назад
Amen 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
@gesinasutherland9241
@gesinasutherland9241 6 месяцев назад
komatu simukuwoneka abusa kapena Maliro achepa dera lanu..ulaliki wanu umatitsitsimutsa ndipo umatisintha..kapena 2024 Mwabwera ndi zina..😂😂
@rev.alexanderkambiri892
@rev.alexanderkambiri892 6 месяцев назад
uthenga si waku maliro okha, tili nawo ma videos ambiri koma sitimatha kutumiza kamba ka kuwonongeka kwa zipangizo zathu zogwiritsa ntchito. pang'ono ndi pang'ono tayambapo kuzitolera ndipo Ambuye atithandiza.
@user-yt6ze8od9d
@user-yt6ze8od9d 6 месяцев назад
Amen Amen
@alexbanda8463
@alexbanda8463 6 месяцев назад
Amen ❤
@user-sn4se3ul7i
@user-sn4se3ul7i 6 месяцев назад
Mulungu alemekezeke
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 месяцев назад
Abusa next week pitani ku STATE HOUSE,,kwaphulika zimimba kumeneko...
@user-vf1kt6fw7y
@user-vf1kt6fw7y 6 месяцев назад
Abusa musataye thawi ndi athu amenewo muchedwa nazo, zonsezo ndi mbamva zotheratu,funso nkumati mwasakha bwanji kulalikira office ya athu akubayo Bola munakapita kumamizi kulalikira km naizi Mmmmmm mbamva
@geoffreykalinda2672
@geoffreykalinda2672 6 месяцев назад
Apitekoso ku police (road traffic)
@funnychinsalu6198
@funnychinsalu6198 6 месяцев назад
Mukayankha pa maso ps mulungu ndalama mutazisiya pansi pano
@numelimtenje5846
@numelimtenje5846 6 месяцев назад
Mwina angalapeko anthu ozunza awa
@khumbomkorongo4108
@khumbomkorongo4108 6 месяцев назад
Powerful
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 месяцев назад
Mukafikeso ku Ma Court...kuli mamafia kumeneko.
@user-xs5mi3fr2y
@user-xs5mi3fr2y 6 месяцев назад
Please stop corruption
@YasiduPemba
@YasiduPemba 6 месяцев назад
Immigration ya malawi ntchito ya NRB mumaidziwa koma chipangisireni chitupa changa sitinafunsidwepo mpaka pano from 2018 ndimafunsidwa ndikapita Zambia Mozambique Tanzania 😂😢😅😅
@amabhohlela.3492
@amabhohlela.3492 6 месяцев назад
Pomaliza chopereka abusa,,,
@josiahgarley3824
@josiahgarley3824 6 месяцев назад
Mpaka mmaoffesi?
@NgomaRaheem
@NgomaRaheem 6 месяцев назад
Athokeni ngamo agalu amenewa akutilangadi passport ya 90pin kudisha 300,pin mulungu awaonedi
@fahadmilanzi
@fahadmilanzi 6 месяцев назад
Ulaliki wabwino aRev gulu lozuza limenelo
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o 6 месяцев назад
Anthu awa amakhalangati anachoka direct kumwamba kuti azagwire ntchito ku immigration
@damianokachingwe3531
@damianokachingwe3531 6 месяцев назад
Anthu opanda chisoni amenewa kuteroko lero lomwe lino amubera wina ndalama kulephera kugwira ntchito mwachilungamo too much corruption
@juliusnjerengo2610
@juliusnjerengo2610 6 месяцев назад
Pastor you are preaching to evil people. Ndinakanika ulendo wanga opita ku UK chifukwa cha asatana ameneo.
@clintonhodda9830
@clintonhodda9830 6 месяцев назад
Anthu a corruption awa
@AlexMwalec
@AlexMwalec 6 месяцев назад
Amen
@user-kd3lh4wy1m
@user-kd3lh4wy1m 6 месяцев назад
Amen
@chisomonyerere7197
@chisomonyerere7197 6 месяцев назад
Amen
@gesinasutherland9241
@gesinasutherland9241 6 месяцев назад
Amen
Далее
MALAWI DEFENCE FORCE TRAINING INSPECTIONS
1:21:37
Просмотров 67 тыс.
MVAMA CCAP
57:35
Просмотров 18 тыс.
Rev. Alexander Kambiri preaching at Mtunthama- Kasungu
1:15:45