this is a well-sophisticated briefing but we hope the implimentation stated will be followed as planned coz the issue is so out hand and the govt needs to react on immediate effect
Press breafing ya kunkuyu ndiyopanda ntchito chifukwa ine dzulo Bakili Muluzi TV anatiuza dzulo with figures, however tikuyenera kumamvera BM TV not wabodza yu. These same krooks told us last 2 weeks kuti mafuta afika thru train koma sanagulitsidwe then tikumva kuti mafuta akusowa. What kind of nonsense government is this
Hey hey hey!!!! They want us ti feel stupid. Hey hey hey!! They want us to think stupid. They told us things will be cheaper! They tikd us things will be easier!! Hey hey hey!!!
Can connect nicely your mike is not connected good zomwe muganiza kut mpakana pano mulibe ndalama ko zoona zomwe mukuyendela maiko akunja mukuzitenga ku😂😂😂😂😂😂😂
Frm today onwards you guys muphunzire kuyankhura n mukamayankhura mudzidziwa kuti ku mwamba kuli Mulungu, munatha mau mmene ankalamulira anzanu aja lero ndi izi zafika pa wes phunzirani kulemekeza kumwamba
Wake up malawi Wake up this is our beloved country no one should treat us like this we the citizens are not fools enough is enough people lets remove this evils they dont care about us people who put into power,people are suffering people are dying in the hospitals people are dying with hunger, what are we waiting for ????? We people have the power to remove this nonsense evils😈 we just have to stand up together we free ourselves from this lions malawi remember God says he helps his people who ask him for help, so let us work together and we will be free
Kodi you telling us that you don't know your budget or kusewera ndi ife a malawi,mukuti covid 19 ndinu akumalawi nokha mukuziwa za covid 19 ndiposo bwanji osakoza mseu kuti galimoto zisayende bwino mu M1 zoona? Muli busy kuwononga ndalama za boma Kuba wina akumanga manyumba 20 plus aluzitenga kuti ndalama zo bwanji ku immigration ma passport mukupanga a fake? Bwanji mwana wa president ndi amene akutsongolera immigration? Musanamepo apa mukuba kwambiri mwalemera vote muzaonaso kuti tizavota bwanji enanu mufunika kukalhala kundende
And ku UNGA simupita ndi MA kwacha, lero chiyambileni MCP bodza lokha lokha opanda chimodzi chokha chowona abale???? This is the worst and shit government serious. 😢😢😢
Koma agalu awa ndiye atisuza kwambiri koma kuba ndalama nde number one palibe chimene tingave apa boma ili lolepela andiso lalepela boma lolepela kuyendesa ziko koma katangale nde number one agalu inu musiona chaka cha mmawa nditu
Boma longosatza ndi mavuto oka oko 😂😂😂😂😂 koma mcp ndiyovesa chisoni kwambiri nditu njala kugwesa ndalama kukwela kwa zinthu ma passport komaso ma passport vegi mavuta kusowa thawi iliyose china chilichose ndichosokonekela ndiye chitukuko cha mcp chimenecho iyhoo mavuto ndiye tilinawo