100% agree, ndimakangana ndi ena pa imfa ya martin nkhana, ndimanena zimenezi kuti anyamata akwathu atha chifukwa chofuna kutchuka, Iiiiiiiiiii Ndinayipalamula kwa ena Amalawi, lero ndi izi apululukabe kukonda kutchuka. thank you brother Twaibu. Zimene akuyimba zaziiiiiiii
I know you man of God and all what you say I believe because is what you went through and you was doing it before.. may God help us in this end time as you continue telling us the truth....
Izi ndithu ndi zinthu zomwe anthu tikamamvetsera zimakhala ngati nkhambakamwa koma kuno kudziko kuli zambiri zomwe zimachitika. Zikutengera mzimu woyera ndi Yesu atalowererapo. Yesu atichitire chifundo. Zikomo chifukwa cha mau amenewo
Apa ndiye mwakamba mwa tchutchu .....wakumva wamva osamva adzakhalabe osamva .sitikukana tonse tidzafa koma izi zokha zawonjeza ....satanic is too much
Ine ndamvela audio bwino bwino koma pali pomwe mwaonesa kuti mubakila bushiri and bushiri si munthu oti mkumu bakila he is the one who is giving money to young artist i have all the evidence he is the devil himsef