Chitsilu cha president,,, up to date still blinding Malawians but why chakwela? 1million jobs in what ways yet you gone through 4yrs and what you archive is kuba
Chitsilu ichi akuti chakwerayi akangokambapo atakhuta nsima yomwe imapezeka tikugula fetereza otchipa muthawi ya Peter osati zalerozi ulamulilo wausi one million Job or Jocks
Chitsilu kwambili chakwera galu wachabe chabe bodza lakuonekera unabisala mbatata.pano ndiye worse anthu akupita ku John kusonyeza kuti kumalawi zinthu sizikuyenda kumalawikuno.anthu akamathawa dziko lawo ndikumapita kwina that is the sign yokut dzikomo zinthu sizilibwino.maiko monga Malawi,zimbabwe,Congo,bulundi,etc anthu akuthawa maiko awo kwambili kumakhamukila ku south africa bcoz of stupid president in there country like Malawi.
Guys apapa Pali mawu a bakili muluzi tv??? Let's be serious mawu awo agaluwa akuwapweteka okha and because of manyazi they turn in kulimbana ndi anthu aphee tivomerezedi kuti tili mu one party regime