God bless you Dr Michael Usi, for remembering the people who you worked with, when God changes your story, it's always Good to remember where you are coming from.
Kodi mukuti awa ndi apurezident a UTM nanga bwanji sakupita kukaona Malo womwe anapangika Ngozi kuwuzana ndi kwantere nzakeyo ? Amalawi khalani ndi nzeru awawa ndi afiti
kodi anthu enanu mukuti usi ntchito akuigwila kodi ntchito yake iti poti sitikuiona Amalawi muzikhala ndi nzeru because usi akungoyendayenda kumupangila Kampen chakwera this is nonsense