My vote is for Apm osati chipani cha zisilu zili apazi ....mukugawa ndalama ndiyetu mupeleke ndalama kwa munthu aliyense mmalawi muno ......chipani copanda maso mphenya....chipani choyendesedwa ndi mbava komanso zigawenga
Ndiye kupusa anthu anyake akulandila ndala ena alipomwepo akukagona ndi njala boma lopusa kwambili ili kumapeleka ndalama pa msonkhano zimenezo ndizosaloledwa pa malamulo a democracy akulu awa ndi mbuli zedi
All the best Athu ambiri mumavutika coz mumakakamila mbali yoluza ndiye zanuzimenezo at the end of the day mumangokhala wokhumudwa komanso akhwiyo pa zaziiiiii