Тёмный
MALAWI WATHU
MALAWI WATHU
MALAWI WATHU
Подписаться
This a channel that we talk about anything to do with Malawi.Things that affect Malawi either positively or negatively.This ranges from politics, entertainment,economy to religion.So join us as we discuss these things.
Osayiwara Kuti Zinayamba Bwanji?
8:51
Месяц назад
Комментарии
@LukaSpoko-i3l
@LukaSpoko-i3l 11 дней назад
Akomaamakana ndipotimawanyadila
@EdisonNakulenga
@EdisonNakulenga 12 дней назад
Akamunaamenewo amativesakukoma jo
@RittoKei
@RittoKei 15 дней назад
Is this comedy 😅😅😅😅
@LonelyKhoma
@LonelyKhoma 17 дней назад
Gwaradi sakufunika kumupasa ndarama ayi kuthandiza kwake kuimirire ndi munthu wina azimupangira kaya ndi nyumba iyeyo akapeze yomanga kare ndikumuikamo mmmm zokhudza bwanji kuntchuka koseku 🤔
@SadguruPrernaTrust
@SadguruPrernaTrust 21 день назад
Jumping Jack !
@user-iv6iw1ck8s
@user-iv6iw1ck8s 22 дня назад
Zopanda ntchito izi, anthu akuvutika kwambiri kumudzi, okalamba, aumphawi, olumala, amasiye, odwala, osamalankhula mwachibwana kut Mulungu Ali mbari yanu yet zinthu sizili bwino, kulankhula ngati anthu opanda mzeru, palibe chanzeru chomwe mukuchita chopindulira Malawi kuposa kumangomanga wanthu ndi kusintha maina azipatala zoti simudamange ndinu, 4 years just for nothing, shame on you guys, mzipatala mankhwala mulibe, chitetezo taaa, ma school Nde mwakweza ma fees, anthu akumudzi omwe alibiletu chiyembekezo ndipo alibe chilichose akwanitsa bwanji kulipilira Ana awo ma school, chakudya Nde kulibiletu, chomwe mukuganiza mkuti tidzadzitsa bwanji matumba wathu kuti tidzabele zisankho, AGALATIYA opusa, oyamba ndi zabwino kutsiliza ndi zoipa, When I said amalawi akuvutika I mean it, mukamadya bwino kumitundako musamati aliyese a kudya, go to the villages and see how life is, you will cry, anthu a kugona ndi njala and you are expecting those people to go and vote for you this coming 2025 nonsense, MAY The Soul of SKC continue to Rest well and hope he is watching you all,
@user-qf7ko2dd5g
@user-qf7ko2dd5g 24 дня назад
Ufiti
@JaytuSaisi
@JaytuSaisi 24 дня назад
amapanga sewero
@GospelSoldiers-sr7np
@GospelSoldiers-sr7np 25 дней назад
Kuyankhula koputsa kwambili,Kodi moyo ndi wanu??? Inu anthu omvetsa chisoni kwambili
@Cathy-oc7vd
@Cathy-oc7vd 25 дней назад
It is supposed to happen.. MCP is a big party sangalore kuberekedwa
@KimuEmmanuel-lv9wt
@KimuEmmanuel-lv9wt 25 дней назад
Chakwera ndi mbudzi yamunthu
@PercyTrading
@PercyTrading 26 дней назад
Koma malawi kodi mukhalabwamji? monga azomba ndi azisuzo mumamwalila apanda kanthu kalikose.
@user-oc9vl9xz8e
@user-oc9vl9xz8e 26 дней назад
Mwagwanayo UTM yakutulukani forever Chakwela kwamai ako
@daviekamanga1417
@daviekamanga1417 26 дней назад
chisankho chabwino koma osanyoza adzanu ayi
@isaaczuze
@isaaczuze 27 дней назад
Chakwera ndi munthu olephela ....mkazi olanda amavuta
@PercyTrading
@PercyTrading 27 дней назад
Anamangindwa chifukwa chani
@mannersaint
@mannersaint 28 дней назад
Ayi ndth anthu matha kuvina eeeee😄
@OsmanOsher-sh6gp
@OsmanOsher-sh6gp 28 дней назад
Osayiwala chipande ndipowomola
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Месяц назад
Tso pali chimene wapanga chakwera success! Agalu achabe chabe.
@user-pv9uk6sc3w
@user-pv9uk6sc3w Месяц назад
Za ziiiiiiii! Chakwera ndi MCP yake akagwere uko
@tisuhmakhwah7085
@tisuhmakhwah7085 Месяц назад
Zakuvutani bas
@victorauwana7258
@victorauwana7258 Месяц назад
2025 president wanu chakwela? Is so sad for Chilima 😢 rest well
@victorauwana7258
@victorauwana7258 Месяц назад
Ubwino simuvota nokha
@user-xe1so5xj2w
@user-xe1so5xj2w Месяц назад
Anthu akuba akugawana ndalama za boma
@user-fm8ed7eo3i
@user-fm8ed7eo3i Месяц назад
Mbudzi ya mdzimayi mulungu dzikusunga ndi moyo wawutali pomzunza anthu
@GiftChitsulo
@GiftChitsulo Месяц назад
Oloko akupaseni ndalama koma dziko lilingati galimoto ngati siiwe dilaiva sungakwanise kuyendesa achakwela alephela
@IsmaelBilal-lh1pi
@IsmaelBilal-lh1pi Месяц назад
Mcp we no need it again yatizuza mokwana
@user-le9su3mt7r
@user-le9su3mt7r Месяц назад
Chakwela Galu wohipaa
@Geraldmkwewu
@Geraldmkwewu Месяц назад
2025votiyo yakuba chani musayi namize fiti yanuyo bozaa Galu lwe
@Geraldmkwewu
@Geraldmkwewu Месяц назад
Agalu lnumuzaziona mungotiphe ndinyani wanuyo agalu lnu
@BrunoChakukuma
@BrunoChakukuma Месяц назад
Mbuzi iweeeeee meeeee 😂
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh Месяц назад
Ameneyo ndi neneli wakale nanga watsopano watipo chani
@Masturdthepoet
@Masturdthepoet Месяц назад
Kuzinamiza pamenrpo😢😢😢
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 Месяц назад
Fack you all you taken advantage our country fack you all amcp
@sharifujoe7633
@sharifujoe7633 Месяц назад
Ohhhhh amenewo nde ma results aifa yachirima inuyo Malawian okuzidwa?
@HusseinAdamLidezo
@HusseinAdamLidezo Месяц назад
Pamsana pako iwe, koma ukuliona dziko, chamba et kuyankhulila kumaliseche kt pant adzimva kapena pakamwa
@danielmuriya8675
@danielmuriya8675 Месяц назад
Oooooh yes, chakwera emweyo mukudya naye bwino
@OrtonKabbichi
@OrtonKabbichi Месяц назад
Wandevu ameneyi sanasochere Wakuda angapezeke kwao
@yusufbakali
@yusufbakali Месяц назад
Ndi chimene chinamupha chilima
@user-dn3gp6yi4y
@user-dn3gp6yi4y Месяц назад
Kuyankhula komaliza mawu anuwo sumuzayankhulaso 2025 mukugwa
@user-xm3zl5cg6x
@user-xm3zl5cg6x Месяц назад
Kd mcp ndichan pamalawi
@user-fd1tu6ku1r
@user-fd1tu6ku1r Месяц назад
Emusipi idziwe kuti kunja kuno kuli Mulungu ndipo Mulungu sangalole Kuti Amalawi tipitirize kuvutika
@user-bg7ur1gw1q
@user-bg7ur1gw1q Месяц назад
Chakwela ndiye chani
@AbdullCassim
@AbdullCassim Месяц назад
Fundo sinakhazikike amtolakhaniwa
@jamesmwamvani8904
@jamesmwamvani8904 Месяц назад
good story scripting i like this
@petercaptain4462
@petercaptain4462 Месяц назад
Very Sad Story 😔😔😔😔😔
@Krisha-q4e
@Krisha-q4e Месяц назад
Nice
@richardskumwendah9072
@richardskumwendah9072 Месяц назад
Tembo
@majaliwamsigwa6206
@majaliwamsigwa6206 Месяц назад
From Tz,nanenso ndinamva kuti anamwalila,ndadabwa kuona alimoyo
@khelebhoofficialkambanje-zs2zk
@khelebhoofficialkambanje-zs2zk Месяц назад
Program yabwino