Тёмный
No video :(

A Michael Usi Alibe Impact Inaliyonse Ku UTM Olo Ukhansala Sangawine - UTM Member 

Nyasa VoiceBox
Подписаться 26 тыс.
Просмотров 18 тыс.
50% 1

On Nyasa VoiceBox, A UTM member says that Vice President Michael Usi has no real impact in UTM, he cannot even contest as a councillor and win.
Pa Nyasa VoiceBox, membala wa UTM wati Vice President Michael Usi alibe chikoka mu UTM, sangapikisane nawo ngati khansala ndikupambana.
#malawi

Опубликовано:

 

28 авг 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 62   
@MPHATSOKALUWA-lm2uy
@MPHATSOKALUWA-lm2uy Месяц назад
And munthu otan oti nd mtsogoleri km ma meeting amwambo wamaliro osapanga attend kmnso akapanga attend osayankhulapo chonsecho nd mtsogoleri amathanthauza chan???
@chippakaribafox2865
@chippakaribafox2865 Месяц назад
Mukufuna achite kukuwuzani yekha kuti ndi sellout?
@SalaJawali
@SalaJawali Месяц назад
Ndipo zodabwitsatu
@josephinemisomali6840
@josephinemisomali6840 Месяц назад
Funso mkumati Kodi nsalu zikugawidwa lerozi Kaya ndingongole zomwe zikufuna kuperekedwa lerozi nthawi yonse zinali kt amadikila Chilima amwalire Kaye UTM gwilanani manja Zambiri zichitika Koma osafooka
@LamieTiger
@LamieTiger Месяц назад
Mbili ya usi amakhala president straight tithakuona khadza Za John Tembo
@user-ck7eb7tb7v
@user-ck7eb7tb7v Месяц назад
Rest in peace SKC , we shall always remember you, 2025 ndipafupi apa
@eliffagondewe8214
@eliffagondewe8214 Месяц назад
Well spoken
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Osamaphweketsa Bon Kalindo. Bon Kalindo analosera za imfa ya Chilima. Ndipo ananena pa 6th June 2024 kuti Chakwera wakonza plan yakupha Chilima ndi ndege. Ndipo anamuuza Chilima asakwere ndege. Pa 10 June ndege ya Chilima inagwetsedwa. Pa 15 June, MCP inamanga Bon Kalindo kamba ka ma audio.
@henryphiri6100
@henryphiri6100 Месяц назад
Tidzadandaula akadzatuluka kaliati chifukwa ndi chipilala cha chipani
@SamuelMthengo
@SamuelMthengo Месяц назад
Very powerful message.
@JohnJohn-og8rt
@JohnJohn-og8rt Месяц назад
Zoona Mau abwino kwambili maso kusongolo
@MariamJohn-dg4em
@MariamJohn-dg4em Месяц назад
Viva UTM viva
@thomasphiri-zr3xs
@thomasphiri-zr3xs Месяц назад
Very true comrade le take on Nyalonje has no political impact indeed in her last constituency b4 her lost her seat pipo in the constituency booted her out bcos of her characters manners...........my plea to UTM G.members mama kaliati do a better research on mps to stand in 2025 elections don't just hand pick the rejects from other parties now are paying back what we sow in 2019.
@alinafesalima5597
@alinafesalima5597 Месяц назад
A Michael Usi ndi munthudi owumila koopsa ine ndagwirizana nanu ndipo sapasa munthu ndalama yake
@thomasphiri-zr3xs
@thomasphiri-zr3xs Месяц назад
Lets allow new members why pipo r flocking to UTM now.....there is potential to win elections though reqiures proper partners. However let's give chance to madam Mary Chilima if so she can accept to compete any position now or later but God shows that in the years to come Shaun Chilima will bounce back into politics same UTM with powerful change and will rule the country. What late VP Chilima was doing hasn't been fulfilled so spiritually power is coming back to complete where left.
@Marymahendra
@Marymahendra Месяц назад
Thanks to god you have come out from the lion side completely different between evil people xx
@khumalonyirenda4437
@khumalonyirenda4437 Месяц назад
Morefire Dr, micheal usi
@VincentMtambo
@VincentMtambo Месяц назад
Kaliati is Very loyal. Ndinaona nthawi ya Bingu sanathawe
@beakab2378
@beakab2378 Месяц назад
Good message, 👏👏👏
@CharityChikomo-hl1gz
@CharityChikomo-hl1gz Месяц назад
Uku ndiye akuyakhula was wondering kuti guys how can u trust Micheal usiiiii???
@BillyMhone-jp3kn
@BillyMhone-jp3kn Месяц назад
UTM siinagawanike koma tsopano tingodziwa kuti ma utm members enieni ndi atiwo Ife till nganganga pa UTM
@daviskamonde4882
@daviskamonde4882 Месяц назад
Reality!!
@suzenzulu9412
@suzenzulu9412 Месяц назад
UTM should support Kaliyati for presidency.
@AbrahamTembo-z5k
@AbrahamTembo-z5k Месяц назад
Zikuwoneka kt alibe impact ku chipani, koma ku Dziko, alinayo. PENYETSETSANI KWAMBIRI OSANGOCHITA ZINTHU ZA PHUMA ndi MKWIYO. S.K.C. pomusankha, adawonamo NZERU ndipo ambiri tinakhutira. Dr Michael Usi, ali ndi popularity across the country. Mwina poti ife tikuziwonera patali mwina.
@isabelmartin7567
@isabelmartin7567 Месяц назад
Usi si wa UTM ndipo kalikonse tikaonana pa 19 Friday li
@user-yv8hc3fd7f
@user-yv8hc3fd7f Месяц назад
We want Kabambe
@user-mj2te7vl6p
@user-mj2te7vl6p Месяц назад
This is good
@JamesIngeni-ku3qj
@JamesIngeni-ku3qj Месяц назад
Manganya is a betrayer and I can believe kut munthuyu ndi oipa nchochi
@user-nj5vu8cd5l
@user-nj5vu8cd5l Месяц назад
Vuto ku Malawi ndi kukoza or kiyanjanisa ayi ndithu koma kupasula ndi kibwelesa chidani pakati pa anthu or chipani UTM be careful mawa sikutali chilima anasankha usi chilipo chomwe anawona mwayiye
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Zoona abwana amene mukuyankhula,,pitilizani kulangiza anthu a UTM,,Bon Kalindo akufunila DPP iwine
@MsondaBanda
@MsondaBanda Месяц назад
Utn kuyaghayika
@eliasmgala8469
@eliasmgala8469 Месяц назад
Micheal Usi mukumunenayotu Chilima dolo amene timamunenayo, anamusankha iye kt akhale Vice wake enanu kukusiyani uko. And I think amaganizadi bwino munthu uja. Imagine akanasankha wina like this one or ena aja!
@GracePendame
@GracePendame Месяц назад
Ndiwakabudura uyu usi simunthu wabwino ndi yudasi uyu osamusekerera
@EliasKawuwa
@EliasKawuwa Месяц назад
Anthu a UTM mwadzadza ndi nkhwidzi pa wina ndi zake, mmalo mongwirizana chifukwa chopititsa patsongolo chipani chanu,mmalo mwatsongoza kuika patsongolo zofuna zanu,choncho mwaononga chipani Cha mwini wake Malemu SKC ,ndipo zimene mukuchitazi,anakakhara kuti SKC Ali moyo,nonse SKC anakakukwapulani kwambiri pazimene mukuchitazi,ngati mmene ambuye Yesu anachitira ataona anthu akungwiritsa tchalitchi kugulitsira malonda, the problem is,nonse mumafuna ma udindou Boma,nde mmalo mwake mwafuna kuuikira azanu ama udindo Boma, that's very bad, just feeling sorry for all UTM members kuti atsongoleri anu onse ndi adyera,ndipo chipani Cha UTM chitha movetsa Chisomo,chifukwa Cha dyera, that's why zipani zambiri Malawi muno ndi family parties,at least zimayendako, koma zinazi nde Kaya ndithu,dyera lakula mu UTM,mwaononga chipani chifukwa Cha Nsanje
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Mwana Wa njoka iwe kagwere
@AMONINICHOLAS-g2m
@AMONINICHOLAS-g2m Месяц назад
Masophenya andari ndi Chilima Inu aye Mp mikuyakhulani mulibe vision
@FrankSpison-o7o
@FrankSpison-o7o Месяц назад
Yudas 😢
@amosnyirenda-pl1ss
@amosnyirenda-pl1ss Месяц назад
wasanje ise nikaliyati wako musiyeni usi alamulile
@BellaMandala
@BellaMandala Месяц назад
Uncle shortawo bas angokhala ku MCP komko bas
@GeorgePhiri-ub2of
@GeorgePhiri-ub2of Месяц назад
anthu ofuna kugulisa utm aja ena ndakuluwa
@JustusSNkhata
@JustusSNkhata Месяц назад
Komanso kuchoka mu mgwirizano chisalhale chifukwa kuti anthu a UTM asiye kutumikila a Makawi
@CharlesChagudubuka-rm6bh
@CharlesChagudubuka-rm6bh Месяц назад
Ndipo sidzawaonaso,apa mwayankhula bwino mwandilumbitsa mtima,anandinyasatu short one ameneyu
@LivaneMsyamboza
@LivaneMsyamboza Месяц назад
Ndipo mwayakhula bwino
@user-gj4li2gc8o
@user-gj4li2gc8o Месяц назад
Onse ankayamba chonchi ndi pang'ono pang'ono uzakhumudwa atakhala nsogoleli wa ziko enanu muli ndi nkhwizi chabe ndi mzanu musiyeni ,gulu la kaliat likufuna kubwerera kwao paja ndi a dpp
@IsaacChapotera
@IsaacChapotera Месяц назад
Mau a mphamvu
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Месяц назад
Akaliayati ndi nkhalidwe lawo atamwalila abingu anachita chi.mozi mozi kunyoza mai j b ndiye amene akuziwa mai kaliyati sakudabwa ayi
@gracemkandawire8769
@gracemkandawire8769 Месяц назад
Anthu akonda ndrama ndi galimoto za Boma,,anthu Albie chikondi
@user-pt8wb4vw6r
@user-pt8wb4vw6r Месяц назад
Inu ndi adpp msatisokose ife ayi adyela ndinuyo mmene anamzuzila adpp lelo adpp bdiabwino kwachilima poti wamwamwalila ayi kaya msanyoze ausi ayi i u ndiamene mkufuna kugulisa chipani kwa adani
@user-wd9yd1bg9n
@user-wd9yd1bg9n Месяц назад
Muziti poti mcp ysmupha nanga mukubisa chani
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Ana anjoka inu mukhalira yomweyo
@beakab2378
@beakab2378 Месяц назад
DPP mukuinyozayo inamusiya Chilima apite wamoyo, iye nkumainyoza nkupita ku ng'ona zokupha. Phunziranipo phunziro.
@user-hm9nc7lz6e
@user-hm9nc7lz6e Месяц назад
Mau omveka bwino micheal utsi pomwe anaoneketa kuti si wa utm ndi nthawi ya maliro achilimA osayakhula chili conse kungofziwiratu kuti ndiyemwe anapereka chilima manja mwa chakwera ndiye manganya si wautm koma mcp
@SildaKatundu
@SildaKatundu Месяц назад
Tisankhe Patricia Kaliati kukhala president .Ndipo ndi munthu olimbikira ,opanda mantha komanso ochuluka mmalawi muno timamudziwa ndi kumukonda
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Zoona Patricia Kaliati mpando omwe Ali akhale omweo
@user-hr6dj4xc8l
@user-hr6dj4xc8l Месяц назад
😂😂😂😂 uko kunali kulira kwa anamalra
@hissimajohn965
@hissimajohn965 Месяц назад
Za ziii
@retirementtoafrica
@retirementtoafrica Месяц назад
Alindi impact mudziko lamalawj kuyambira kelekale. Sagawa masweet.
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di Месяц назад
Say NO to Kabambe (utm presidency)
@user-er7ub4ug7y
@user-er7ub4ug7y Месяц назад
Atumidwa ndi MCP awa
@JaneMoyo-ws2di
@JaneMoyo-ws2di Месяц назад
Awalandire alendo ofuna kulowa UTM koma osati zogulisa chipani kumpasa obwera (mlendo) kumpatsa u president kodi nkatimwanu mulibe angaimire u president? Mene mwavutikira basi mukagulisa chipani iyo ndi trick Say NO to Kabambe (UTM presidency) pls
Далее
Woman = best friend🤣
00:31
Просмотров 3,7 млн
Ati Gule uyu Salivina Bwino Mmbwalo.
7:28
Просмотров 12 тыс.
Ndikuopsyezedwa Chifukwa Cha Ma VN - Pastor Shumba
16:55
sendera sisters-patali
2:00
Просмотров 4,5 тыс.
Woman = best friend🤣
00:31
Просмотров 3,7 млн