Тёмный

JOSHUA VARELA KUDZUDZULA MKHALIDWE OIPA OKHUDZA IMFA YA SAULOS CHILIMA 

MALAWI TODAY
Подписаться 10 тыс.
Просмотров 85 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

13 окт 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 69   
@MaggieCement
@MaggieCement 2 месяца назад
Amen Mary apume abale olo ine zinandibowa kwabasi kuwayankhula bwino akubanja Muthu akhudze imfa ya munake koma Ambuye amukhuze Mary muthawi yowawitsayi
@shayrafernandeslatif9556
@shayrafernandeslatif9556 2 месяца назад
MHSRIP 🌹 may almighty God still xomfort the family to be strong ameen
@LouisAndrew-jr1yj
@LouisAndrew-jr1yj 2 месяца назад
Indeed we lost a strong man 🕊️😭😍
@MemoryKaunda-bx3ii
@MemoryKaunda-bx3ii 2 месяца назад
ineyo zoti chilima anamwalira sindikhulupilirabe aaaaaaa😭😭😭😭
@PotipherMithi-qz4rr
@PotipherMithi-qz4rr 2 месяца назад
Exactly my dear
@Saeedibn
@Saeedibn 2 месяца назад
Nde pita ukamutenge komwe alikotu ngati sukukhulupulira
@ovahamalambo2676
@ovahamalambo2676 2 месяца назад
Ineso, kuvomeleza kuvuta 😢😢😢😢
@TamikaKaponya
@TamikaKaponya 2 месяца назад
zikomo​@@Saeedibn
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 2 месяца назад
Nanga zot Yesu Khristu ndi Ambuye do you believe this??
@ThokoLungu-tq6pw
@ThokoLungu-tq6pw 2 месяца назад
Skc 😭😭why? Only almighty God knows everything. Abieni 😭😭😭😭😭
@MariamJohn-dg4em
@MariamJohn-dg4em 2 месяца назад
Yamakenduloyo mukunama anthu sangasiye, Rest in peace SKC
@lindaphiri3543
@lindaphiri3543 2 месяца назад
Ine usi yo akungondinyasa
@victorbanda9039
@victorbanda9039 2 месяца назад
Onyasa kwambiri ndiiweyo
@JoyceGondwe-ve1zu
@JoyceGondwe-ve1zu 2 месяца назад
Kulankhula motani. Nsanje basi. Whether you like it or not he's the vice president. The Bible says respect your leasers.
@SamuelThanganyika
@SamuelThanganyika 2 месяца назад
Biyeni😭MYSRIP.
@Princessmary-wf6bk
@Princessmary-wf6bk 2 месяца назад
We lost a strong man 😭😭😭
@ReubenGama
@ReubenGama 2 месяца назад
Mukumva bwanji amagazi m'manja inu, simunati candlelight ija ikuotchani m'matako zenizeni, kupha anthu 9 ma million aziombela m'manja zopusazo in multiparty system of government, kale lomwelija chifukwa chipani chidali chimodzi, anthu chisoni mbiri yanu idzapindula chani padziko lapansi pano. 😢😢
@emmanuelchokocha
@emmanuelchokocha 2 месяца назад
I miss him already kulira kwake kaya mkumatan mmmh
@MercyJohnsonkanchure
@MercyJohnsonkanchure 2 месяца назад
😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
@atupelemposa4786
@atupelemposa4786 2 месяца назад
Am still in denial
@MarthaPhiri-q8m
@MarthaPhiri-q8m 2 месяца назад
Mau abwino ndithu 🙏
@GloriaChikwawe
@GloriaChikwawe 2 месяца назад
Mtima udakawawabe ine 😢😢😢😢
@AustinMilazi
@AustinMilazi 2 месяца назад
Hi
@MikeTwaibu-i1h
@MikeTwaibu-i1h 2 месяца назад
Kunena zoona chilima anakhiyidwa , komanso munthu amene uja anatipwetekesa, koma sanachite bwino kumuchita chiwembu
@GIFTNAMPINGA
@GIFTNAMPINGA 2 месяца назад
MWADYA BANZI INUUUU
@fannyzimba149
@fannyzimba149 2 месяца назад
Amen indeed 😭 😭 😭
@VictoriaSibande
@VictoriaSibande 2 месяца назад
Inu mkumayimba fon kwa Mary Chilima ndinu opusa zichepe zimenezo mkufuna mumutani zitsiru
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 2 месяца назад
Kumakana ndithu AAA osazamuyimbila phone my chilima ,musiyen alire malilo amwamuna wake
@Hellenistic109
@Hellenistic109 2 месяца назад
😭😭😭😭😭😭😭😭
@SildaKatundu
@SildaKatundu 2 месяца назад
Ngopanda mantha chani, mmesa anali ndi asilikali mbweeee kuposa okafufuza ndege ya SKC and 8 others
@jacquechisale6809
@jacquechisale6809 2 месяца назад
Komano akubanja mwaiwala kutiko chilima anali ndani ... anthutu sasiya kupitako kumandako coz muthu uja anthu amamukonda
@rashidadan2533
@rashidadan2533 2 месяца назад
Mukafatsakwambili chipanicha UTM chitha , akulu aja anali ofasa mozipweteka okha
@EsetaGerate
@EsetaGerate 2 месяца назад
😭😭😭😭
@NattyMaloni
@NattyMaloni 2 месяца назад
Pumulani mwa Ambuye
@Musa1828-l5d
@Musa1828-l5d 2 месяца назад
Yama kandulo sikutha mpaka zaka 50 muuzane a MCP
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh 2 месяца назад
Muyaluka osamakayatsa pokumbukira Bingu wanuyo
@directorvjshiiz7104
@directorvjshiiz7104 2 месяца назад
Koma ngati sewero inu zoti chilima anamwalira mmmmmmmm
@MelissaMondey
@MelissaMondey 2 месяца назад
😭😭😭😭😭🙏🙏🙏👍🕊️
@MartinOdala-wb9mt
@MartinOdala-wb9mt 2 месяца назад
@DjshukulanGift
@DjshukulanGift 2 месяца назад
Kwambili
@CosmasChikwindi
@CosmasChikwindi 2 месяца назад
Uku ndiko kulankhula osati zomwe akulankhula azibusa opusa analowa ubusa chifukwa chosowantchito.
@AchinaKellz
@AchinaKellz 2 месяца назад
Ine siwandale koma ndimava kuwawa achakwera munaganiza Bwanji?
@charlesmbale7739
@charlesmbale7739 2 месяца назад
Tilira mpaka kalekale
@gersommalama
@gersommalama 2 месяца назад
Mau amphabvu kwambiri. Zikoma kwambiri
@saimonekatole3288
@saimonekatole3288 2 месяца назад
Zovu zed
@ChifundoZimba-jh7dh
@ChifundoZimba-jh7dh 2 месяца назад
DPP ili pa ganyu koma ikulenga kwambili
@AchinaKellz
@AchinaKellz 2 месяца назад
Manganya garu akuzatani😢mfiti
@KassimSteven
@KassimSteven 2 месяца назад
Gona bwino chimwene mabara mutima anakawawabe nzimu wako uwuse mutendere wosatha ame
@DeresiMbewe
@DeresiMbewe 2 месяца назад
Zoonadi
@YamikanChirwa
@YamikanChirwa 2 месяца назад
Ngat bodza
@SolokingChimzy-yt7dj
@SolokingChimzy-yt7dj 2 месяца назад
Mwana wa nkaz wa achilima uli ndi mphuno yosefukila bwino kwambir
@PaulMvuma
@PaulMvuma 2 месяца назад
But why a dpp people were there whalist they hurted this man called chilima that's funny
@amoschisisi2070
@amoschisisi2070 2 месяца назад
The people who hated chilima are the MCP people
@CosmasChikwindi
@CosmasChikwindi 2 месяца назад
Awanso amakendulowa muwalese zomwe akupanga atsokoneza dziko, kulila aphatikiza ndi ndale
@UseniMailosi
@UseniMailosi 2 месяца назад
Aàaa makendulo alipo pakaaa
@BrightZionga
@BrightZionga 2 месяца назад
Kkkkkk wakutuma ken msonda 😂😂😂 mfiti imadana ndi mapemphero fire🔥🔥🔥
@MadaBuleya
@MadaBuleya 2 месяца назад
Iweyo ngati zikukunyasa zama candle usamazisate its not your business
@BillyKalambo-jx3vf
@BillyKalambo-jx3vf 2 месяца назад
Za candle sitisiya ndipo iweyo chikukhuza ndichani ngati Eni akewo akuti tilira mpaka kale kale nafeso ma candle tiyasa mpaka kale kale Chilima anali wandale ifeso tikulira malirowo mwa ndale ndiye zikukhuzani ndichani
@LukaThawe
@LukaThawe 2 месяца назад
Candle 🕯️🕯️🕯️ group
@yowasschitsosa5348
@yowasschitsosa5348 2 месяца назад
Muuzeni kalindo, ndi mtanyiwa apeleke ulemu ku banja misala yakeyo akapangile infa ya alomwe anzake,
@Tawina0101
@Tawina0101 2 месяца назад
Iwe Machende ako wamva
@RachealPongolani
@RachealPongolani 2 месяца назад
😂😂😂😂​@@Tawina0101
@FidelisNthenda-qq5sg
@FidelisNthenda-qq5sg 2 месяца назад
😭😭😭
Далее
А я с первого раза прошла (2024)
01:00
Мои нет в ЛАПКЕРАХ
00:11
Просмотров 322 тыс.
Gwanda's Funeral - Last Sermon
25:21
Просмотров 160 тыс.
Brian With Msonda // Zingaiwalike
8:37
Просмотров 28 тыс.
Top 6 Most Protected Presidents in East Africa 2024
8:57