Amen Mary apume abale olo ine zinandibowa kwabasi kuwayankhula bwino akubanja Muthu akhudze imfa ya munake koma Ambuye amukhuze Mary muthawi yowawitsayi
Za candle sitisiya ndipo iweyo chikukhuza ndichani ngati Eni akewo akuti tilira mpaka kale kale nafeso ma candle tiyasa mpaka kale kale Chilima anali wandale ifeso tikulira malirowo mwa ndale ndiye zikukhuzani ndichani