Тёмный
No video :(

AFORD AKUPEPHA UTM KUTI APANGE ALLIANCE- ZOMWE ZAYANKHULIDWA KU NSOKHANO 

HOT 265
Подписаться 74 тыс.
Просмотров 23 тыс.
50% 1

Опубликовано:

 

12 июл 2024

Поделиться:

Ссылка:

Скачать:

Готовим ссылку...

Добавить в:

Мой плейлист
Посмотреть позже
Комментарии : 66   
@RachelDongolosi
@RachelDongolosi Месяц назад
Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe
@BlessigsChabzola
@BlessigsChabzola Месяц назад
😊09
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga Месяц назад
MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO
@jameshuwanzulu
@jameshuwanzulu Месяц назад
ubwino wake simukavota nokha
@user-fl6zc5gz5r
@user-fl6zc5gz5r Месяц назад
Ndilibe lawyer mkanakuyankha
@GiftJulius-gx2kb
@GiftJulius-gx2kb 23 дня назад
Utm udf my vote
@doreenkaliati3166
@doreenkaliati3166 Месяц назад
That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano
@chrispinechirwa2655
@chrispinechirwa2655 Месяц назад
Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢
@marthaphiri3600
@marthaphiri3600 Месяц назад
Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.
@chrisboyce2
@chrisboyce2 Месяц назад
UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance
@KikaImran
@KikaImran Месяц назад
You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies
@josephgabriel1016
@josephgabriel1016 Месяц назад
Timothy sangatinamize for the second time.....
@RobertGoliat-gt2qh
@RobertGoliat-gt2qh Месяц назад
Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤
@YasinMusa-ym8lp
@YasinMusa-ym8lp Месяц назад
Bomo ylo ❤
@LuwisKaigwaze-gr6cg
@LuwisKaigwaze-gr6cg Месяц назад
Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford
@WatipaCawinga
@WatipaCawinga Месяц назад
Magufuli wathu kupoto
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja
@JumaGadaff
@JumaGadaff Месяц назад
Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu
@jamessoko9480
@jamessoko9480 Месяц назад
Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.
@user-hh4wn4vf9e
@user-hh4wn4vf9e Месяц назад
Amen 🙏
@johnussenu2848
@johnussenu2848 Месяц назад
Utm and udf boma
@yusufsadic2930
@yusufsadic2930 Месяц назад
Wabodz uyu Mumater mukamafun mavot Mumakhal ngat anthabwino Chilimanso amater Chakweranso amater
@IshmailDukuturu
@IshmailDukuturu Месяц назад
Mbuzi iyi Timothy
@WanangwaMfune
@WanangwaMfune Месяц назад
Join
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤
@PrinceKachimanga
@PrinceKachimanga Месяц назад
Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂
@user-rg9zc6eo2q
@user-rg9zc6eo2q Месяц назад
My vote afod
@user-tb6yh1kx3o
@user-tb6yh1kx3o Месяц назад
Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere
@user-bv8wo2fn4e
@user-bv8wo2fn4e Месяц назад
I hope if all mupoto must vote for AFORD
@yassinn5634
@yassinn5634 Месяц назад
Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Chihana is my vote
@PeterPhiri-u7h
@PeterPhiri-u7h Месяц назад
MuKufuna alliance mukuopa chani
@Dickies-mk8cd
@Dickies-mk8cd Месяц назад
Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.
@BwanaGD
@BwanaGD Месяц назад
Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa
@Donnex-gn2sf
@Donnex-gn2sf Месяц назад
Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣
@user-qp8kh2hj9o
@user-qp8kh2hj9o Месяц назад
Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂
@alickkachepa3801
@alickkachepa3801 Месяц назад
Move
@ntombiunice8637
@ntombiunice8637 Месяц назад
Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera
@yassinn5634
@yassinn5634 Месяц назад
Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.
@ChrifordBiziel
@ChrifordBiziel Месяц назад
Zimenezo2 zithera konko mwene
@Syakinongwa
@Syakinongwa Месяц назад
Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.
@user-wk7ut7ld1x
@user-wk7ut7ld1x Месяц назад
Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction
@BestonChagala
@BestonChagala Месяц назад
Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential
@BestonChagala
@BestonChagala Месяц назад
Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa
@BrightNyoni-yd4ip
@BrightNyoni-yd4ip Месяц назад
Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana
@user-im7sc2my4w
@user-im7sc2my4w Месяц назад
I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina
@actuarialscience2283
@actuarialscience2283 Месяц назад
Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.
@user-jn9tz3li3v
@user-jn9tz3li3v Месяц назад
Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta
@HappyAntenna-sf9qx
@HappyAntenna-sf9qx Месяц назад
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
@BestonChagala
@BestonChagala Месяц назад
Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD
@MercyNkhoma-b6h
@MercyNkhoma-b6h Месяц назад
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
@Pangolinimw
@Pangolinimw Месяц назад
🫡🫡🫡🫡🫡🫡
@samdiverson9733
@samdiverson9733 Месяц назад
Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP
@spargomw
@spargomw Месяц назад
I agree with you 100%❤❤
@emmanuelsambo1158
@emmanuelsambo1158 Месяц назад
It was only SKC
@MercyNkhoma-b6h
@MercyNkhoma-b6h Месяц назад
Koma chaka chino ziliko ndithu.
@MosesNyalugwe-ll8hh
@MosesNyalugwe-ll8hh Месяц назад
Maloto achumba
@chrispinechirwa2655
@chrispinechirwa2655 Месяц назад
Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂
@VungaQueen
@VungaQueen Месяц назад
Kkkk😂😂😂😂😂
@chrisgremu740
@chrisgremu740 Месяц назад
Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?
@petertaulo8014
@petertaulo8014 Месяц назад
Sangawine mark my words
@user-eh1gn1nj9d
@user-eh1gn1nj9d Месяц назад
Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu
@TiyesNayuma
@TiyesNayuma Месяц назад
Chitsilu iweyo you failed as a minister
@HappyAntenna-sf9qx
@HappyAntenna-sf9qx Месяц назад
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
@MercyNkhoma-b6h
@MercyNkhoma-b6h Месяц назад
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
Далее
BRIAN BANDA NDI A PETER MUNTALIKA
24:42
Просмотров 523
OKWOGELA KWA FRANK GASHUMBA MUKUZIIKA TAMALE MIRUNDI
8:20
DR MICHAEL USI TSOPANO KUYANKHULA
13:08
Просмотров 405
BRIAN NDI A SHADRICK NAMALOMBA KUPANIKIZANA MAFUSO
32:31
KUYANKHULA KWA PETER MUNTALIKA🙌🙌
23:27
Просмотров 3,4 тыс.
KAMLEPO KALUA KUYANKHULA MOSAOPA 🙌
23:27
Просмотров 9 тыс.
UKU KWATELERA MUPWETEKANA MAFUNSO
22:13
Просмотров 8 тыс.
DPP CONVENTION KU BLANTYRE UKU KWACHEMA🙌🙌
23:36