Osamathamangila kuweruza sionse abodza ena ndiophera km Ali asatanic amenewo ndye abodza osamatenga opephera ose ndabodza ena akupemphera Ali thumwi zasatana ena akupemphera Ali ake Eni Eni aMulungu samalani poyakhula
Komatu nyimbo zinazi ndiutumiki eish, am not here to judge but sometimes we have to ask yourself about your position .mkazi wabusa kukonda nyimbo za anthu ovula kuchita kuyitsata
12 years nkukhala uli pa banja? after might prayers anakhailita yekha yekha ndi family ya abusa zoona? anali ndi mission mzimayiyu ulape ulape plz mzimayi iwe chonde
inenso ndikuona boza mu story iyi bcz sanali maneba how come osungitsa key. adutse wapafupi kwambiri? again munthu omukonda ngati akuthetsa chibwenzi akanafunsa why? whats wrong? ndiwachimaso maso pastor ameneyo